< Gesami Hea:su 132 >

1 Hina Gode! Da: ibidi amola ea se baligili nabasu, amo mae gogolema!
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Inu Yehova, kumbukirani Davide ndi mavuto onse anapirira.
2 Hina Gode! Di da Ya: igobe ea Gode Bagadedafa. Da: ibidi ea Dima ilegele sia: i amo mae gogolema! E amane ilegele sia: i,
Iye analumbira kwa Yehova ndi kulonjeza kwa Wamphamvu wa Yakobo kuti,
3 “Na da na diasua hame masunu amola hame golamu, amola hele mae fili galeawane, Hina Gode (Ya: igobe ea Gode Bagadedafa) Ea: diasu gagumu.”
“Sindidzalowa mʼnyumba mwanga kapena kugona pa bedi langa:
4
sindidzalola kuti maso anga agone, kapena zikope zanga ziwodzere,
5
mpaka nditamupezera malo Yehova, malo okhala a Wamphamvu wa Yakobo.”
6 Ninia da Bedeleheme moilaiga esaloba, Dia Gousa: su Sema Gagili ea hou nabi. Ninia da amo hogolala, Yialimi soge ganodini dialebe ba: i.
Zoonadi, tinamva za Bokosi la Chipangano ku Efurata, tinalipeza mʼminda ya ku Yaara:
7 Ninia amane sia: i, “Ninia Hina Gode Ea diasuga afia: la: di. Ninia Ea Fisu midadi nodone sia: ne gadomusa: afia: la: di.
“Tiyeni tipite ku malo ake okhalamo; tiyeni tikamulambire pa mapazi ake.
8 Hina Gode! Debolo diasuga misa! Amola Dia Gousa: su Sema Gagili da Dia gasa bagade hou dawa: digima: ne olelesuba: le, amo Dia gaguli misini, amogawi mae fisili, eso huluane esalalaloma!
‘Dzukani Yehova, ndipo bwerani ku malo anu opumulira, Inuyo ndi Bokosi la Chipangano limene limafanizira mphamvu zanu.
9 Dia gobele salasu dunu da eso huluane moloidafa hou abula agoane salimu da defea. Dia fi dunu ilia hahawaneba: le gesami hea: mu da defea.
Ansembe anu avekedwe chilungamo; anthu anu oyera mtima ayimbe nyimbo mwachimwemwe.’”
10 Di da Dia hawa: hamosu dunu Da: ibidi, ema ilegele sia: i dagoi. Amaiba: le, Dia ilegei hina bagade amo higale mae yolesima.
Chifukwa cha Davide mtumiki wanu, musakane wodzozedwa wanu.
11 Di da Da: ibidima dafawanedafa ilegele sia: su hamoi, amola amo ilegele sia: i Di da hamedafa bugimu. Di amane ilegele sia: i, “Na da dia mano afae amo hina bagade hamomu, amola e da di bagia Isala: ili fi ouligilalumu.
Yehova analumbira kwa Davide, lumbiro lotsimikizika kuti Iye sadzasintha: “Mmodzi wa ana ako ndidzamuyika pa mpando waufumu;
12 Dia mano ilia Na gousa: su noga: le nabasea, amola Na hamoma: ne sia: i ilima i, amo nabawane hamosea, ilia mano amola da di bagia, eso huluane mae fisili, Isala: ili fi ouligilalumu.”
ngati ana ako azisunga pangano langa ndi malamulo amene ndiwaphunzitsa, pamenepo ana awo adzakhala pa mpando wako waufumu kwamuyaya ndi muyaya.”
13 Hina Gode da Saione Moilai Bai Bagade amo ganodini E esaloma: ne, ilegei dagoi.
Pakuti Yehova wasankha Ziyoni, Iye wakhumba kuti akhale malo ake okhalamo:
14 E amane ilegele sia: i, “Na da Saione Moilai Bai Bagade amo ganodini eso huluane fifi ahoanumu. Na da amogawi Isala: ili fi ouligilalumu hanai galebe.
“Awa ndi malo anga opumapo ku nthawi za nthawi; ndidzakhala pano pa mpando waufumu, pakuti ndakhumba zimenezi.
15 Na da Saione fi dunu ilia esaloma: ne lamu liligi defele ilima imunu. Na da Saione Moilai Bai Bagadega esalebe hame gagui dunu, ilima sadima: ne ha: i manu imunu.
Ndidzadalitsa mzindawu ndi zinthu zambiri; anthu ake osauka ndidzawakhutitsa ndi chakudya.
16 Na da Saione fi ilia gobele salasu dunu, ilia hamobe huluane amo ganodini, gaga: su hou abula agoane ilima imunu. Amola Saione fi dunu da hahawaneba: le, gesami hea: mu amola wele sia: mu.
Ndidzaveka ansembe ake chipulumutso, ndipo anthu ake oyera mtima adzayimba nthawi zonse nyimbo zachimwemwe.
17 Goegawi, Na da Da: ibidi egaga fi Dunu afae amo Hina Bagadedafa hamomu. Amola Na da Na ilegei Hina Bagade Ea ouligisu hou noga: le gaga: mu.
“Pano ndidzachulukitsa mphamvu za Davide ndi kuyikapo nyale ya wodzozedwa wanga.
18 Na da Ea ha lai dunu amo gogosiama: ne hamomu. Be Ea ouligibi da bagade gaguiwane heda: mu.”
Ndidzaveka adani ake manyazi, koma chipewa chaufumu pamutu pake chidzakhala chowala.”

< Gesami Hea:su 132 >