< Gesami Hea:su 81 >
1 Ninia Gaga: su Hina Gode Ema nodone wele sia: ma! Ya: igobe ea Gode Ema nodone gesami hea: ma!
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a gititi. Salimo la Asafu. Imbani mwachimwemwe kwa Mulungu mphamvu yathu; Fuwulani mokweza kwa Mulungu wa Yakobo!
2 Ilibu muni ba: gu da la: idi la: idi figi amoga duma. Noga: le hanai nabima: ne, ilibu amola sani baidama duma.
Yambani nyimbo, imbani tambolini imbani pangwe wolira bwino ndi zeze.
3 Lolo nasea, oubi da genoni aligila heda: i lelea amola oubi da ufa manea, dalabede fulaboma.
Imbani lipenga la nyanga ya nkhosa yayimuna pa mwezi watsopano, ndi pamene mwezi waoneka wonse, pa tsiku la phwando;
4 Amo da Isala: ili fi ganodini sema agoane hamoi, amola amo Ya: igobe ea Gode Hi hamoma: ne sia: i.
ili ndi lamulo kwa Israeli, langizo la Mulungu wa Yakobo.
5 Gode da Idibidi soge amoma doagala: loba, E da amo hamoma: ne sia: i Isala: ili dunu ilima iasi. Na da Dia hame dawa: sia: amoga agoane sia: be nabala,
Iye anapereka lamulolo kwa zidzukulu za Yosefe pamene anatuluka kulimbana ndi Igupto, kumene tinamva chiyankhulo chimene sitinachidziwe.
6 “Na da dilia baligia dioi dialu amo fadegale fasi. Na da osoboga hamoi igi dilia gaguli ahoasu amo ligisima: ne logo doasi.
Iye akunena kuti, “Ine ndinachotsa zolemetsa pa mapewa awo; Manja awo anamasulidwa mʼdengu.
7 Dilia da dilima bidi hamosu doaga: beba: le Nama wele sia: i, amola Na da dili gaga: i. Na da Na wamoaligisu soge mulu amo ganodini esala, dia sia: amoma dabe sia: i. Na da Meliba guhano amoga dilima adoba: su hamoi.
Pa mavuto anu munayitana ndipo ndinakulanditsani, ndinakuyankhani kuchokera mʼmitambo ya mabingu; ndinakuyesani pa madzi a ku Meriba. (Sela)
8 Na dunu, Na sisa: ne sia: be amo nabima. Isala: ili fi! Abuli hamone Na sia: nabima: bela: ?
“Imvani anthu anga, ndipo ndidzakuchenjezani ngati mungathe kumvetsera, Inu Israeli!
9 Dilia da eno Godema maedafa nodone sia: ne gadoma.
Musadzakhale ndi mulungu wachilendo pakati panu; musadzagwadire mulungu wina.
10 Na da dilia Hina Gode. Dili Idibidi soge ganodini esaloba, Nisu da dili fadegai. Dilia lafi dagale gama, amasea Na da diligili ha: i manu mugusimu.
Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndinakutulutsani mʼdziko la Igupto. Yasamani kukamwa kwanu ndipo ndidzakudyetsani.
11 Be Na dunu ilia da Na sia: be hame nabi. Isala: ili ilia da Na sia: be didili hame hamoi.
“Koma anthu anga sanandimvere; Israeli sanandigonjere.
12 Amaiba: le, Na da ilisu gasa fi hou hamonanoma: ne yolesi, amola ili hanai hamoma: ne yolesi.
Kotero ndinawasiya ndi mitima yawo yosamverayo kuti atsate zimene ankafuna.
13 Abuli hamone Na fi dunu ilia da Na sia: nabima: bela: , abuli hamone ilia da Na sia: didili hamoma: bela: ?
“Anthu anga akanangondimvera, Israeli akanatsatira njira zanga,
14 Ilia da agoai hamomu ganiaba, Na da hedolowane ilima ha lai dunu ili hasalasila: loba, amola ilima ha lai dunu huluane ilima gasa fili hasalasila: loba.
nʼkanafulumira motani kuti ndigonjetse adani awo ndi kutembenuza mkono wanga kulimbana ndi amaliwongo!
15 Nama higale ba: su dunu ilia da beda: iba: le, na midadi dialuma fili begudumu. Ilima se bidi iasu da maedafa yolele, gebewane dialumu.
Iwo amene amadana ndi Yehova akanakhwinyata pamaso pake, ndipo chilango chawo chinakakhala mpaka kalekale.
16 Be amomane Na da dilima widi ha: i manu ianumu amola na da dili sadima: ne soge agime hano moma: ne imunu.”
Koma inu mukanadyetsedwa tirigu wabwino kwambiri; ndikanakukhutitsani ndi uchi wochokera pa thanthwe.”