< Gesami Hea:su 17 >

1 Hina Gode! Na sia: be goe nabima. Na moloidafa fofada: su ba: ma: ne Dima edegesa. Na da Dia na fidima: ne Dima diginiwane wele sia: sa. Dia nabima. Na da ogogole hame sia: ne gadosa.
Pemphero la Davide. Imvani Inu Yehova pempho langa lachilungamo; mverani kulira kwanga. Tcherani khutu kuti mumve pemphero langa popeza silikuchokera pakamwa pachinyengo.
2 Dia da na moloidafa hou dawa: beba: le, Dia da na fidima: ne fofada: mu.
Kusalakwa kwanga kuchokera kwa inu; maso anu aone chimene ndi cholungama.
3 Dia na dogo dawa: Di da gasi ganodini nama misini, na hou huluane abodele ba: su. Di da na hou amo ganodini, wadela: i hanai hou hamedafa ba: i.
Ngakhale Inu mutafufuza mtima wanga ndi kundisanthula usiku, ngakhale mutandiyesa, simudzapeza kanthu; Ine ndatsimikiza kuti pakamwa panga sipadzachimwa.
4 Eno dunu da wadela: i sia: bagade sia: sa. Be na lafiga agoai hame sia: sa. Na da Dia hamoma: ne sia: i amo fa: no bobogei. Amola nimi bagade hou amoma hame fa: no bobogei.
Kunena za ntchito za anthu, monga mwa mawu a pakamwa panu, Ine ndadzisunga ndekha posatsata njira zachiwawa.
5 Na da eso huluane Dia logodili ahoasu amola na da afuda: le hamedafa asi.
Mayendedwe anga akhazikika pa njira zanu; mapazi anga sanaterereke.
6 Hina Gode! Na Dima sia: ne gadosu amo da Dia na sia: ne gadobe bu alofele iaha. Amaiba: le, nama ba: leguda: le, na sia nabima.
Ine ndikuyitana Inu, Mulungu wanga, pakuti mudzandiyankha; tcherani khutu lanu kwa ine ndipo mumve pemphero langa.
7 Dia asigidafa hou amo nama olelema amola na gaga: ma. Na da Di guga esalea, na da na ha lai ilima gaga: i dagoi ba: sa.
Onetsani kudabwitsa kwa chikondi chanu chachikulu, Inu amene mumapulumutsa ndi dzanja lanu lamanja iwo amene amathawira kwa inu kuchoka kwa adani awo.
8 Di da Dia si amoma gaga: su hou amo defele, na gaga: ma. Wadela: i hamosu dunu da nama doagala: sa: besa: le, Dia ogelebaha na wamolegema. Nimi bagade ha lai dunu da na guba: le sisiga: sa. Ilia da asigi hou hame dawa: amola ilia da gasa fili sia: daha.
Mundisunge ine ngati mwanadiso; mundibise mu mthunzi wa mapiko anu,
9
kuchoka kwa oyipa amene amandizinga ine, kuchoka kwa anthu amene ndi adani anga, amene andizungulira ine.
Iwo amatseka mitima yawo yopanda chifundo, ndi pakamwa pawo amayankhula modzitamandira.
11 Ilia da na sisiga: le disi. Ilia da na hiougia gudumusa: logo hogoi helesa.
Andisaka, tsopano andizungulira ndi maso awo atcheru, kuti andigwetse pansi.
12 Ilia da soge laione wa: me agoai, na desega aligili medole manusa: amola dodosa: ne manusa: oulela.
Iwo ali ngati mkango wofuna nyama; ngati mkango waukulu wokhala mobisala.
13 Hina Gode misa! Na ha lai ilima gegene sefasima. Amola, ilima hasalasima. Dia gobihei bagade amoga gegebeba: le, na gaga: ma.
Dzukani Yehova, mulimbane nawo ndipo muwagwetse pansi; landitseni kuchoka kwa oyipa ndi lupanga lanu.
14 Wadela: i hamosu dunu da osobo bagadega esalea, ilia da ilia hanai liligi huluane gagusa. Ilia da nama ha laiba: le, Di na gaga: ma. Dia da se iasu bagade ilima ima: ne, gagadole ilegei dagoi. Amo se iasu da ilima ianu, ili baligili amola ilia mano amola ilia mano ilia mano amo defele ilima se iasu ima: ne ba: mu da defea.
Inu Yehova, pulumutseni ndi dzanja lanu kwa anthu otere, kwa anthu a dziko lino amene mphotho yawo ili mʼmoyo uno. Inu mumaletsa njala kwa amene asangalatsidwa nanu; ana awo aamuna ali ndi zinthu zambiri, ndipo iwo amasunga chuma cha ana awo.
15 Be na da wadela: le hame hamoiba: le, na da Di ba: mu. Amola, na da nedigisia, Di guga esalebeba: le, na da hahawane bagade ba: mu.
Ndipo ine mʼchilungamo ndidzaona nkhope yanu; pamene ndidzadzuka, ndidzakondwera kwambiri poonana nanu.

< Gesami Hea:su 17 >