< Gesami Hea:su 18 >
1 Hina Gode! Na da Dima bagadewane asigisa. Di da na gaga: sudafa.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide mtumiki wa Yehova. Iye anayimbira Yehova nyimbo iyi pamene Yehovayo anamupulumutsa mʼdzanja la adani ake onse ndiponso mʼdzanja la Sauli. Davide anati: Ine ndimakukondani Inu Yehova, mphamvu zanga.
2 Hina Gode da na gaga: sudafa. E da na gasa bagade gagoi gala. E da na gaga: sa amola na da E guga esalea, enoga wadela: mu da hamedei. E da gaga: su liligi agoaiga na gaga: sa.
Yehova ndiye thanthwe langa, chitetezo changa ndi mpulumutsi wanga; Mulungu wanga ndi thanthwe langa mʼmene ndimathawiramo. Chishango changa ndi ndodo yachipulumutso changa, ndi linga langa.
3 Na da Hina Godema wele sia: sea, E da na ha lai ilima na gaga: sa. Hina Godema nodoma!
Ndimayitana Yehova amene ndi woyenera matamando, ndipo ndapulumutsidwa kwa adani anga.
4 Na bogomu gadenenewane ba: i. Wadela: su liligi hano fugala: i agoane da na dedebomu galu.
Zingwe za imfa zinandizinga; mitsinje yothamanga yachiwonongeko inandiopsa kwambiri.
5 Na bogomu da gadenenewane ba: i. Bogoi uli dogoi da sani agoane dili dialu. (Sheol )
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol )
6 Na da se nababeba: le, Hina Godema wele sia: i dagoi. Na da E na fidima: ne wele sia: i. E da Ea Debolo diasu ganodini na fidima: ne wele sia: su nabi dagoi.
Mʼmasautso anga ndinapemphera kwa Yehova; ndinalirira kwa Mulungu wanga kuti andithandize. Ali mʼNyumba yake, anamva mawu anga; kulira kwanga kunafika pamaso pake ndi mʼmakutu mwake.
7 Amalalu, osobo bagade da fofogoi. Goumi ilia bai amola da igugui. Bai Gode da ougi bagade ba: i.
Dziko lapansi linanjenjemera ndi kuchita chivomerezi, ndipo maziko a mapiri anagwedezeka; ananjenjemera chifukwa Iye anakwiya.
8 Ea mi gelabo amoga lalu mobi ahoanebe ba: i. Ea lafidili, lalu sawa: amo da liligi nenanebedawa: , amola nasubu su gilisili ahoanebe ba: i.
Mʼmphuno mwake munatuluka utsi; moto wonyeketsa unatuluka mʼkamwa mwake, makala amoto anali lawilawi mʼkamwa mwake.
9 E da mu alalo gadelai amola mu mobi gasimiginisi gala amo da: iya osoboga dalebe ba: i.
Iye anangʼamba thambo natsika pansi; pansi pa mapazi ake panali mitambo yakuda.
10 E da liligi hedofo galebe amoga fila heda: le ahoanebe ba: i. E da fedege agoane fo da hedofo galebe amoga fila heda: le ahoanebe ba: i.
Iye anakwera pa Kerubi ndi kuwuluka; nawuluka ndi mphepo mwaliwiro.
11 E da gasimigi amoga uligi ba: i. Mu mobi gadugagi amo da hanoga nabai amoga E sisiga: i dagoi.
Iye anapanga mdima kukhala chofunda chake, chophimba chake chomuzungulira chinali mitambo yakuda ya mlengalenga.
12 Mugene igi agoai amola lalu gona: su digagala: su da ha: ha: na bagade amoga misini mu mobi gasimigi amo dugagale dalebe ba: i.
Mʼkuwala kumene kunali pamaso pake munkachokera matalala, makala amoto ndi ziphaliwali zongʼanima.
13 Amalalu, Hina Gode Ea sia: da muagado gugelebe agoane nabi. Dunu huluane da Gode Gadodafa Ea sia: nabi.
Yehova anabangula kumwamba ngati bingu, mawu a Wammwambamwamba anamveka ponseponse.
14 E da Ea dadi dili fisiagagai. Ea ha lai dunu huluane da afafane hobea: i. E da ha: ha: na digagala: su amoga gala: beba: le, ilia da hobea: i dagoi.
Iye anaponya mivi yake nabalalitsa adani ake, ndi zingʼaningʼani zake anawagonjetsa.
15 Hina Gode! Di da Dima ha lai ilima gagabole sia: noba amola ilima ougiba: le gasa bagade sia: noba, hano wayabo bagade da hale hafoga: i dagoi ba: i. Osobo bagade ea bai huluane ba: i dagoi.
Zigwa za mʼnyanja zinaonekera poyera; maziko a dziko lapansi anakhala poyera, Yehova atabangula mwaukali, pamene mpweya wamphamvu unatuluka mʼmphuno mwanu.
16 Hina Gode da ea lobo gududa: le guduli, na gagulaligi, amola hano lugudu bagade amoga na hiougili gadoi.
Ali kumwamba, Iye anatambalitsa dzanja lake ndipo anandigwira; anandivuwula mʼmadzi ozama.
