< Gesami Hea:su 37 >

1 Wadela: i hamosu dunu ilia hou hamobeba: le, mae da: i dioma! Giadofale hamobe dunu da liligi bagade lasea, mae mudale ba: ma!
Salimo la Davide. Usamavutike chifukwa cha anthu oyipa kapena kuchitira nsanje amene akuchita cholakwa;
2 Ilia da gisi amo da hedolo bioi gia: su defele, hedolowane alalolesimu. Ilia da bugi amo bioi gia: su defele, hedolo bogomu.
pakuti monga udzu iwo adzafota msanga, ngati mbewu zobiriwira adzanyala msanga.
3 Dilia! Hina Gode Ea hou dafawaneyale dawa: le, moloidafa hou hamoma! Soge amoga fifilale, gaga: iwane esaloma!
Khulupirira Yehova ndipo uzichita zabwino; khazikika mʼdziko ndi kutsata zokhulupirika.
4 Hina Gode Ea hou amo ganodini hahawane hou hogoi helema! E da dia dogoga, hanasu hou hamoma: mu.
Udzikondweretse wekha mwa Yehova ndipo Iye adzakupatsa zokhumba za mtima wako.
5 Dina: disu Hina Godema ima, amola Ema dafawaneyale dawa: ma! Amasea, E da di fidimu.
Pereka njira yako kwa Yehova; dalira Iye ndipo Iyeyo adzachita izi:
6 E da dima moloidafa hou hahamonesimu. Amola Ea hamobeba: le, di da esomogoa eso diga: be agoai ba: mu.
Iye adzachititsa chilungamo chako kuwala ngati mʼbandakucha, chiweruzo chako ngati dzuwa la masana.
7 Hina Gode Ea hanaiga hamoma: ne, ha: aligima! Wadela: i dunu ilia da liligi bagade gagusia, amola hahawane wadela: i ilegesu hou amo hamosea, mae da: i dione ba: ma.
Khala chete pamaso pa Yehova ndipo umudikire mofatsa; usavutike pamene anthu apambana mʼnjira zawo, pamene iwo achita zinthu zawo zoyipa.
8 Da: i dione amola ougili mae hamoma! Amoga da bidi hamosu fawane ba: mu.
Pewa kupsa mtima ndipo tembenuka kuchoka ku ukali, usavutike chifukwa zimenezi zimatsogolera ku zoyipa.
9 Be nowa dunu ilia da Hina Godema dafawaneyale dawa: sea, ilia fawane da osobo bagade ouligimu. Be wadela: i hamosu dunu da gadili sefasi dagoi ba: mu.
Pakuti anthu oyipa adzachotsedwa, koma iwo amene amayembekeza mwa Yehova adzalandira dziko.
10 Wadela: i hamosu dunu da hedolowane alalolesi dagoi ba: mu. Dia da ili hogoi helemu, be hame ba: mu.
Kwa kanthawi oyipa sadzapezekanso; ngakhale muwafunefune, sadzapezekanso.
11 Bodogi dunu da osobo bagade ouligimu. Amola bagade gaguiwane amola olofoiwane esalebe ba: mu.
Koma ofatsa adzalandira dziko ndipo adzasangalala ndi mtendere waukulu.
12 Wadela: i hamosu dunu da noga: le hamosu dunu amo wadela: lesimusa: ilegesa, amola ema higale ougili ba: sa.
Oyipa amakonza chiwembu kutsutsana ndi olungama ndipo amawakukutira mano;
13 Be Hina Gode da wadela: le hamosu dunu iliba: le, ousa. Bai E dawa: Ilia da hedolowane gugunufinisi dagoi ba: mu.
koma Ambuye amaseka oyipa pakuti Iye amadziwa kuti tsiku lawo likubwera.
14 Wadela: i hamosu dunu da hame gagui dunu amola moloidafa hamosu dunu medole legemusa: , ilia gegesu gobihei amo duga: le gadosa, amola ilia oulali disa.
Oyipa amasolola lupanga ndi kupinda uta kugwetsa osauka ndi osowa, kupha iwo amene njira zawo ndi zolungama.
