< Gesami Hea:su 65 >
1 Gode! Ninia da Saione Moilai Bai Bagade amo ganodini Dima nodone sia: mu amola Dima ilegele sia: i liligi dafawane hamomu da defea.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Nyimbo. Matamando akudikira Inu Mulungu mu Ziyoni; kwa inu malumbiro athu adzakwaniritsidwa.
2 Bai Di da ninia sia: ne gadosu amoma dabe adole iaha. Dunu fifi asi huluane da ilia wadela: i hou dawa: beba: le, Dima sisane fofada: musa: misunu. Ninia giadofasu da nini hasalasa. Be Di da ninima gogolema: ne olofosu iaha.
Inu amene mumamva pemphero, kwa inu anthu onse adzafika.
Pamene tinathedwa nzeru ndi machimo, Inu munakhululukira mphulupulu zathu.
4 Nowa dunu amo Dia ilegele lale, Dia Hadigi Sogebi amo ganodini esaloma: ne oule maha, amo dunu da hahawane bagade gala. Ninia da Dia sema Debolo Diasu hahawane dogolegele liligi lai dagoiba: le, denesi ba: mu.
Odala iwo amene inu muwasankha ndi kuwabweretsa pafupi kukhala mʼmabwalo anu! Ife tadzazidwa ndi zinthu zabwino za mʼNyumba mwanu, za mʼNyumba yanu yoyera.
5 Di da ninia sia: ne gadosu amoma dabe adole iasisia, ninia da ninima ha lai dunu ilima hasalasa. Amola Di da ninima gaga: ma: ne, hou noga: idafa hamosa. Dunu osobo bagadega fifi asi gala dialebe amola hano wayabo bagade la: idi fifi asi dialebe, huluane da Dima dafawaneyale dawa: sa
Mumatiyankha ife ndi ntchito zodabwitsa zachilungamo, Inu Mulungu Mpulumutsi wathu, chiyembekezo cha mathero onse a dziko lapansi ndi cha nyanja zomwe zili kutali kwambiri,
6 Di da Dia gasa bagade hou amo olema: ne, Di goumi alelaloi amo ilia sogebi amogai bugisisu.
amene munapanga mapiri ndi mphamvu zanu, mutadziveka nokha ndi mphamvu.
7 Di da hano wayabo bagade ea gobe amola hano gafulubi bagade amo ouiya: lesisa. Amola fifi asi gala dunu ilia gugulubi amo ouiya: lesisa.
Amene munakhalitsa bata nyanja kukokoma kwa mafunde ake, ndi phokoso la anthu a mitundu ina.
8 Osobo bagade fifi asi gala huluanedafa da Dia hahamoi liligi ba: beba: le, fofogadigili aligisa. Osobo bagade fifi asi gala huluane, la: idi bega: asili la: idi bega: , da Dia hahamoi amo ba: le, nodone wele sia: sa.
Iwo amene akukhala kutali amaopa zizindikiro zozizwitsa zanu; kumene dzuwa limatulukira ndi kumene dzuwa limalowera. Inu mumafuna nyimbo zachimwemwe.
9 Di da osobo bagade soge amoma gagagulasu hou olelema: ne, gibu iaha. Di da soge noga: le nasegagima: ne hamosa. Di da hano logo amo hanoga nabalesisa. Di da osobo amo hulu ha: i nasu bugili iasisa.
Inu mumasamalira dziko lapansi ndi kulithirira; Inuyo mumalilemeretsa kwambiri. Mtsinje wa Mulungu ndi wodzaza ndi madzi kuti upereke tirigu kwa anthu, pakuti Inu munakhazikitsa zimenezi.
10 Di da agoane hamosa. Di da gibu bagadedafa amo osobo gidinaiga soga: sisa. Amola ilia da nanegai dagoi ba: sa. Di da osobo dasama: ne, sasafi gilisisa. Amasea, ha: i manu waha heda: be, amo noga: le heda: sa.
Mwadzaza nthaka yake ndi madzi ndi kusalaza migula yake, mwayifewetsa ndi mvula yamawawa ndi kudalitsa mbewu zake.
11 Dia hou noga: idafa da gamisu bagadedafa ninima iaha. Di da habi ahoasea, amogai da ha: i manu osea: idafa ba: mu.
Inu mumaveka chaka ndi zinthu zochuluka, ndipo ngolo zanu zimasefukira ndi zinthu zochuluka.
12 Ohe fofole nasu soge huluane da ohe wa: i amoga nabai gala. Agolo la: idi soge amoga hahawane hou da nabai.
Malo a udzu a mʼchipululu amasefukira; mapiri avekedwa ndi chisangalalo.
13 Ohe fofole nasu soge da sibi amoga dedeboi dagoi. Fago da widi sagaiga nabai. Liligi huluanedafa da hahawaneba: le, ha: gi wele sia: sa amola gesami hea: lala.
Madambo akutidwa ndi zoweta ndi zigwa zavekedwa ndi tirigu; izo pamodzi zikufuwula ndi kuyimba mwachimwemwe.