< Gesami Hea:su 42 >

1 Gode! ‘Dia’ gebo da hano anegagi manusa: hohogola ahoa amo defele Na da Di hogosa.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Ndakatulo ya ana a Kora. Monga mbawala ipuma wefuwefu kufunafuna mitsinje yamadzi, kotero moyo wanga upuma wefuwefu kufunafuna Inu Mulungu.
2 Esalusudafa Gode! Na Dima hanai da hano hanai defele gala. Na da habogala Dia midadi, Dima nodone sia: ne gadomusa: masa: bela: ?
Moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Mulungu, lofuna Mulungu wamoyo. Kodi ndipite liti kukakumana ndi Mulungu?
3 Eso haga amola gasia huluane na da disa, amola na si hano da na ha: i manu agoane gala. Eso huluane nama ha lai dunu da nama amane adole ba: sa, “Dia Gode da habila: ?”
Misozi yanga yakhala chakudya changa usana ndi usiku, pamene anthu akunena kwa ine tsiku lonse kuti, “Mulungu wako ali kuti?”
4 Na da ni musa: hamoi amo dadawa: sea, na dogo da sesa. Na da Hina Gode Ea diasu ganodini masunusa: gilisi amo ilima madelale ili da na bisili oule ahoasu, amola amo gilisisu ilia da Godema hahawane gesami hehea: la amola wele sia: sa ahoasu.
Zinthu izi ndimazikumbukira pamene ndikukhuthula moyo wanga: momwe ndinkapitira ndi gulu lalikulu, kutsogolera mayendedwe a ku Nyumba ya Mulungu ndi mfuwu yachimwemwe ndi mayamiko pakati pa anthu a pa chikondwerero.
5 Abuliba: le na da bagadewane da: i dioi ganabela: ? Abuliba: le na da na dogo ganodini bagadewane se nabawane dawa: sala: ? Na da dafawane hamoma: beyale dawa: su amo Godema fawane dawa: mu, amola na da bu enowane Ema nodone, “Na Gaga: su amola na Gode,” agoane sia: mu.
Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni, iwe moyo wanga? Nʼchifukwa chiyani wakhumudwa iwe mʼkati mwanga? Yembekezera Mulungu, pakuti ndidzamulambirabe, Mpulumutsi wanga ndi
6 Na da goeguda: mugululi misi. Amola na da na dogo ganodini bogomuwane se naba. Amaiba: le, na da na asigi dawa: su Godema bu sinidigili dawa: sa. E da nama se bagadedafa iasi. Bidi hamosu da hano heda: i defele nama gosa. Bidi hamosu da Hemone Goumi amola Misa Goumi amoga hano nawa: li mogosobe, Yodane Hano amoga gudu daha, amo defele, gugelebe agoane nama gole wesa.
Mulungu wanga. Moyo wanga uli ndi chisoni mʼkati mwanga kotero ndidzakumbukira Inu kuchokera ku dziko la Yorodani, ku mitunda ya Herimoni kuchokera ku phiri la Mizara.
7
Madzi akuya akuyitana madzi akuya mu mkokomo wa mathithi anu; mafunde anu onse obwera mwamphamvu andimiza.
8 Hina Gode da Ea mae fisili asigidafa hou amo esoga olelemu da defea. Amasea na da gasia Ema gesami hea: mu amola na esalusu ouligisu Gode, Ema sia: ne gadomu.
Koma usana Yehova amalamulira chikondi chake, nthawi ya usiku nyimbo yake ili nane; pemphero kwa Mulungu wa moyo wanga.
9 Na da na gaga: su Gode, Ema sia: sa, “Dia da abuliba: le na gogoleila: ? Nama ha lai gasa fi dunu da nama gebewane se iaha. Na da abuliba: le eso huluane se nabala: ?
Ine ndikuti kwa Mulungu Thanthwe langa, “Nʼchifukwa chiyani mwandiyiwala? Nʼchifukwa chiyani ndiyenera kuyenda ndikulira, woponderezedwa ndi mdani?”
10 Ilia da nama gebewane odagia gadele sia: beba: le, na da gala: la sa: i dagoi ba: sa. Ilia da gebewane nama amane adole ba: lala, “Dia Gode da habila: ?”
Mafupa anga ali ndi ululu wakufa nawo pamene adani anga akundinyoza, tsiku lonse akunena kuti, “Mulungu wako ali kuti?”
11 Na da abuliba: le baligili da: i diobela: ? Na da abuliba: le dogo se nabawane esalabela: ? Na Godema dafawane hamoma: beyale dawa: mu. Na da bu enowane Ema nodone sia: mu. Bai E da na Gaga: sudafa amola na Godedafa.
Bwanji ukumva chisoni, iwe mtima wanga? Chifukwa chiyani ukuvutika chonchi mʼkati mwanga? Khulupirira Mulungu, pakuti ndidzamutamandanso, Iye amene ali thandizo langa ndi Mulungu wanga.

< Gesami Hea:su 42 >