< Gesami Hea:su 51 >

1 Gode! Nama asigima! Bai Di da mae fisili asigidafa hou amola gogolema: ne olofosu hou dawa: Amaiba: le, na wadela: i hou huluane doga: le fasima.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pamene Mneneri Natani anabwera kwa iye atachita chigololo ndi Batiseba. Mundichitire chifundo, Inu Mulungu, molingana ndi chikondi chanu chosasinthika; molingana ndi chifundo chanu chachikulu mufafanize mphulupulu zanga.
2 Na da bu foloai ba: ma: ne, na wadela: i ledo hou amo dodofele fasima.
Munditsuke zolakwa zanga zonse ndipo mundiyeretse kuchotsa tchimo langa.
3 Na da ni giadofale hamosu amo ea bai amo ni ba: le, dawa: digisa. Na da eso huluane wadela: i hou na hamoi, amo dawa: digisa.
Pakuti ndikudziwa mphulupulu zanga, ndipo tchimo langa lili pamaso panga nthawi zonse.
4 Na da enoma hame wadela: le hamoi, be Dima fawane wadela: le hamoi. Amola Dia higa: i ba: su, amo na da giadofale hamoi. Amaiba: le Dia nama fofada: mu da defea, amola Di da moloidafaba: le nama fofada: ne, diwaneya udidili, nama se dabe imunu da defea.
Motsutsana ndi Inu, Inu nokha, ndachimwa ndipo ndachita zoyipa pamaso panu, Kotero kuti inu mwapezeka kuti ndinu wolungama pamene muyankhula ndi pamene muweruza.
5 Na da na lalelegei esoha amogaini wadela: i hou hahamona misi. Na da na: me ea hagomoga mano hahamoia amoganini wali, wadela: i hou hahamona misi.
Zoonadi ine ndinali wochimwa pomwe ndimabadwa, wochimwa kuyambira pa nthawi imene amayi anga anakhala woyembekezera ine.
6 Dia da moloidafa amola dafawanedafa hou amo ilegesa. Amaiba: le Dia na asigi dawa: su amo Dia bagade dawa: su amoga nabalesima.
Zoonadi inu mumafuna choonadi mu ziwalo zamʼkati mwanga; mumandiphunzitsa nzeru mʼkati mwanga mwenimweni.
7 Na wadela: i hou hamoi amo Dia doga: le fasima. Amasea na wadela: i hou da doga: iba: le, na da foloai dagoi ba: mu. Na wadela: i hou dodofelesima. Amasea na da foloaidafa mu gohona: amo baligi ba: ma: ma.
Mundiyeretse ndi hisope ndipo ndidzayera, munditsuke ndipo ndidzayera kuposa matalala
8 Na da hahawane nodosu sia: amo nabima: ma, be amomane Di da na dadalega: le amola dadamunisali galu. Be na da bu hahawane hamoi ba: mu.
Mundilole ndimve chimwemwe ndi chisangalalo, mulole kuti mafupa amene mwawamphwanya akondwere.
9 Di da na wadela: i hou hamoi amoga si sisigili mae ba: ma! Amola na wadela: i hou hamoi huluane doga: le fasima!
Mufulatire machimo anga ndi kufafaniza zolakwa zanga zonse.
10 Gode! Nama dogo gaheabolo hahamonesili, na da: i hodo ganodini salima! Amola a: silibu gaheabolo amola Dima fa: no bobogesu fisisu hame dawa: a:silibu, amo na da: i hodo ganodini salima.
Mulenge mʼkati mwanga mtima woyera Inu Mulungu ndi kukonzanso mzimu wokhazikika mwa ine.
11 Dia midadi amoga na mae fisiagama! Dia A: silibu Ida: iwane Gala nama mae fadegale fasima!
Musandichotse pamaso panu kapena kuchotsa Mzimu wanu Woyera mwa ine.
12 Di da dunu gaga: sea, ilia da hahawane bagade ba: sa. Amo hahawane hou nama bu ima. Na da Dima bu nabawane fa: no bobogema: ne, Dia hahamonesima!
Bwezeretsani mwa ine chimwemwe cha chipulumutso chanu ndipo mundipatse mzimu wofuna kumvera kuti undilimbitse.
13 Amasea, na da wadela: i hamosu dunu ilima Dia hamoma: ne sia: i olelemu. Amola ilia da amo nababeba: le, Dima bu sinidigimu.
Pamenepo ndidzaphunzitsa anthu amphulupulu njira zanu kuti ochimwa adzabwerere kwa inu.
14 Gode! Na esalusu gaga: ma! Amasea na da nonodoia Dia moloidafa hou enoma sisia: i lamu.
Mundipulumutse ku tchimo lokhetsa magazi, Inu Mulungu, Mulungu wa chipulumutso changa, ndipo lilime langa lidzayimba zachilungamo chanu.
15 Hina Gode! Na sia: sia: ma: ne fidima! Amasea, Na da Dima nodone sia: mu.
Inu Ambuye tsekulani milomo yanga, ndipo pakamwa panga padzalengeza matamando anu.
16 Di da gobele salasu lamu hame hanai. Di da amo lamu hanai ganiaba, na da amo Dima ia: noba. Di da gobei gobele salasu amoma hame nodosa.
Inu simusangalatsidwa ndi nsembe wamba. Ndikanapereka nsembe yopsereza, Inu simukondwera nayo.
17 Gode! Na Dima gobele salasu da asaboi a: silibu fawane. Na dawa: ! Di da asabole amola Dima sinidigimusa: dawa: su dunu amo hame higamu.
Nsembe za Mulungu ndi mzimu wosweka; mtima wosweka ndi wachisoni Inu Mulungu simudzawunyoza.
18 Gode! Saione Moilai Bai bagade amoma asigima! E fidima! Yelusaleme ea dobea fei amo bu gaguma!
Mwa kukoma mtima kwanu mupange Ziyoni kuti alemere; mumange makoma a Yerusalemu.
19 Amasea, Di da gobele salasudafa amola ninia gobei gobele salasu amo nodone ba: mu. Amola bulamagau gawali da Dia oloda da: iya gobele salabe ba: mu.
Kotero kudzakhala nsembe zachilungamo, nsembe yonse yopsereza yokondweretsa Inu; ndipo ngʼombe zazimuna zidzaperekedwa pa guwa lanu la nsembe.

< Gesami Hea:su 51 >