< Gesami Hea:su 105 >

1 Hina Godema nodone sia: ma! Ea gasa bagade hou olelema! Ea hamobe amo fifi asi gala huluanema olelema!
Yamikani Yehova, itanani dzina lake; lalikirani pakati pa anthu a mitundu ina zimene Iye wachita.
2 Hina Godema nodone gesami hea: le ima! Amola liligi noga: idafa Ea hamobe amo adodoma.
Imbirani Iye, imbani matamando kwa Iyeyo; fotokozani za machitidwe ake onse odabwitsa.
3 Nini da Ea fi dunuba: le, hahawane nodoma. Amola dunu huluane Ema nodone sia: ne gadobe amo da hahawane nodoma: ma.
Munyadire dzina lake loyera; mitima ya iwo amene amafunafuna Yehova ikondwere.
4 Hina Gode Ea fidima: ne lala masa, amola Ema mae yolele nodonanoma!
Dalirani Yehova ndi mphamvu zake; funafunani nkhope yake nthawi yonse.
5 Dilia da Gode Ea hawa: hamosu dunu A: ibalaha: me amola Ya: igobe, Hi ilegele lai, egaga fifi mana. Dilia da Gode Ea musa: degabo hame ba: su hou hamoi amo dawa: ma, amola se imunusa: fofada: su Ea hamoi, amo bu dawa: ma.
Kumbukirani zodabwitsa zimene Iye anazichita, zozizwitsa zake ndi maweruzo amene anapereka,
6
inu zidzukulu za Abrahamu mtumiki wake, inu ana a Yakobo, osankhika ake.
7 Hina Gode da ninia Gode. Ea hamoma: ne sia: i, E da osobo bagade fifi asi huluane ilima sia: i.
Iye ndiye Yehova Mulungu wathu; maweruzo ake ali pa dziko lonse lapansi.
8 E da Ea Gousa: su sema hamoi amo eso huluane mae fisili ouligilalumu. E hamomusa: ilegei da fifi manebe 1,000 bobaligila masunu, ilima dialumu.
Iyeyo amakumbukira pangano lake kwamuyaya, mawu amene analamula kwa mibado yonse,
9 E da A: ibalaha: me amola Aisage elama hamomusa: ilegele sia: i, amo E da gagui dialumu.
pangano limene Iye anapanga ndi Abrahamu, lumbiro limene analumbira kwa Isake.
10 Hina Gode da Ya: igobema eso huluane dialoma: ne gousa: su hamoi.
Iye analitsimikiza kwa Yakobo monga zophunzitsa, kwa Israeli monga pangano lamuyaya:
11 E amane ilegele sia: i, “Na da Ga: ina: ne soge dima imunu. Amo soge da di fawane gaguli esalumu.”
“Ndidzapereka kwa iwe dziko la Kanaani ngati gawo la cholowa chako.”
12 Gode Ea fi dunu da bagahame galu. Ilia da Ga: ina: ne soge ganodini ga fi dunu agoane ba: i.
Pamene iwo anali ngati anthu ochepa mʼchiwerengero, ochepa ndithu, ndiponso alendo mʼdzikolo,
13 Ilia da soge enoga enogaia udigili lafiadalu. Ilia da fifilai enoga enogaia udigili lafiadalu.
ankayendayenda kuchoka ku mtundu wina wa anthu ndi kupita ku mtundu wina, kuchoka mu ufumu wina kupita ku wina.
14 Be Gode da ili gaga: iba: le, eno fi da ili hame banenesi. Ili gaga: ma: ne, Gode da eno hina bagade dunu ilima amane sisane i,
Iye sanalole wina aliyense kuwapondereza; anadzudzula mafumu chifukwa cha iwo:
15 “Na ilegei hawa: hamosu dunu, ilima mae se nabasima. Na balofede dunuma, mae digili ba: ma!”
“Musakhudze odzozedwa anga; musachitire choyipa aneneri anga.”
