< Gesami Hea:su 123 >

1 Hina Gode! Di da Hebene fi ouligisa. Na da Dima ba: le gadosa.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga kwa Inu, kwa Inu amene mumakhala kumwamba.
2 Hawa: hamosu dunu da ea hina dunu da e ouligima: ne dawa: sa, amola hawa: hamosu uda da ea hina uda e ouligima: ne dawa: sa. Amo defele, ninia Hina Gode, Dia ninima asigili gogolema: ne olofosu ima: ne, nini da ouesalumu.
Taonani, monga momwe maso a akapolo amayangʼana mʼdzanja la mbuye wawo, monga momwenso maso a mdzakazi amayangʼana mʼdzanja la dona wake, choncho maso athu ali kwa Yehova Mulungu wathu, mpaka atichitire chifundo.
3 Hina Gode! Dia asigili gogolema: ne olofosu ninima ima! Dunu eno da ninima bagadewane higasu.
Mutichitire chifundo, Inu Yehova mutichitire chifundo, pakuti tapirira chitonzo chachikulu.
4 Bagade gagui dunu da eso bagohamedafa baligili ninima haboseselalu. Hidale gasa fi dunu da eso bagohamedafa nini higale ba: lalu.
Ife tapirira mnyozo wambiri kuchokera kwa anthu odzikuza, chitonzo chachikulu kuchokera kwa anthu onyada.

< Gesami Hea:su 123 >