17 Na ha lai dunu da gasa bagade. Ilia gasa da na gasa baligi dagoi. Ilia da na bagade higasa. Be ilia da nama doagala: lalu, Hina Gode da na gaga: i.
Anandipulumutsa kwa mdani wanga wamphamvu, adani anga, amene anali amphamvu kuposa ine.
18 Na da se nabaloba, ilia da na doagala: musa: misi, be amomane Hina Gode da na gaga: i.
Adaniwo analimbana nane pamene ndinali pa mavuto, koma Yehova anali thandizo langa.
19 E da nama hahawaneba: le, na gaga: i.
Iye anandipititsa kumalo otakasuka; anandipulumutsa chifukwa amakondwera nane.
20 Na da wadela: i hou hame amola moloidafa hou fawane hamobeba: le, Hina Gode da na hahawane dogolegele fidisa amola nama bidi ida: iwane iaha.
Yehova wandithandiza molingana ndi chilungamo changa; molingana ndi makhalidwe anga abwino, Iye wandipulumutsa.
21 Na da Gode Ea hamoma: ne sia: i dedei amoma fa: no bobogesu amola Godema fa: no bobogei na da hame buhagi.
Pakuti ine ndinatsata njira za Yehova; ndilibe mlandu wochoka pamaso Mulungu wanga.
22 Na da Ea sema huluane nabawane hamosu amola Ea sia: nababeba: le hame nabasu hou hame hamosu.
Malamulo ake onse ali pamaso panga; sindinasiye malangizo ake.
23 Na da afuda: le hame hamoi amola moloi hou fawane hamonanu. Hina Gode da na hou dawa:
Ndakhala moyo wosalakwa pamaso pake ndipo ndakhala ndi kupewa tchimo.
24 Amo na hou dawa: beba: le, E da nama bidi ida: iwane iaha.
Yehova wandipatsa mphotho molingana ndi chilungamo changa, molingana ndi kuyera kwa manja anga pamaso pake.
25 Hina Gode! Nowa dunu da Dima mae fisili, Dia hou dafawaneyale dawa: iwane hamonanea, Di da amo dunu amola hamedafa yolesimu. Di da nowa dunu moloidafa ba: sea, amo dunu hahawane fidisa.
Kwa wokhulupirika, Inu mumaonetsa kukhulupirika kwanu; kwa anthu amakhalidwe abwino, Inu mumaonetsanso makhalidwe abwino,
26 Di da ledo hamedei fofoloi dunu ilima fofoloi ba: sa. Be wadela: i hamosu dunu Di higasa.
kwa woyera mtima, Inu mumaonetsa kuyera mtima kwanu, koma kwa achinyengo mumaonetsanso kunyansidwa nawo.
27 Nowa dunu amo ea hou hi fonobosea, Di da amo dunu gaga: sa. Be nowa da ilila: hou gaguia gadobe, amo Di da banenesisa.
Inu mumapulumutsa anthu odzichepetsa, koma anthu amtima odzikuza mumawatsitsa.
28 Hina Gode! Di da nama hadigi iaha. Amola gasimigi Dia fadegale fasisa.
Inu Yehova, sungani nyale yanga kuti iziyakabe; Mulungu wanga wasandutsa mdima wanga kukhala kuwunika.
29 Di da nama gasa amo nama ha lai dunuma doagala: musa: defele gala, amo iaha. Amola gasa amo ha lai dunu ilia gagoi amo mugulumusa: defele gala, Dia da nama iaha.
Ndi thandizo lanu nditha kulimbana ndi gulu la ankhondo; ndi Mulungu wanga nditha kuchita zosatheka ndi munthu.
30 Gode Ea hou da noga: idafa amola moloidafa. Ea adi hamomusa: sia: sea, E da hamosa. Nowa dunu Ema masea, E da gaga: su liligi defele amo dunu ea ha lai dunuma gaga: sa.
Kunena za Mulungu, zochita zake ndi zangwiro; mawu a Yehova alibe cholakwika. Iye ndi chishango kwa onse amene amathawira kwa Iye.
31 Hina Gode Hi fawane da Godedafa. Hi fawane da nini gaga: su dunu.
Mulungu wina ndi uti wofanana nanu Yehova? Ndipo ndani amene ndi Thanthwe kupatula Mulungu wathu?
32 Gode Hi fawane da nama gasa iaha amola na da logoba: le ahoasea, E da na noga: le ouligisa.
Ndi Mulungu amene anandipatsa mphamvu ndi kulungamitsa njira yanga.
33 E da na goumiba: le noga: le heda: ma: ne, na emo amo “dia” ohe ea emo defele hamosa. Amola na da goumiga ahoasea, E da na mae dafama: ne noga: le ouligisa.
Iye amasandutsa mapazi anga kukhala ngati ambawala yayikazi; Iye amandithandiza kuyimirira pamwamba pa mapiri.
34 E da gegesu hou nama olelesa. Na da gasa bagade oulali amoga gegemusa: , E da nama gasa iaha.
Iye amaphunzitsa manja anga kuchita nkhondo; manja anga amatha kuthyola uta wachitsulo.
