< Gesami Hea:su 21 >

1 Hina Gode! Hina bagade da hahawane gala. Bai Di da ema gasa iabeba: le. Di da ema hasalasu hou iabeba: le, e da hahawane nodosa.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Inu Yehova, mfumu ikusangalala mu mphamvu yanu, chimwemwe chake nʼchachikuludi pa kupambana kumene mumapereka!
2 Dia, ea dogoga hanai liligi amo ema i dagoi, amola ea Dima adole ba: i, amo Di ema i dagoi.
Inu mwayipatsa zokhumba za mtima wake ndipo simunayimane zopempha za pa milomo yake. (Sela)
3 Dia ema nodosu liligi bagade gaguli misi, amola habuga gouliga hamoi amo ema figisi.
Inu munayilandira ndi madalitso ochuluka ndipo munayiveka chipewa chaufumu chagolide weniweni pa mutu wake.
4 E da esalusu Dima adole ba: i. Amanoba, Di da osobo bagadega sedagili esaloma: ne ema i.
Iye anakupemphani moyo, ndipo munamupatsa masiku ochuluka kwamuyaya.
5 Dia da e noga: le fidibiba: le, ea hadigi da bagade amola dunu eno da ema nodosa.
Kudzera mʼzigonjetso zimene munapereka, ulemerero wake ndi waukulu; Inu mwapereka pa iyo ulemerero ndi ufumu.
6 Dia ema hahawane dogolegele hou da eso huluane dialumu. Amola Di da ema gadenene esalebeba: le, e da hahawane bagade.
Zoonadi Inu mwayipatsa madalitso amuyaya, Inu mwayipatsa chisangalalo ndi chimwemwe chimene chili pamaso panu.
7 Hina bagade da Hina Gode Bagadedafa Ea hou dafawaneyale dawa: le, lalegagusa. Hina Gode da ema mae yolele, asigiba: le, e eso huluane gaga: i esalumu.
Pakuti mfumu imadalira Yehova; kudzera mʼchikondi chake chosatha cha Wammwambamwamba, iyo sidzagwedezeka.
8 Hina bagade da ea ha lai dunu huluane gagumu, amola Ema higa: i ba: sea, amo huluane gagulaligimu.
Dzanja lanu lidzayimitsa adani anu onse; dzanja lanu lamanja lidzagwira adani anu.
9 Hina Gode masea da, ili huluane lalu helowa: i bagade agoane amoga nene, wadela: lesi dagoi ba: mu. Hina Gode ea ougi amoga ili medole legele, laluga nene sa: i dagoi ba: mu.
Pa nthawi ya kuonekera kwanu mudzawasandutsa ngʼanjo yamoto yotentha. Mu ukali wake Yehova adzawameza, ndipo moto wake udzawatha.
10 Iligaga fi afae da hamedafa esalebe ba: mu, amola hina bagade, ea ili huluane medole legemu.
Inu mudzawononga ana awo pa dziko lapansi, zidzukulu zawo pakati pa anthu.
11 Ilia asigi dawa: su ganodini ilegele, Godema hasalasimusa: dawa: lala, be amomane ilia da Ema hame hasalasimu.
Ngakhale iwo akukonzereni chiwembu mwa kuchenjera kwawo sadzapambana;
12 E da, Ea dadiga gala: le, ili sesele, amalu ilia sinidigili hobeale masunu.
pakuti mudzawapirikitsa ndipo adzaonetsa misana yawo pamene mudzawaloza ndi mivi yanu.
13 Hina Gode! Dia gasa bagade ba: beba: le, ninia Dima bagade nodosa. Ninia da Dima nodone gesami hea: le, dia gasa bagade hou gaguia gadomu.
Mukwezeke Inu Yehova mʼmphamvu yanu, ife tidzayimba nyimbo ndi kutamanda mphamvu yanu.

< Gesami Hea:su 21 >