< Gesami Hea:su 71 >

1 Hina Gode! Na da Dia gaga: ma: ne Dima misi. Nama enoga maedafa hasalasima: ma!
Mwa Inu Yehova ine ndathawiramo; musalole kuti ndichititsidwe manyazi.
2 Bai Di da moloidafaba: le, na fidili gaga: ma. Na sia: nabawane, na gaga: ma!
Mundilanditse ndi kundipulumutsa mwa chilungamo chanu, mutchere khutu lanu ndi kundipulumutsa.
3 Dia na ougihalisima! Na gaga: musa: , na gagili salima! Di da na gagili salasu amola gaga: sudafa gala.
Mukhale thanthwe langa lothawirapo, kumene ine nditha kupita nthawi zonse; lamulani kuti ndipulumuke, pakuti Inu ndinu thanthwe langa ndi linga langa.
4 Na Gode! Wadela: i amola dodona: gi dunu da na wadela: lesisa: besa: le, na gaga: ma!
Landitseni Inu Mulungu wanga, kuchoka mʼdzanja la oyipa, kuchoka mʼdzanja la oyipa ndi anthu ankhanza.
5 Hina Gode! Na da Dima dafawane hamoma: beyale dawa: sa! Na da na goihadini eso amoganini, Dima dafawaneyale dawa: su.
Pakuti Inu mwakhala chiyembekezo changa, Inu Ambuye Wamphamvuzonse, chilimbikitso changa kuyambira ndili mwana.
6 Na da na esalusu huluane Dima fa: no bobogesu. Na lalelegei eso amoganini, Dia da na gaga: i. Na da eso huluane Dima nodone sia: mu.
Kuyambira pamene ndinabadwa, ndakhala ndikudalira Inu; Inu munanditulutsa mʼmimba mwa amayi anga, ndipo ndidzakupembedzani nthawi zonse.
7 Na da Dia hou gasawane lalegaguiba: le, dunu bagohame da Dia hou lalegagui. Bai Di da na gasa bagade gaga: su dunu galu.
Ine ndakhala chinthu chodabwitsa kwa anthu ambiri koma Inu ndinu wonditchinjiriza wamphamvu.
8 Hahabe asili daeya, na da Dima nodone sia: sa amola Dia hadigi eno dunuma sisia: i laha.
Pakamwa panga padzaza ndi matamando anu, kulengeza ulemerero wanu tsiku lonse.
9 Na da da: i hamoiba: le, na mae higale yolesima! Na da da: i hamone gasa hamedeiba: le, na mae higale yolesima!
Musanditaye pamene ndakalamba; musandisiye pamene mphamvu zanga zatha.
10 Nama ha lai dunu da na fane legemusa: hanai gala. Ilia da na fane legemusa: ilegele sia: daha.
Pakuti adani anga ayankhula motsutsana nane; iwo amene amadikira kuti andiphe amapangana pamodzi.
11 Ilia da amane sia: sa, “Gode da amo dunu fisiagai dagoi. Ninia da e bobogele, gagula: di! E gaga: mu dunu da hame gala.”
Iwo amati, “Mulungu wamusiya; mutsatireni ndi kumugwira, pakuti palibe amene adzamupulumutse.”
12 Gode! Nama badiliadafa mae esaloma! Na Gode! Hedolo na fidila misa!
Musakhale kutali ndi ine Inu Mulungu, bwerani msanga, Inu Mulungu wanga; thandizeni.
13 Dunu amo ilia da nama doagala: sa, amo hasalasili, gugunufinisima: ma! Dunu amo ilia da nama se ima: ne hamosu dunu, amo gogosiama: ma!
Ondineneza anga awonongeke mwa manyazi, iwo amene akufuna kundipweteka avale chitonzo ndi manyazi.
14 Na da eso huluane Dima dafawane hamoma: beyale dawa: lumu. Na Dima gebewane baligili nodone sia: nanumu. Dia gaga: su hou amo na dawa: mu gogolesa.
