< Gesami Hea:su 75 >

1 Gode! Ninia da Dima nodone sia: sa! Ninia da Dima nodone sia: sa! Ninia da Di gasa bagade hou amo sisia: i laha. Dia noga: idafa hamoi liligi amo sisia: i laha.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe, potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Salimo la Asafu. Nyimbo. Tikuthokoza Inu Mulungu, tikuthokoza, pakuti dzina lanu lili pafupi nafe, anthutu amafotokoza za ntchito zanu zodabwitsa.
2 Gode da amane sia: sa, “Na da fofada: su eso amo ilegei dagoi. Amola Na da moloidafawane fofada: mu.
Mumati, “Ine ndimayika nthawi yoyenera, ndine amene ndimaweruza mwachilungamo.
3 Osobo bagade hisu da igugumu, amola esalebe liligi huluane da fofogomu. Be na da osobo bagade ea bai amo mae muguluma: ne ga: nasilisimu.
Pamene dziko lapansi ndi anthu ake onse anjenjemera, ndine amene ndimagwiriziza mizati yake molimba. (Sela)
4 Na da wadela: i hamosu dunu ilima, ilia da mae gasa fima: ne sia: sa.
Kwa odzitama ndikuti, ‘Musadzitamenso,’ ndipo kwa oyipa, ‘Musatukulenso nyanga zanu.
5 Ilia da ilia hidale sia: su yolesima: ne Na da sia: sa.”
Musatukule nyanga zanu motsutsana ndi kumwamba; musayankhule ndi khosi losololoka.’”
6 Fofada: su houdafa da gusudili o guma: dini o gadili (north) o la: idi gadili (south) amoganini hame maha.
Kugamula milandu sikuchokera kummawa kapena kumadzulo kapena ku chipululu.
7 Be fofada: su dunudafa da Gode Hi fawane. E da dunu mogili se dabe lama: ne iaha amola mogili da moloiba: le, se dabe mae lama: ne fisiagasa.
Koma ndi Mulungu amene amaweruza: Iyeyo amatsitsa wina, nakwezanso wina.
8 Hina Gode da fedege agoane faigelei ea loboga gagusa. Amo ganodini sali da gasa bagade waini hano ba: sa. Amo waini hano da fedege agoane Ea ougi bagade. E da amo sogadigili, amola wadela: i hamosu dunu da amo naha. Ilia da amo waini hano huluanedafa naha ebelesa.
Mʼdzanja la Yehova muli chikho chodzaza ndi vinyo wochita thovu, wosakanizidwa ndi zokometsera; Iye amamutsanulira pansi ndipo onse oyipa a dziko lapansi amamwa ndi senga zake zonse.
9 Be na da mae fisili, Ya: igobe ea Gode Ea hou eno dunuma sisia: i lale, Ema nodone gesami hea: lalumu.
Kunena za ine, ndidzalengeza izi kwamuyaya; ndidzayimba matamando kwa Mulungu wa Yakobo.
10 E da wadela: i hamosu dunu ilia gasa amo fifilisimu. Be E da moloidafa dunu ilia gasa amo fufugilisimu.
Ndidzadula nyanga za onse oyipa koma nyanga za olungama zidzakwezedwa.

< Gesami Hea:su 75 >