< Gesami Hea:su 120 >

1 Na da bidi hamosu ba: beba: le, Hina Godema wele sia: i. Amola E da nama dabe adole i.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
2 Ogogosu dunu da nama hasalasisa: besa: le, Dia na gaga: ma.
Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
3 Dilia ogogosu dunu! Gode da dilima adi hamoma: bela: ? E da habodane dilima se dabe ima: bela: ?
Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
4 Amabela: ? E da dadi gagui dunu ea dadi agei o lalu oso gia: i bagade amoga se dabe ima: bela: ?
Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
5 Dili bisili fifi labe da wadela: idafa Misiege amola Gida dunu fi amo ganodini ili bisili fifi labe defele gala.
Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
6 Na da eso bagohamedafa fifi lai amo da olofosu higasa, amo ganodini esalebe ba: i.
Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
7 Na da olofoma: ne ilima sia: sea, ilia da ha lamusa: fawane dawa: sa.
Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.

< Gesami Hea:su 120 >