< Gesami Hea:su 131 >

1 Hina Gode! Na da na hidale gasa fisu hou yolesi dagoi. Na da mimogo hou, amola liligi huluane amo nama da gasa bagade ba: sa, na da bu hame dawa: lumu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide. Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza, maso anga siwonyada; sinditengeteka mtima ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
2 Be amomane, na da hahawane olofole esala. Mano amo da eme hi fei dialea, ouiya: le dialebe defele, na dogo da denesini diala.
Koma moyo wanga ndawutontholetsa ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa, moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
3 Isala: ili fi! Hina Gode Ea hou eso huluane mae fisili, dafawaneyale dawa: laloma!
Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< Gesami Hea:su 131 >