< Gesami Hea:su 4 >
1 Na sia: ne gadobe goe bu sia: ne ima. Hina Gode, Di da na gaga: su dunu. Na se nabaloba, Dia na fidi. Wali, Di da nama asigima amola na sia: ne gadobe nabima.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe wa zida za zingwe. Salimo la Davide. Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu, Inu Mulungu wa chilungamo changa. Pumulitseni ku zowawa zanga; chitireni chifundo ndi kumva pemphero langa.
2 Eso habowali dilia fi dunu da nama higama: bela: ? Eso habowali dilia da hamedei liligi amo hanama: bela: , amola ogogosu liligi amoma fa: no bobogema: bela: ?
Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi? Mpaka liti mudzakonda zachabe ndi kufuna milungu yabodza? (Sela)
3 Dawa: ma! Hina Gode da moloidafa noga: i dunu amo Ea fidafa hamomusa: ilegei dagoi. Amola na da Ema wele sia: sea, E da na wele sia: su naba.
Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika; Yehova adzamva pamene ndidzamuyitana.
4 Dilia beda: ga yaguguma! Amola wadela: le hamosu hou fisima. Dilia da ouiya: le agoane dilia debea da: iya dialea, bagade dadawa: laloma.
Kwiyani koma musachimwe; pamene muli pa mabedi anu, santhulani mitima yanu ndi kukhala chete. (Sela)
5 Gobele salasu moloidafa amo Hina Godema ima, amola Ema dafawaneyale dawa: ma.
Perekani nsembe zolungama ndipo dalirani Yehova.
6 Dunu bagohame da agoane sia: ne gadosa, “Hina Gode! Ninima Dia hahawane fidisu hou baligili ima. Ninima asigiwane ba: ma.”
Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?” Kuwunika kwa nkhope yanu kutiwalire, Inu Yehova.
7 Ilia da gagoma amola waini lai dagoiba: le hahawane ba: sa. Be hahawane hou Di da nama i dagoi, amo da amo osobo bagade hou bagadewane baligisa.
Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu kuposa kuchuluka kwa tirigu wawo ndi vinyo watsopano.
8 Na diasa: ili gasia golai dialoba, hahawane golasa. Hina Gode! Di fawane da na noga: le gaga: sa.
Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere, pakuti Inu nokha, Inu Yehova, mumandisamalira bwino.