35 Hina Gode! Di da na gaga: lala. Dia ouligisu hou da na fidibiba: le, eno dunu da nama nodosa. Dia gasa fawane da na gaga: i dagoi.
Inu mumandipatsa chishango chachipambano, ndipo dzanja lanu lamanja limandichirikiza; mumawerama pansi kundikuza.
36 Dia fidibiba: le, na da na ha lai amoga hame gagulaligi ba: i. Na da hamedafa dafai.
Munakulitsa njira yoyendamo ine, kuti mapazi anga asaguluke.
37 Na da na ha lai dunu sefasili, gagulaligisa. Amasea, gegesu mae fisili, ilia da wadela: lesi dagoi ba: sea fawane yolesisa.
Ndinathamangitsa adani anga ndi kuwapitirira; sindinabwerere mpaka atawonongedwa.
38 Na da ili fane legesea, ilia da bu wa: legadomu gogolesa. Ilia da na emo gadenene dafasea, hasali dagoi ba: sa.
Ndinakantha adaniwo kotero kuti sanathenso kudzuka; anagwera pa mapazi anga.
39 Di fawane da na gegema: ne nimi iaha amola na ha lai dunuma hasalasima: ne gasa iaha.
Inu munandiveka ndi mphamvu yokachitira nkhondo, munachititsa kuti ndigonjetse adani anga.
40 Dia hamobeba: le, na ha lai da naba: le hobeasa. Nowa da nama higasa, na da wadela: lesisa.
Inu munachititsa adani anga kutembenuka, kuonetsa misana yawo pothawa, ndipo ine ndinawononga adani angawo.
41 Ilia da fidima: ne diginiwane wele sia: sa. Be gaga: su dunu hame ba: sa. Ilia da Hina Godema wele sia: sa, be E da hame alofesa.
Iwo anafuwula kupempha thandizo, koma panalibe ndi mmodzi yemwe owapulumutsa. Analirira kwa Yehova koma sanawayankhe.
42 Na da ili gagoudane amola ilia gulu dou agoane hamone da fo misini doga: le fasisa, amo defele ilia da fafu logoga dialebe agoane ba: sa amola na da ilima ososa: gisa.
Ine ndinawaperesa ngati fumbi lowuluka ndi mphepo. Ndinawapondaponda ngati matope a mʼmisewu.
43 Hame nabasu dunu da nama hasalasimusa: dawa: i. Be Di da na gaga: i. Di da na fifi asi gala ilima hina bagade hamoi. Amola dunu fi na da musa: hame dawa: i, amo da na ouligimusa: , nama misi dagoi.
Inu mwandipulumutsa mʼmanja mwa anthu; mwandisandutsa kukhala mtsogoleri wa anthu a mitundu ina. Anthu amene sindikuwadziwa ali pansi pa ulamuliro wanga.
44 Ga soge fi dunu da nama beguduli, na sia: nabawane fa: no bobogesa.
Alendo amadzipereka okha pamaso panga; akangomva za ine amandigonjera.
45 Ilia da beda: ga ilia gasa bagade gagoi amo fisili, yaguguiwane gadili maha.
Iwo onse anataya mtima; anatuluka mʼmalinga awo akunjenjemera.
46 Hina Gode da esala. Na Gaga: su dunuma nodoma! Na Gaga: su Gode amo Ea gasa bagade hou amo dunu huluanema olelema.
Yehova ndi wamoyo! Litamandidwe Thanthwe langa! Akuzike Mulungu Mpulumutsi wanga!
47 Ea da na ha lai ilima hasalasimusa: nama gasa iaha. Na da dunu fi ilima hasalasimusa: , E da amo dunu fi banenesisa.
Iye ndi Mulungu amene amabwezera chilango, amene amagonjetsa anthu a mitundu yonse amene ali pansi pa ulamuliro wanga,
48 E da na gaga: sa. Hina Gode! Na da nama ha lai ilima hasalasimusa: Dia hamosa. Amola nimi bagade dunu nama mae doagala: ma: ne, Dia da na gaga: sa.
amene amandipulumutsa mʼmanja mwa adani anga. Inu munandikuza kuposa adani anga; munandilanditsa mʼmanja mwa anthu ankhanza.
49 Amaiba: le, na da dunu fifi asi gala amo ganodini Dima nodosa. Na da Dima nodone gesami hea: sa.
Choncho ine ndidzakutamandani pakati pa anthu a mitundu ina, Inu Yehova; ndidzayimba nyimbo zotamanda dzina lanu.
50 Gode da Ea hina bagade ilegei ema hasalasisu hou bagade iaha. E da dunu amo E da ilegei ema Ea asigidafa hou olelesa. E da Da: ibidi amola egaga fi ilima Ea asigidafa hou mae fisili eso huluane olelelalumu.
Iye amapereka chipambano chachikulu kwa mfumu yake; amaonetsa chikondi chosasinthika kwa wodzozedwa wake, kwa Davide ndi zidzukulu zake kwamuyaya.