15 Be ilia da ilila: gegesu gobihei amogawane ilila: fane legei dagoi ba: mu. Amola ilia oulali da fifili sali ba: mu.
Koma malupanga awo analasa mitima yawo yomwe, ndipo mauta awo anathyoka.
16 Moloidafa dunu ea fonobahadi gagui da wadela: i hamosu dunu huluane ilia bagade gagui amo baligisa.
Zabwino zochepa zimene olungama ali nazo ziposa chuma cha anthu oyipa ambiri;
17 Bai Hina Gode da wadela: i hamosu dunu ilia gasa fadegale fasimu. Be E da molole hamosu dunu ili gaga: mu.
pakuti mphamvu ya oyipa idzasweka, koma Yehova amasunga olungama.
18 Hina Gode da Ea sia: nabawane hamosu dunu amo noga: le ouligisa. Amola Ea nana liligi da eso huluane ilia: fawane dialumu.
Masiku a anthu osalakwa amadziwika ndi Yehova, ndipo cholowa chawo chidzakhala mpaka muyaya.
19 Wadela: i eso da doaga: sea, ilia da se hame nabimu. Ha: i da doaga: sea, ilia da hame ha: gia: mu.
Pa nthawi ya mavuto iwo sadzafota; mʼmasiku a njala adzakhala ndi zinthu zambiri.
20 Be wadela: i hamosu dunu ilia da bogogia: mu. Hina Godema ha lai dunu, ilia da mosoi gilidabe defele gilisa: i dagoi ba: mu. Mobi da hedolowane geale asi. amo defele ilia da hedolowane alalolesi dagoi ba: mu.
Koma oyipa adzawonongeka; adani a Yehova adzakhala ngati kukongola kwa kuthengo, iwo adzazimirira ngati utsi.
21 Wadela: i hamosu dunu da fa: no bidi imunusa: liligi udigili laha be fa: no hame iaha. Be noga: i dunu da hahawane mae dawa: iwane iaha.
Oyipa amabwereka ndipo sabweza koma olungama amapereka mowolowamanja.
22 Nowa dunu ilia da Hina Gode Ea hahawane dogolegele ba: su galea, ilia da osobo bagade nana liligi defele amo lamu. Be nowa da Ea gagabui amoga aligi galea, ilia da gadili sefasi dagoi ba: mu.
Iwo amene Yehova amawadalitsa adzalandira dziko, koma amene Iye amawatemberera adzachotsedwa.
23 Hina Gode da dunu Ea masa: ne dawa: i logo, amoga masa: ne noga: le ouligisa. Amola E da nowa dunu amo da E nodoma: ne hamosa, amo noga: le gaga: sa.
Ngati Yehova akondwera ndi njira ya munthu, amakhazikitsa mayendedwe ake;
24 Ilia da dafasea, gebe gudu hame dialumu. Bai Hina Gode da ili wa: legadolesimu.
ngakhale atapunthwa sadzagwa, pakuti Yehova amamutchinjiriza ndi dzanja lake.
25 Na da waha da: i hamoi dagoi. Na da fifi misi helei. Be na da Hina Gode noga: i dunu afae fisiagai amo hamedafa ba: i. Amola noga: i dunu ea mano ha: i manu hameba: le, edegenanebe hamedafa ba: i.
Ine ndinali wamngʼono ndipo tsopano ndakalamba koma sindinaonepo olungama akusiyidwa kapena ana awo akupempha chakudya.
26 Noga: i dunu da eso huluane udigiliwane enoma sagosa. Amola e da enoma liligi bu hi lamusa: hahawane iasisa. Amola ea mano da eno dunuma hahawane dogolegele hamosa.
Iwo ndi owolowamanja nthawi zonse ndipo amabwereketsa mwaufulu; ana awo adzadalitsika.
27 Wadela: i hamonanu fisiagale, moloidafa hou hamoma. Amasea, digaga fifi manebe da eso huluane esalalalumu.
Tembenuka kuchoka ku zoyipa ndipo chita zabwino; pamenepo udzakhazikika mʼdziko kwamuyaya.
28 Bai Hina Gode da moloidafa hou amoma asigisa. Amola E da Ea dafawaneyale dawa: be dunu amo hame fisiagasa. E da mae fisili, ili gebewane gaga: lala. Be wadela: i hamosu dunu iligaga fifi manebe dunu da gadili sefasi dagoi ba: mu.
