< Gesami Hea:su 50 >

1 Hina Gode Bagadedafa da sia: sa. E da osobo bagade fifi asi gala huluanedafa, gusudili asili guma: dini, ilima wele sia: sa.
Salimo la Asafu. Wamphamvuyo, Yehova Mulungu, akuyankhula ndi kuyitanitsa dziko lapansi kuyambira kotulukira dzuwa mpaka kumene limalowera.
2 Saione Moilai Bai Bagade da isisima: goi ida: iwanedafa. Amoganini, Gode Ea hadigi da diga: sa.
Kuchokera ku Ziyoni, mokongola kwambiri Mulungu akuwala.
3 Ninia Gode da manebe. Be E da ouiya: lewane hame maha. Gegemoi lalu da E bisili ahoa. Amola mulu bagade da E sisiga: le disisa.
Mulungu wathu akubwera ndipo sadzakhala chete; moto ukunyeketsa patsogolo pake, ndipo pomuzungulira pali mphepo yamkuntho
4 E da Ea fi dunuma fofada: musa: , mu amola osobo bagade ba: su hou hamoma: ne elama ilegele wele sia: sa.
Iye akuyitanitsa zamumlengalenga ndi za pa dziko lapansi kuti aweruze anthu ake.
5 E da amane sia: sa, “Na mae fisili fa: no bobogesu dunu, ilia da Nama gobele salawane gousa: su hamoi, amo huluane Nama gegedole oule misa!”
Mundisonkhanitsire okhulupirika anga, amene anachita pangano ndi ine pochita nsembe.
6 Mu da amane sisia: laha, “Gode da moloidafa amola Hisu da fofada: su dunudafa!”
Ndipo mayiko akumwamba akulengeza chilungamo chake, pakuti Mulungu mwini ndi woweruza.
7 Hina Gode da amane sia: sa, “Na fi dunu! Nabima! Na da sia: mu! Na da dilia, Isala: ili dunu dilima diwaneya udidimu. Na da Gode! Na da dilia Gode!
Imvani inu anthu anga, ndipo Ine ndidzayankhula, iwe Israeli, ndipo Ine ndidzayankhula mokutsutsa; ndine Mulungu, Mulungu wako.
8 Dilia da mae fisili gobei gobele salasu Nama gaguli maha. Amoga, Na da dilima hame gagabole sia: sa.
Sindikudzudzula chifukwa cha nsembe zako, kapena nsembe zako zopsereza zimene zili pamaso panga nthawi zonse.
9 Be bulamagau gawali dilia afugi amoga lai amola goudi dilia goudi fofoi wa: i amoga lai, amo Na da hame hanasa.
Ine sindikufuna ngʼombe yayimuna kuchokera mʼkhola lako kapena mbuzi za mʼkhola lako,
10 Bai ohe huluane iwilaga esala da Na: fawane. Amola bulamagau agolo osea: idafa amoga esala da Na: fawane.
pakuti nyama iliyonse yakunkhalango ndi yanga ndiponso ngʼombe za ku mapiri ochuluka.
11 Sigua sio huluanedafa da Na: fawane. Amola liligi huluane amo da moifufu sogega esalebe, da Na: fawane.
Ine ndimadziwa mbalame iliyonse mʼmapiri ndiponso zolengedwa zonse zakutchire ndi zanga.
12 Na da ha: i ganiaba, Na da dilima hame adola: loba. Bai osobo bagade amola liligi huluane amo ganodini gala da Na: fawane.
Ndikanakhala ndi njala sindikanakuwuzani, pakuti dziko lonse ndi zonse zimene zili mʼmenemo ndi zanga.
13 Na da bulamagau gawali ilia hu nabela: ? Na da goudi ilia maga: me nabela: ? Hame naha!
Kodi ndimadya nyama ya ngʼombe zazimuna kapena kumwa magazi a mbuzi?
14 Be dilia Godema gobele salasu hou dafawanedafa da Ema nodone sia: su. Amola Hina Bagadedafa Ema dilia imunu ilegei amo huluane defele Ema ima.
“Pereka nsembe zachiyamiko kwa Mulungu, kwaniritsa malonjezo ako kwa Wammwambamwamba.
15 Bidi hamosu da dilima doaga: sea, Nama fidima: ne wele sia: ma! Amasea, Na da dili gaga: mu. Amola dilia da Nama nodomu.”
Ndipo undiyitane pa tsiku lako la masautso; Ine ndidzakulanditsa, ndipo udzandilemekeza.”
16 Be Gode da wadela: i hamosu dunu ilima amane sia: sa, “Dilia da abuliba: le Na hamoma: ne sia: i amo sia: daha? Dilia da abuliba: le Na gousa: su hamoi, amoga fada: i sia: dahabela: ?
Koma kwa woyipa, Mulungu akuti, “Kodi uli ndi mphamvu yanji kuti uzinena malamulo anga kapena kutenga pangano langa pa milomo yako?
17 Na gagabole sia: amo dilia higasa. Amola Na hamoma: ne sia: i higale, nabawane hame hamosa.
Iwe umadana ndi malangizo anga ndipo umaponyera kumbuyo kwako mawu anga.
18 Dilia da nowa wamolasu dunu ba: sea, amo dilia dogolegei sama agoane hamosa. Amola dilia da inia uda adole lasu dunu ilima gilisisa.
Ukaona wakuba umamutsatira, umachita maere ako pamodzi ndi achigololo
19 Dilia da eso huluane wadela: i hou fuligala: ma: ne sia: musa: momagele esala. Amola hedolowane ogogole sia: daha.
Umagwiritsa ntchito pakamwa pako pa zinthu zoyipa ndipo umakonza lilime lako kuchita chinyengo.
20 Dilia da diolalalidafa ilima diwaneya udidima: ne momagele esala. Amola ilia giadofai hogole, hedolowane olelesa.
Nthawi zonse umayankhula motsutsana ndi mʼbale wako ndipo umasinjirira mwana wa amayi ako enieni.
21 Amo hou huluane, dilia da hamoi dagoi. Be Na da dilima hame sia: i. Amaiba: le, dilia da Na hou da dilia hou defele dawa: i. Be wali Na da dilima gagabole sia: sa. Dilia wadela: le hamoi, amo Na da dili noga: le dawa: ma: ne, dilima olelesa.
Wachita zimenezi ndipo Ine ndinali chete; umaganiza kuti ndine wofanana nawe koma ndidzakudzudzula ndipo ndidzakutsutsa pamaso pako.
22 Dilia Nama hame dawa: digisu dunu! Na sia: nabima! Dilia da Na sia: hame nabasea, Na da dili wadela: lesimu. Amola dilia da gaga: su dunu hame ba: mu.
“Ganizira izi, iwe amene umayiwala Mulungu kuti ndingakukadzule popanda wokupulumutsa:
23 Nama gobele salasu houdafa da Nama nodone sia: ne gadosu hou, amo fawane. Amola nowa da Na sia: nabawane hamosea, Na da amo dunu dafawane gaga: mu.”
Iye amene amapereka nsembe yamayamiko amandilemekeza, ndipo amakonza njira zake kuti ndimuonetse chipulumutso cha Mulungu.”

< Gesami Hea:su 50 >