< Gesami Hea:su 52 >

1 Gasa fi dunu! Abuliba: le di da dia wadela: i houba: le hidasala: ? Gode Ea asigidafa hou da eso huluane dialalalumu.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe, ndakatulo ya Davide; pamene Doegi Mwedomu anapita kwa Sauli ndi kunena kuti “Davide wapita ku nyumba ya Ahimeleki.” Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira ndi zoyipa, iwe munthu wamphamvu? Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira tsiku lonse, iwe munthu wochititsa manyazi pamaso pa Mulungu?
2 Di da eno dunu wadela: lesimusa: ilegesa. Dia gona: su da gobimedai mei agoai gala. Di da mae fisili, eso huluane ogogosu sia: hahamonesilala.
Tsiku lonse umakhalira kuganizira za kuwononga ena; lilime lako lili ngati lumo lakuthwa, ntchito yako nʼkunyenga.
3 Di da wadela: i hou hanane, hou noga: i amo higasa. Di da ogogosu hanane, dafawane sia: amo higasa.
Iwe umakonda choyipa mʼmalo mwa kuyankhula choonadi. Umakonda kunama kupambana kuyankhula zoona. (Sela)
4 Di da ogogosu dunu! Di da dia sia: ga eno dunu se nabima: ne hanasa.
Umakonda mawu onse opweteka, iwe lilime lachinyengo!
5 Amaiba: le Gode da di eso huluane amane dialoma: ne wadela: lesimu. E da di gaguli, dia diasu amoga di mae esaloma: ne di fadegale fasimu. E da di medole legemu.
Zoonadi Mulungu adzakutsitsa kupita ku chiwonongeko chamuyaya: iye adzakukwatula ndi kukuchotsa mʼtenti yako; iye adzakuzula kuchoka mʼdziko la amoyo.
6 Moloidafa dunu da amo hou ba: beba: le, beda: mu. Amasea, ilia da dima oufesega: ne, amane sia: mu,
Olungama adzaona zimenezi ndi kuchita mantha; adzamuseka nʼkumanena kuti,
7 “Ba: ma! Amo dunu da Godema gaga: su lama: ne hame asi. Be e da ea bagade gagui hou amola ea wadela: i hou amoga e gaga: ma: beyale dawa: i.
“Pano tsopano pali munthu amene sanayese Mulungu linga lake, koma anakhulupirira chuma chake chambiri nalimbika kuchita zoyipa!”
8 Be na da olife ifa Gode Ea diasu ganodini heda: lebe, agoane ba: sa. Na da Ea maedafa fisili asigidafa hou amo dafawaneyale dawa: lala.
Koma ine ndili ngati mtengo wa olivi wobiriwira bwino mʼnyumba ya Mulungu; ndimadalira chikondi chosatha cha Mulungu kwa nthawi za nthawi.
9 Gode! Na da eso huluane Dia nama hamobe amoba: le Dima nodone sia: nana. Amola Dia fi dunu ilia si da: iya, Dia noga: idafa hou amo olelelalumu.
Ine ndidzakutamandani kwamuyaya chifukwa cha zimene mwachita; chifukwa cha zimene mwachita; mʼdzina lanu ndidzayembekezera pakuti dzina lanulo ndi labwino. Ndidzakutamandani pamaso pa oyera mtima anu.

< Gesami Hea:su 52 >