16 Hina Gode da ilia sogega ha: iasi amola ilia ha: i manu logo hedofai dagoi.
Iye anabweretsa njala pa dziko ndipo anawononga chakudya chonse;
17 Be E da dunu ea dio amo Yousefe, (e da udigili hawa: hamomusa: bidi lai) amo ili bisima: ne asunasi.
Iyeyo anatumiza munthu patsogolo pawo, Yosefe anagulitsidwa ngati kapolo.
18 Ea emo da sia: inega la: gi amola ea galogoa sisiga: le, ouli gisa: gisu ba: i.
Iwo anavulaza mapazi ake ndi matangadza, khosi lake analiyika mʼzitsulo,
19 E da se nabawane ouesalu amogainini ea musa: ba: la: lusu liligi da dafawane doaga: i dagoi ba: i. Hina Gode Ea sia: da ea ba: la: lusu da dafawane olelei.
mpaka zimene Iye ananeneratu zitakwaniritsidwa, mpaka mawu a Yehova ataonetsa kuti Iye ananena zoona.
20 Amalalu, Idibidi hina bagade (e da fifi asi gala bagohame ouligisu) ea se iasu diasu logo doasima: ne sia: i.
Mfumu inatuma munthu kukamumasula, wolamulira wa mitundu ya anthu anamasula iyeyo.
21 E da Yousefe amo Idibidi gamane ouligima: ne sia: i. E da Idibidi soge huluane, ea fawane ouligima: ne sia: i. Yousefe da eagene dunu amola hina bagade
Anamuyika kukhala wolamulira nyumba yake, wolamulira zonse zimene iye anali nazo,
22 Hina bagade ea sia: beba: le, Yousefe da eagene dunu amola hina bagade ea fada: i sia: su dunu huluanema ouligi galu.
kulangiza ana a mfumu monga ankafunira ndi kuphunzitsa nzeru akuluakulu.
23 Amalalu, Ya: igobe da Idibidi sogega asili, ha: ini fi.
Tsono Israeli analowa mu Igupto; Yakobo anakhala monga mlendo mʼdziko la Hamu.
24 Hina Gode da Ea fi dunuma, mano bagohame i. E da ilima ha lai dunu baligima: ne, gasa bagade Ea fi dunuma i.
Yehova anachulukitsa anthu ake; ndipo anachititsa kuti akhale ochuluka kwambiri kuposa adani awo;
25 Hina Gode da hamobeba: le, Idibidi dunu da Gode Ea fi dunuma bagade higasu. Idibidi dunu da Isala: ili dunuma bagadewane ogogosu.
amene mitima yawo anayitembenuza kuti idane ndi anthu ake, kukonzera chiwembu atumiki ake.
26 Amalalu, Gode da Ea ilegei hawa: hamosu dunu Mousese amola Elane ela asunasi.
Yehova anatuma Mose mtumiki wake, ndi Aaroni amene Iye anamusankha.
27 Ela da Gode Ea gasa bagade hou amola musa: hame ba: su hou amo Idibidi soge ganodini hamoi.
Iwo anachita zizindikiro zozizwitsa pakati pawo, zodabwitsa zake mʼdziko la Hamu.
28 Gode da Idibidi sogega gasi iasi. Be Idibidi dunu da Ea hamoma: ne sia: i nabawane hame hamoi.
Yehova anatumiza mdima nasandutsa dziko kuti likhale la mdima. Koma anthuwo anakaniratu mawu a Yehova.
29 E da ilia hano huluane maga: me a: i asili, menabo huluane bogogia: i.
Yehova anasandutsa madzi awo kukhala magazi, kuchititsa kuti nsomba zawo zife.
30 Guama da ilia soge huluane nabalesi. Hina bagade ea diasu amolawane guamaga nabalesi.
Dziko lawo linadzaza ndi achule amene analowa mʼzipinda zogona za olamulira awo.
