< Gesami Hea:su 141 >

1 Hina Gode! Na Dima wele sia: sa! Wahadafa, na fidima! Na Dima wele sia: sea, Dia nabima!
Salimo la Davide. Inu Yehova ndikukuyitanani; bwerani msanga kwa ine. Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu.
2 Na sia: ne gadosu amo gabusiga: gobele salasu defele, Dia lama. Na lobo gaguia gadobeba: le, Dia amo hou daeya gobele salasu defele ba: ma.
Pemphero langa lifike kwa Inu ngati lubani; kukweza manja kwanga kukhale ngati nsembe yamadzulo.
3 Hina Gode! Na lafi noga: le sosodo aligima! Na lafi logoga, sosodo aligisu dunu asunasima!
Yehova ikani mlonda pakamwa panga; londerani khomo la pa milomo yanga.
4 Na da wadela: i hou hanasa: besa: le, Di fidima. Amola na da wadela: i hamosu dunuma mae gilisima: ne, amola ilia lolo nasu amoga mae masa: ne, Di fidima.
Musalole kuti mtima wanga ukokedwere ku zoyipa; kuchita ntchito zonyansa pamodzi ndi anthu amene amachita zoyipa; musalole kuti ndidye nawo zokoma zawo.
5 Dunu noga: idafa da nama asigiba: le, dawa: ma: ne se iasu amola gagabosu nama imunu da defea. Be wadela: i hamosu dunu ilia nama nodosu, amo na da hame lale salimu. Bai na da eso huluane ilia wadela: i hou fisima: ne sia: ne gadolala.
Munthu wolungama andikanthe, chimenecho ndiye chifundo; andidzudzule ndiye mafuta pa mutu wanga. Mutu wanga sudzakana zimenezi. Komabe pemphero langa nthawi zonse ndi lotsutsana ndi ntchito za anthu ochita zoyipa.
6 Ilia ouligisu dunu da igi gafulua bogoma: ne fulisali ba: sea, dunu eno da na sia: i liligi da dafawane galebeyale dawa: le sia: mu.
Olamulira awo adzaponyedwa pansi kuchokera pa malo okwera kwambiri, ndipo anthu oyipa adzaphunzira kuti mawu anga anayankhulidwa bwino.
7 Lalu ifa da gaga: ne habele dudunumiai ba: mu. Amo defele, amo dunu ilia gasa da bogoi ulidogoi bega: afagogoi ba: mu. (Sheol h7585)
Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol h7585)
8 Be Ouligisudafa Hina Gode! Na Dima dafawaneyale dawa: lala. Na da Dia gaga: su hou hogosa. Amola na mae bogoma: ne, Di gaga: ma.
Koma maso anga akupenyetsetsa Inu Ambuye Wamphamvuzonse; ndimathawira kwa Inu, musandipereke ku imfa.
9 Wadela: i hamosu dunu, ilia da na sa: ima: ne sani dilisisa. Dia na gaga: ma!
Mundipulumutse ku misampha imene anditchera, ku makhwekhwe amene anthu oyipa andikonzera.
10 Wadela: i hamosu dunu ilila: sani amoga ilila: sa: imu da defea. Amola na da hahawane masa: ne, Di fidima!
Anthu oyipa akodwe mʼmaukonde awo, mpaka ine nditadutsa mwamtendere.

< Gesami Hea:su 141 >