< Gesami Hea:su 48 >

1 Hina Gode da bagadedafa. Amola Ema baligiliwane nodomu da defea. Ea Moilai Bai Bagade amola Ea sema agolo amogai Ema baligiliwane nodomu da defea.
Nyimbo. Salimo la ana a Kora. Wamkulu ndi Yehova, ndi woyenera kwambiri matamando mu mzinda wa Mulungu wathu, phiri lake loyera.
2 Gode Ea Goumi amo Saione, da gadodafa amola ida: iwanedafa gala. Hina Bagadedafa Ea Moilai Bai Bagade da osobo bagade fifi asi gala dunu huluane ilima hahawane hou iaha.
Lokongola mu utali mwake, chimwemwe cha dziko lonse lapansi. Malo aatali kwambiri a Zafoni ndiye Phiri la Ziyoni, mzinda wa Mfumu yayikulu.
3 Gode da Ea gagili sali Moilai Bai Bagade amo ganodini esala. Amola nowa da amo ganodini E gilisili esalea, amo dunu da gaga: su ba: mu. Gode da amo hou olelei dagoi.
Mulungu ali mu malinga ake; Iye wadzionetsa yekha kuti ndiye malinga akewo.
4 Osobo bagade hina bagade dunu da gilisili, Saione Goumi doagala: musa: misi.
Pamene mafumu anasonkhana pamodzi, pamene anayendera pamodzi kudzalimbana nafe,
5 Be ilia da amo ba: loba, fofogadigili, bagade beda: i. Beda: iba: le, ilia hobea: i dagoi.
iwo anaona mzindawo ndipo anadabwa kwambiri; anathawa ndi mantha aakulu.
6 Uda da mano lalelegemu gadenesea se nabasu amo defele, amola dusagai bagade hano wayabo bagade ahoanoba, mulu amo ganodini gigiwigisu defele, ilia beda: i bagade amola se nabi dagoi.
Pomwepo anagwidwa nako kunjenjemera, ululu wonga wa mkazi woyembekezera pa nthawi yochira.
7
Inu munawawononga monga sitima zapamadzi za ku Tarisisi zitawonongeka ndi mphepo ya kummawa.
8 Ninia da Gode Ea hamobe amo ninia gega nabi dagoi. Amola wali ninia da ninia Hina Gode Bagadedafa Ea Moilai Bai Bagade amo ganodini Ea hamobe ninia siga ba: i dagoi. E da Ea Moilai Bai Bagade mae fisili gaga: lalumu.
Monga momwe tinamvera, kotero ife tinaona mu mzinda wa Yehova Wamphamvuzonse, mu mzinda wa Mulungu wathu. Mulungu adzawuteteza kwamuyaya.
9 Gode! Ninia da Dia Debolo Diasu ganodini Dia maedafa fisili asigidafa hou amo dawa: lala.
Mʼkati mwa Nyumba yanu Mulungu, ife timalingaliramo zachikondi chanu chosasinthika.
10 Osobo bagade fifi asi gala dunu huluanedafa da Dia hou dawa: Amola amoba: le nodosa. Bai Di da moloidafawane ouligilala.
Monga dzina lanu, Inu Mulungu, matamando anu amafika ku malekezero a dziko lapansi dzanja lanu lamanja ladzaza ndi chilungamo.
11 Saione esalebe dunu ilia da hahawane ba: mu da defea. Bai Dia da moloidafa fofada: su hamosa. Yuda moilai ganodini amo hahawane hou dialumu da defea.
Phiri la Ziyoni likukondwera, midzi ya Yuda ndi yosangalala chifukwa cha maweruzo anu.
12 Gode Ea fi dunu, dilia! Saione Moilai Bai Bagade sisiga: le ahoa gagagula heda: le gagai diasu amo idima!
Yendayendani mu Ziyoni, uzungulireni mzindawo, werengani nsanja zake.
13 Fa: no fifi mabe ilima olelemusa: , dobea fei amola gagili gagoi amo abodema. Bai dilia da fa: no fifi mabe ilima amane sia: ma: ne,
Yangʼanitsitsani bwino mipanda yake, penyetsetsani malinga ake, kuti mudzafotokoze za izo ku mʼbado wotsatira.
14 “Goe Gode da ninia Gode. E da eso huluane esalalalumu. E eso huluane mae fisili, nini bisili ouligilalumu.”
Pakuti Mulungu uyu ndi Mulungu wathu ku nthawi zosatha; Iye adzakhala mtsogoleri wathu mpaka ku mapeto.

< Gesami Hea:su 48 >