< Gesami Hea:su 74 >

1 Gode! Di da abuliba: le amaiwane nini higale fisiagabela: ? Di da Dia fidafa dunu ilima eso huluane ougiwane dialoma: bela: ?
Ndakatulo ya Asafu. Nʼchifukwa chiyani mwatitaya ife kwamuyaya, Inu Mulungu? Chifukwa chiyani mkwiyo wanu ukutukutira pa nkhosa za busa lanu?
2 Dia fi dunu amo bu dawa: ma! Di da musa: hemonega Dia fi dunu Disu ili ilegele lai. Ilia da udigili hawa: hamonanu. Be Di da ili amoga fadegale, Dia fidafa esaloma: ne gadili oule asi. Di da musa: Saione Goumia esalu. Amo bu dawa: ma!
Kumbukirani anthu amene munawagula kalekale, fuko la cholowa chanu, limene Inu munaliwombola, phiri la Ziyoni, kumene inuyo mumakhala.
3 Saione Moilai Bai Bagade mugului amoba: le ososa: masa. Ninia ha lai da liligi huluane Debolo ganodini galu amo wadela: lesi dagoi.
Tembenuzani mapazi kuloza ku mabwinja awa amuyaya chiwonongeko ichi chonse mdani wabweretsa pa malo opatulika.
4 Dima ha lai dunu ilia hasalasisa gugulubi da Debolo diasu ganodini nabi dagoi. Ilia da ilia hasalasu olelema: ne, ilia da ilia eso gosagisu amogawi bugi dagoi.
Adani anu anabangula pa malo pamene Inu munkakumana nafe; anayimika mbendera zawo monga zizindikiro zachigonjetso.
5 Ilia da ifa damusu dunuga ifa goaheiga damuni salabe, agoaiwane ba: su.
Iwo anachita ngati anthu oti anyamula mbendera zawo kuti adule mitengo mʼnkhalango.
6 Ilia da ifa gaga: i huluane amo ilia goahei amola ha: ma bagade amoga gagoudane salasu.
Kenaka anaphwanya ndi nkhwangwa ndi akasemasema awo zonse zimene tinapachika.
7 Ilia da Dia Debolo wadela: lesili, laluga ulagisi. Ilia da sogebi amoga dunu da Dima nodone sia: ne gadosu, amo ledo hamone, wadela: lesi dagoi.
Iwo anatentha malo anu opatulika mpaka kuwagwetsa pansi; anadetsa malo okhalamo dzina lanu.
8 Ilia da nini huluanedafa gugunufinisimusa: hanai galu. Hadigi sogebi huluanedafa Isala: ili soge ganodini galu, amo ilia da ulagili sali.
Ndipo anati mʼmitima yawo, “Tawatha kwathunthu.” Anatentha malo aliwonse amene Mulungu amapembedzedwerako mʼdzikomo.
9 Ninia sema dawa: digima: ne olelesu liligi huluane da asi dagoi, hame ba: sa. Balofede (Gode Sia: Alofesu dunu) afae yolesi da hamedafa. Amola dunu afaega amo hou dagomu eso hame dawa:
Ife sitinapatsidwe chizindikiro chodabwitsa; palibe aneneri amene atsala ndipo palibe aliyense wa ife akudziwa kuti izi zidzatenga nthawi yayitali bwanji.
10 Gode! Habowali seda ninima ha lai dunu ilia da Diba: le oufesega: noma: bela: ? Ilia da eso huluane mae fisili gebewane Dia Dio gadela: loma: bela: ?
Kodi mpaka liti, mdani adzanyoze Inu Mulungu? Kodi amaliwongowa adzapeputsa dzina lanu kwamuyaya?
11 Abuliba: le Dia da nini fidimu higabela: ? Abuliba: le Dia lobo da baligiagai ganabela: ?
Chifukwa chiyani mukubweza dzanja lanu lamanja? Litulutseni kuchoka pachifuwa chanu ndipo muwawononge!
12 Gode! Di da osobo bagade hamoia amogainini, ninima Hina Bagade esalu. Di da eso bagohame nini gaga: lalu.
Koma Inu Mulungu, ndinu Mfumu yanga kuyambira kalekale; Mumabweretsa chipulumutso pa dziko lapansi.
13 Di da Dia gasa bagade amoga hano wayabo bagade amo dogoa hedofalesi. Amola hano wayabo bagade ohe fi liligi ilia dialuma goudai.
Ndinu amene munagawa nyanja ndi mphamvu yanu; munathyola mitu ya zirombo za mʼmadzi.
14 Di da ohe bagade (Lefaiada: ne) ea dialuma sasalugufai amo goudanesili, ea da: i amo hafoga: i sogega ohe fi iligili moma: ne i.
Ndinu amene munaphwanya mitu ya Leviyatani ndi kuyipereka ngati chakudya cha zirombo za mʼchipululu.
15 Di da hano bubuga: su amola gu hano masa: ne doasi. Di da hano bagade amo hale, hafoga: lesi.
Ndinu amene munatsekula akasupe ndi mitsinje, munawumitsa mitsinje imene siphwa nthawi zonse.
16 Di da gasi amola hayo hahamoi. Di da eso amola oubi elea lelebe sogebi amoga sagasi.
Masana ndi anu ndipo usiku ndi wanunso; Inuyo munakhazikitsa dzuwa ndi mwezi.
17 Di da osobo bagade ea alalo hamoi. Di da woufo amola ode i amo hahamoi.
Ndinu amene munakhazikitsa malire onse a dziko lapansi; munakhazikitsa chilimwe ndi dzinja.
18 Be Hina Gode! Dima ha lai dunu ilia Dima ousa. Amola ilia Di hame dawa: amola Dima higasa. Amo Di bu dawa: ma.
Kumbukirani momwe mdani wakunyozerani Inu Yehova, momwe anthu opusa apeputsira dzina lanu.
19 Dia fi gasa hamedei dunu, ilia dodona: gi ha lai dunu ilima hasalasisa: besa: le, ili mae fisiagama! Dia fi dunu da enoga se bagade nababeba: le, amo mae gogolema.
Musapereke moyo wa nkhunda yanu ku zirombo zakuthengo; nthawi zonse musayiwale miyoyo ya anthu anu osautsidwa.
20 Dia ninima sema gousa: su hamoi amo bu dawa: loma! Ninia soge amo ganodini, gasi dunasi la: idi bega: asili la: idi bega: , amo ganodini bidi hamosu amola wili gala: su fawane ba: sa.
Mukumbukire pangano lanu, pakuti malo obisika a mʼdziko asanduka mochitira zachiwawa zochuluka.
21 Dia banenesi fi dunu mae gogosiama: ma! Amola hame gagui hahani dunu Dima nodone sia: ma: ma!
Musalole kuti osautsidwa abwerere mwamanyazi; osauka ndi osowa atamande dzina lanu.
22 Gode! Di wa: legadoma! Dia hou heda: ma: ne gaga: ma! Gode Ea hou hame dawa: dunu ilia hahabe asili daeya huluane Diba: le oufesega: sa, amo dawa: ma.
Dzukani Inu Mulungu ndipo dzitetezeni pa mlandu; kumbukirani momwe opusa akukunyozerani tsiku lonse.
23 Dima ha lai dunu ilia da Dima ougiba: le, mae fisili halalalebe, amo mae gogolema!
Musalekerere phokoso la otsutsana nanu, chiwawa cha adani anu, chimene chikumveka kosalekeza.

< Gesami Hea:su 74 >