< Gesami Hea:su 39 >

1 Na da amane sia: i, “Na da dawa: iwane hamomu. Na da na gona: su amoga mae wadela: le hamoma: mu. Wadela: i hamosu dunu da na gadenene aligisia, na da sia: hamedafa sia: mu.”
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Kwa Yedutuni. Salimo la Davide. Ndinati, “Ndidzasamalira njira zanga ndipo ndidzasunga lilime langa kuti ndisachimwe; ndidzatseka pakamwa panga ndi chitsekerero nthawi yonse imene woyipa ali pamaso panga.”
2 Na da ouiya: le esalu. Noga: i hou amolawane, na da hamedafa sia: i. Be na da bu baligiliwane se nabi.
Koma pamene ndinali chete osanena ngakhale kanthu kalikonse kabwino mavuto anga anachulukirabe.
3 Amalalu, beda: su hou da na hasali dagoi. Na da bu dawa: lalu amola bu baligili beda: i galu. Na da adole ba: su ouiya: mu da hamedei. Na da Hina Godema amane adole ba: i,
Mtima wanga unatentha mʼkati mwanga, ndipo pamene ndinkalingalira, moto unayaka; kenaka ndinayankhula ndi lilime langa:
4 “Hina Gode! Na da habowali seda esaloma: bela: ? Na da habogala bogoma: bela: ? Nama adoma! Na esalusu da habogala dagoma: bela: ?”
“Yehova ndionetseni mathero a moyo wanga ndi chiwerengero cha masiku anga; mundidziwitse kuti moyo wanga ndi wosakhalitsa motani.
5 Di da nama esalusu dunumuni fawane i dagoi. Na esalusu da Dia siga hamedei agoane ba: sa. Dafawane! Esalebe dunu huluane afae afae ea esalusu da foga afae fulabole fasibi defele gala.
Inu mwachititsa kuti masiku anga akhale ochepa kwambiri, kutalika kwa zaka zanga ndi kopanda phindu pamaso panu; moyo wa munthu aliyense ndi waufupi. (Sela)
6 Ea esalusu da baba ba: be defele amola seda hame gala. Ea hamobe huluane da udigili fawane hamosa. E da muni amola liligi gagadosa. Be amo fa: no lamu dunu e da hame dawa:
Munthu ali ngati chithunzithunzi chake pamene akuyenda uku ndi uku: Iye amangovutika koma popanda phindu; amadzikundikira chuma, osadziwa kuti chidzakhala chayani.
7 Hina Gode! Amai galea, na da adi dafawane hamoma: beyale dawa: ma: bela: ? Na dafawane hamoma: beyale dawa: su da Dima dawa: lumu.
“Koma tsopano Ambuye kodi ndifunanso chiyani? Chiyembekezo changa chili mwa Inu.
8 Na wadela: i hou hamoi huluane, amoga Dia na gaga: ma. Amola gagaoui dunu ilia naba: le mae oufesega: ma: ma.
Pulumutseni ku zolakwa zanga zonse; musandisandutse chonyozeka kwa opusa.
9 Na da ouiya: i dialumu, na da sia: afae hame sia: mu. Bai na agoane se nabima: ne, Difawane agoane hahamonesi.
Ine ndinali chete; sindinatsekule pakamwa panga pakuti Inu ndinu amene mwachita zimenezi.
10 Di da nama dawa: ma: ne olelesu se iasu bu mae ima! Na da Dia fane sali amoga bogomu agoai galebe.
Chotsani mkwapulo wanu pa ine; ndagonjetsedwa ndi nkhonya ya dzanja lanu.
11 Dunu ilia da wadela: i hou galea fawane, Di da ilima se bidi iaha. Amola Di da aowaba agoane, ilia liligi amoga ilia da asigi amo wadela: lesisa. Dafawane! Osobo bagade dunu da foga afae fulabolesibi amo defele gala.
Inu mumadzudzula ndi kulanga anthu chifukwa cha tchimo lawo; mumawononga chuma chawo monga njenjete; munthu aliyense ali ngati mpweya. (Sela)
12 Hina Gode! Na Dima sia: ne gadobe nabima! amola na Dima dini iabe nabima! Na da dinanea, nama fidila misa! Na da na aowalali defele, wahamusu dima sofe misi esala.
“Imvani pemphero langa Inu Yehova, mverani kulira kwanga kopempha thandizo; musakhale chete pamene ndikulirira kwa Inu, popeza ndine mlendo wanu wosakhalitsa; monga anachitira makolo anga onse.
13 Na da hedolowane asili, bu hame ba: muba: le, Dia na fonobahadi hahawane hamoma: ne, na yolesima.
Musandiyangʼane mwaukali, choncho ndidzatha kusangalala ndisanafe ndi kuyiwalika.”

< Gesami Hea:su 39 >