< Gesami Hea:su 121 >

1 Na da goumiga ba: le gadosa. Na fidisu da habodili misa: bela: ?
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga ku mapiri; kodi thandizo langa limachokera kuti?
2 Nama fidisu da Hina Gode, mu amola osobo bagade hahamosu, Emadi maha.
Thandizo langa limachokera kwa Yehova, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
3 E da di dafama: ne logo hame doasimu. Di Gaga: su dunu da mae golale esala.
Sadzalola kuti phazi lako literereke; Iye amene amakusunga sadzawodzera.
4 Isala: ili fi dunu ilia Gaga: su Dunu da golamu hamedafa dawa:
Taonani, Iye amene amasunga Israeli sadzawodzera kapena kugona.
5 Hina Gode da di sosodo aligimu. E da dia afoguga aligili, di gaga: sa.
Yehova ndiye amene amakusunga; Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
6 Eso yoga, di da esoga hame gia: mu. Gasia, di da oubi yoga se hame nabimu.
Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana, kapena mwezi nthawi ya usiku.
7 Hina Gode da di se mae nabima: ne, di ouligimu. E da di gaga: mu.
Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse; adzasunga moyo wako.
8 Di da misini bu ahoasea, E da eso huluane mae fisili di gaga: lalumu.
Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako; kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< Gesami Hea:su 121 >