31 Gode da hamoma: ne sia: beba: le, gagoba: amola mimini da soge huluane ganodini bagadewane wa: le lafia: su.
Iye anayankhula, ndipo kunabwera ntchentche zochuluka ndi nsabwe mʼdziko lawo lonse.
32 E da gibu mae iawane, mugene amola ha: ha: na fawane ilia sogega iasi.
Iyeyo anatembenuza mvula yawo kukhala matalala, ndi zingʼaningʼani mʼdziko lawo lonse;
33 Amoga E da ilia waini efe amola figi ifa amola ifa huluane gugunufinisi dagoi.
Anagwetsa mitengo yawo ya mpesa ndi mitengo yawo ya mkuyu, nawononganso mitengo ina ya mʼdziko lawolo.
34 E da hamoma: ne sia: beba: le, danuba: wa: i osea: i, idimu hamedeidafa, amo ilima asunasi.
Iye anayankhula, ndipo dzombe linabwera, ziwala zosawerengeka;
35 Ilia da ifalabo amola ha: i manu bugi amo huluane na dagoi.
zinadya chilichonse chobiriwira cha mʼdziko lawo, zinadya zonse zotuluka mʼnthaka yawo.
36 E da Idibidi sosogo fi magobo dunu mano huluane fane lelegei.
Kenaka anakantha ana onse oyamba kubadwa a mʼdziko lawo, zipatso zoyamba za umunthu wawo wonse.
37 Amalalu, E da Isala: ili dunu gadili oule asi. Ilia da silifa amola gouli gisawene gadili asi. Ilia huluane da dagumui amola gasa bagade ba: i.
Yehova anatulutsa Israeli, atatenga siliva ndi golide wambiri, ndipo pakati pa mafuko awo palibe mmodzi amene anafowoka.
38 Idibidi dunu da iliba: le beda: i, amola ili ahoabeba: le hahawane ba: i.
Dziko la Igupto linakondwa pamene iwo anachoka, pakuti kuopsa kwa Israeli kunawagwera iwo.
39 Gode da Ea fi dunuma mu mobiga dedeboi. Amola gasia hadigima: ne lalu iasi.
Iye anatambasula mitambo ngati chofunda chawo, ndi moto owawunikira usiku.
40 Ilia Ema edegeiba: le, e da ilima aiyei (quail) sio i. E da Hebeneganini, ili sadima: ne, ha: i manu i.
Iwo anapempha, ndipo Iye anawabweretsera zinziri ndipo anawakhutitsa ndi chakudya chochokera kumwamba.
41 E da igi da: iya fabeba: le, hano fudagala: le, musa: le sa: ili, hano bagadewane hafoga: i sogega hano yogo asi.
Iye anatsekula thanthwe, ndipo madzi anatuluka; ngati mtsinje anayenda mʼchipululu.
42 E da musa: Ea hawa: hamosu dunu A: ibalaha: mema hadigi ilegele sia: su, amo bu dawa: i.
Pakuti anakumbukira lonjezo lake loyera limene linaperekedwa kwa Abrahamu mtumiki wake.
43 Amaiba: le, e da Ea ilegei fi dunu gadili oule asi. Amola ilia da hahawaneba: le, nodone gesami hea: i amola wele sia: i.
Iye anatulutsa anthu ake akukondwera, osankhika ake akufuwula mwachimwemwe;
Iye anawapatsa mayiko a anthu a mitundu ina ndipo anakhala olowamʼmalo a zimene ena anazivutikira,
45 Ea fi dunu da Ea sema amo noga: le nabawane hamoma: ne, amola Ea hamoma: ne sia: i amo huluane noga: le fa: no bobogema: ne, E da eno dunu fi ilia soge samogene, Ea fi dunuma i. Amola Ea fi dunu da eno dunu ilia bugili nasu soge gesoama: ne, E da logo doasi. Hina Godema nodoma!
kuti iwo asunge malangizo ake ndi kutsatira malamulo ake. Tamandani Yehova.

< Gesami Hea:su 105 >