Koma ine ndidzakhala ndi chiyembekezo mwa Inu nthawi zonse, ndidzakutamandani mowirikizawirikiza.
15 Na da Dia noga: idafa hou amo eno dunuma sisia: i lamu. Be hahabe asili daeya huluane, na da Dia gaga: su amo sisia: i lamu.
Pakamwa panga padzafotokoza za chilungamo chanu, za chipulumutso chanu tsiku lonse, ngakhale sindikudziwa muyeso wake.
16 Ouligisudafa Hina Gode! Na da Dia gasa bagade hou amoma nodonanumu. Di fawane da noga: idafa. Dia noga: idafa hou amo na da sisia: i lamu.
Ndidzabwera ndi kulengeza za machitidwe amphamvu zanu Inu Ambuye Wamphamvuzonse. Ndidzalengeza chilungamo chanu, chanu chokha.
17 Dia da na goihadini esoganini nama Dia hou olelesu. Amola na da mae fisili, Dia ida: iwane hamosu hou sisia: i lala.
Kuyambira ubwana wanga, Inu Mulungu mwakhala mukundiphunzitsa, ndipo mpaka lero ine ndikulengeza za ntchito zanu zodabwitsa
18 Wali na da da: i hamone, na dialuma da gago aligi gala. Be Gode! Dia na mae fisiagama! Na da Dia gasa bagade hou fifi asi gala manebe dunu ilima sisia: i lasea, Di da ani galoma: ma.
Ngakhale pamene ndakalamba ndipo imvi zili mbuu musanditaye Inu Mulungu, mpaka nditalengeza mphamvu zanu kwa mibado yonse yakutsogolo.
19 Gode! Dia moloidafa hou heda: le muagado doaga: sa. Di da liligi bagadedafa hahamoiba: le, dunu afae da Di agoai hame gala.
Mphamvu zanu ndi kulungama kwanu zimafika mpaka kumwambamwamba. Ndani wofanana nanu Inu Mulungu, amene mwachita zazikulu?
20 Di da nama bidi hamosu amola se nabasu amo huluane nama iasi dagoi. Be Di da na gasa bu nama imunu. Di da na bogoi uli dogoi amo gudu mae sa: ima: ne gaga: mu.
Ngakhale mwandionetsa mavuto ambiri owawa, mudzabwezeretsanso moyo wanga; kuchokera kunsi kwa dziko lapansi, mudzandiukitsanso.
21 Di da na bu baligili bagadedafa hahamonesimu, amola Di da na bu hahawane hahamonesimu.
Inu mudzachulukitsa ulemu wanga ndi kunditonthozanso.
22 Na da dafawane Dima sani baidama dusa nodone sia: mu. Bai Di da Isala: ili Hadigi Godedafa! Na: Gode! Na da Dia mae fisili dafawane noga: i hou amoma nodone sia: mu.
Ndidzakutamandani ndi zeze chifukwa cha kukhulupirika kwanu Mulungu, ndidzayimba matamando kwa Inu ndi pangwe, Inu Woyera wa Israeli.
23 Na sani baidama dusia, na da hahawane wele sia: mu. Na da na da: i huluane amoga gesami hea: mu. Bai Dia da na gaga: i dagoi!
Milomo yanga idzafuwula ndi chimwemwe pamene ndidzayimba matamando kwa Inu amene mwandiwombola.
24 Hahabe asili daeya huluane, na da Dia moloidafa hou sisia: i lamu. Bai dunu ilia da nama se imunusa: dawa: i, ilia da hasalasali amola gogosia: i dagoi ba: sa.
Lilime langa lidzafotokoza za ntchito zanu zachilungamo tsiku lonse, pakuti iwo amene amafuna kundipweteka achititsidwa manyazi ndi kusokonezedwa.

< Gesami Hea:su 71 >