Pakuti Yehova amakonda wolungama ndipo sadzasiya okhulupirika ake. Iwo adzatetezedwa kwamuyaya, koma zidzukulu za oyipa zidzachotsedwa;
29 Moloidafa dunu ilia da osobo bagade nana liligi agoane amo lale, amola amo ganodini, eso huluane fifi lalalumu.
olungama adzalandira dziko ndipo adzakhazikikamo kwamuyaya.
30 Noga: idafa dunu ea sia: da bagade dawa: su gala. Amola e da eso huluane moloidafa hou hamonana.
Pakamwa pa munthu wolungama pamayankhula za nzeru, ndipo lilime lake limayankhula zolungama.
31 E da ea Hina Gode Ea malasu sia: ea dogo ganodini dawa: i diala. Amola e da amo malasu nabawane hamonaneawane hamedafa yolesisa.
Lamulo la Mulungu wake lili mu mtima mwake; mapazi ake saterereka.
32 Wadela: i hamosu dunu da noga: idafa dunu amo ba: lala. Amola e fane legemusa: logo hogosa.
Oyipa amabisala kudikira olungama; kufunafuna miyoyo yawoyo;
33 Be noga: i dunu da ema ha lai dunu ea gasaga wadela: lesi, amo hamedafa ba: mu. Amola fofada: su ganodini, se dabe hame lamu. Bai Hina Gode da e fisiagamu hamedafa dawa:
koma Yehova sadzawasiya pansi pa mphamvu yawo kapena kuti atsutsidwe pamene abweretsedwa pa milandu.
34 Hina Gode da dima hobea misunu hou amo ouligimu, amo dafawaneyale dawa: ma, amola Ea hamoma: ne sia: i, amo nabawane hamoma. Amasea, E da dima nodoma: ne, soge dima imunu. Amola, di da wadela: i hamosu dunu gadili sefasi dagoi ba: mu.
Khulupirira Yehova, ndipo sunga njira yake; Iye adzakukweza ndipo udzalandira dziko kuti likhale lako; udzaona anthu oyipa akuwonongeka.
35 Na da ha afaega, gasa fi wadela: i hamosu dunu dawa: i galu. E da dolo ifa gahe Lebanone sogega hahawane lelebe agoai ba: i.
Ine ndinaona munthu woyipa ndi munthu wopanda chifundo akupeza bwino ngati mtengo wobiriwira pa nthaka ya makolo ake.
36 Be fa: no na amo baligisa ba: loba, e da amogai hame ba: i. Na da e hogoi be hame ba: i.
Koma sanachedwe kumwalira ndipo sanaonekenso; ngakhale ndinamuyangʼanayangʼana, sanapezekenso.
37 Dilia! Dunu noga: i amo noga: le hogole ba: ma! Ea moloidafa hou noga: le hogoma! Olofole hamosu dunu da egaga fifi ahoanebe ba: mu.
Ganizira za munthu wosalakwa, yangʼanitsitsa munthu wolungama; udzaona kuti ali ndi tsogolo labwino ndipo ali ndi zidzukulu zambiri.
38 Be wadela: i hamosu dunu ilia da wadela: lesidafa ba: mu. Amola iligaga fi da halesali dagoi ba: mu.
Koma anthu ochimwa adzawonongeka; iwowo pamodzi ndi zidzukulu zawo zomwe.
39 Hina Gode da moloidafa dunu ili gaga: sa. Bidi hamosu eso da ilima doaga: sea, E da ili gaga: sa.
Chipulumutso cha olungama chimachokera kwa Yehova; Iye ndiye linga lawo pa nthawi ya masautso.
40 E da ili fidisa amola gaga: sa. Wadela: i hamosu dunu da ili wadela: lesisa: besa: le, E da ili gaga: sa. Bai ilia da ilila: gaga: ma: ne, Ema ahoa.
Yehova amawathandiza ndi kuwalanditsa; Iye amawalanditsa kwa oyipa ndi kuwapulumutsa, pakuti amathawira kwa Iye.

< Gesami Hea:su 37 >