< Gesami Hea:su 38 >

1 Hina Gode! Dia ougiba: le, nama se bidi mae ima!
Salimo la Davide. Kupempha. Yehova musandidzudzule mutapsa mtima kapena kundilanga muli ndi ukali.
2 Di da na Dia dadi amoga fa: ginisi, amola na fane sanasi.
Pakuti mivi yanu yandilasa, ndipo dzanja lanu latsika ndipo landifikira.
3 Dia da nama ougiba: le, na se baligili nabala. Na wadela: i hou hamobeba: le, na da: i huluane da olo bagade madelasa.
Chifukwa cha ukali wanu mulibe thanzi mʼthupi langa; mafupa anga alibe mphamvu chifukwa cha tchimo langa.
4 Na da nina: wadela: i hamonana fedege agoane hano heda: i amoga gela daha. Na wadela: i hou da fedege agoane, liligi bagadedafa aguni masunu hamedei agoai ba: sa.
Kulakwa kwanga kwandipsinja ngati katundu wolemera kwambiri kuposa mphamvu zanga.
5 Bai na da gagaoule hamobeba: le, na aiya da dasale gahasa.
Mabala anga akuwola ndipo akununkha chifukwa cha uchitsiru wa moyo wanga wauchimo.
6 Na da se nabawane beguduli, gala: la sa: i. Na da hahabe asili daeya, mae fisili, dinana.
Ine ndapindika msana ndipo ndawerama kwambiri; tsiku lonse ndimangolira.
7 Na da asugiba: le, da: i goaeasa. Amola na da bogomu gadenei ba: sa.
Msana wanga wagwidwa ndi ululu wosasimbika, mulibe thanzi mʼthupi langa.
8 Na da gasa hamedene, dafawane gala: la sa: i. Na da da: i dioi, amola se nababeba: le gayasa.
Ndilibe mphamvu ndipo ndakunthidwa kwathunthu; ndikubuwula ndi ululu wa mumtima.
9 Hina Gode! Na hanai amo Dia dawa: ! Na gayabe huluane Dia naba!
Zokhumba zanga zonse zili poonekera pamaso panu Ambuye, kusisima kwanga sikunabisike kwa Inu.
10 Na habe da ha: ha: sa, amola na gasa da asi dagoi. Na si da mobi sa: i dagoi.
Mtima wanga ukugunda, mphamvu zanga zikutha; ngakhale kuwala kwachoka mʼmaso mwanga.
11 Na da aiya bagohame madelaiba: le, na sama amola na na: iyado fi dunu ilia da nama hame gadenena maha. Na sosogodafa amolalia na hagasa.
Abwenzi anga ndi anzanga akundipewa chifukwa cha mabala anga; anansi anga akhala kutali nane.
12 Dunu da na medole legemusa: dawa: be, ilia da na sa: ima: ne sanenisa. Amola dunu da nama se ima: ne dawa: be, ilia da na wadela: lesimusa: magagisa. Ilia da na wadela: lesimusa: sia: fane ilegesu hou hame yolesisa.
Iwo amene akufunafuna moyo wanga atchera misampha yawo, oti andipwetekewo amayankhula za kuwonongeka kwanga; tsiku lonse amakonza zachinyengo.
13 Na da ge ga: i dunu defele, hame naba. Amola na da sia: hamedei dunu agoane, hame sia: da.
Ine ndili ngati munthu wosamva amene sangamve, monga wosayankhula, amene sangathe kutsekula pakamwa pake;
14 Na da ge ga: iba: le, dabe adole imunu hamedei dunu agoai gala.
Ndakhala ngati munthu amene samva, amene pakamwa pake sipangathe kuyankha.
15 Hina Gode, na da dima dafawaneyale dawa: sa, amola Di da na Hina Godeba: le, nama dabe adole imunu.
Ndikudikira Inu Yehova; mudzayankha, Inu Ambuye Mulungu wanga.
16 Na da se nabasu baligilidafa nababeba: le, nama ha lai dunu da na mae habosesema: ma. Ilia da na dafai hou ba: beba: le, Dia mae habosesele sia: ma: ma!
Pakuti Ine ndinati, “Musawalole kuti akondwere kapena kudzikweza okha pa ine pamene phazi langa laterereka.”
17 Na da maedafa fisili, se naba. Amola na da dafamu gadenei ba: sa.
Pakuti ndili pafupi kugwa, ndipo ndikumva kuwawa nthawi zonse.
18 Na da na wadela: i hou sisane fofada: sa. Be na da amo dawa: beba: le, bagadewane beda: sa.
Ndikuvomereza mphulupulu zanga; ndipo ndavutika ndi tchimo langa.
19 Na ha lai dunu da dagumui noga: i amola gasa fi gala. Nama ha lai dunu bagohame da nama bai hamedene, higale ba: sa.
Ambiri ndi adani anga amphamvu; amene amandida popanda chifukwa alipo ochuluka kwambiri.
20 Dunu amo da noga: le hamobe dunuma wadela: i dabe iaha, ilia da na higale ba: sa. Bai na da moloi hou amoga hamomusa: , logo hogobeba: le.
Iwo amene amandibwezera zoyipa mʼmalo mwa zabwino amandinyoza pamene nditsatira zabwino.
21 Hina Gode! Dia na mae fisiagama! Na Gode! Nama gasigale mae aligima!
Inu Yehova, musanditaye; musakhale kutali ndi ine Mulungu wanga.
22 Hina Gode! Na Gaga: sudafa! Wahadafa, na fidima!
Bwerani msanga kudzandithandiza, Inu Ambuye Mpulumutsi wanga.

< Gesami Hea:su 38 >