< Gesami Hea:su 56 >

1 Gode! Nama asigiba: le, fidima! Bai nama ha lai dunu da nama doagala: sa. Ilia da eso huluane, nama se iaha.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Njiwa pa Mtengo wa Thundu wa Kutali.” Mikitamu ya Davide, pamene Afilisti anamugwira ku Gati. Mundichitire chifundo Inu Mulungu, pakuti anthu akundithamangitsa kwambiri; tsiku lonse akundithira nkhondo.
2 Hahabe asili daeya mae fisili, ilia da nama doagala: sa. Nama gegebe dunu da bagohamedafa.
Ondinyoza akundithamangitsa tsiku lonse, ambiri akumenyana nane monyada.
3 Hina Gode Bagadedafa! Na da beda: i galea, na da Dima dafawaneyale dawa: mu.
Ndikachita mantha ndimadalira Inu.
4 Na da Godema dafawaneyale dawa: beba: le, hame beda: sa. Na da Ea hamomusa: ilegei amo ba: beba: le, Ema nodosa. Be osobo bagade dunu da na wadela: lesimu hame dawa:
Mwa Mulungu, amene mawu ake ine ndimatamanda, mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha. Kodi munthu amene amafa angandichite chiyani?
5 Nama ha lai dunu da hahabe asili daeya amo na se nabima: ne, bidi hamosu hamonana. Ilia da esoha huluane mae fisili, na se nabima: ne ilegelala.
Tsiku lonse amatembenuza mawu anga; nthawi zonse amakonza zondivulaza.
6 Ilia da wamoaligisu sogebi amo ganodini gilisili, na hamobe huluane ba: lala. Ilia da na medole legemu hanai.
Iwo amakambirana, amandibisalira, amayangʼanitsitsa mayendedwe anga ndipo amakhala ndi chidwi chofuna kuchotsa moyo wanga.
7 Gode! Ilia wadela: i hou hamobeba: le, ilima se dabe ima. Dia amo dunuma ougili hasalima.
Musalole konse kuti athawe; mu mkwiyo wanu Mulungu mugwetse mitundu ya anthu.
8 Na se nabasu huluane, amo Di dawa: Di da na disa si hano amo idili dedena sa: i diala. Amo da Dia buga ganodini dedei diala.
Mulembe za kulira kwanga, mulembe chiwerengero cha misozi yanga mʼbuku lanu. Kodi zimenezi sizinalembedwe mʼbuku lanulo?
9 Esoha amoga na da Dima wele sia: sea, nama ha lai dunu da sinidigili, sefasi dagoi ba: mu. Amo na dawa: Bai Gode da namagai gala.
Adani anga adzabwerera mʼmbuyo pamene ndidzalirira kwa Inu. Pamenepo ndidzadziwa kuti Mulungu ali ku mbali yanga.
10 E da Hina Godedafa amola na da Ea sia: i ilegei amoma nodosa.
Mwa Mulungu amene mawu ake ndimawatamanda, mwa Yehova amene mawu ake ndimawatamanda,
11 Na da Ema dafawaneyale dawa: sa. Amaiba: le, na da hame beda: mu! Amola osobo bagade dunu da na wadela: lesimu hamedeidafa.
mwa Mulungu ine ndimadalira ndipo sindidzachita mantha. Kodi munthu angandichite chiyani?
12 Gode! Na da Dima imunusa: ilegei liligi amo Dima dafawane imunu. Na da Dia nodoma: ne gobele salasu amo Dima imunu.
Ndiyenera kuchita zomwe ndinalumbira kwa Mulungu; ndidzapereka nsembe zanga zachiyamiko kwa inu.
13 Bai Dia da na mae bogoma: ne, na gaga: i dagoi. Amola nama ha lai ilia na mae hasalima: ne hamoi. Amaiba: le na da Gode Ea midadi, hadigi amo da esalebe dunuma diga: be, amo ganodini lala.
Pakuti mwawombola moyo wanga ku imfa ndi mapazi anga kuti ndingagwe, kuti ndiyende pamaso pa Mulungu mʼkuwala kwa moyo.

< Gesami Hea:su 56 >