< Gesami Hea:su 103 >

1 Hina Godema nodoma! Na asigi dawa: su amola na esalusu huluane amoga Hina Gode Ea Hadigi Dio amoma nodomu da defea.
Salimo la Davide. Tamanda Yehova, iwe moyo wanga; ndi zonse zamʼkati mwanga zitamande dzina lake loyera.
2 Na asigi dawa: suga na da Hina Gode Ea Dio nodone gaguia gadosa. Na da Ea asaboi asigi hou, amo hame gogolemu.
Tamanda Yehova, iwe moyo wanga, ndipo usayiwale zabwino zake zonse.
3 E da na wadela: i hou huluane gogolema: ne olofosa. Amola na olo huluane uhinisisa.
Amene amakhululuka machimo ako onse ndi kuchiritsa nthenda zako zonse,
4 E da na bogosa: besa: le gaga: sa. E da nama asigiba: le amola nama gogolema: ne olofosu iabeba: le, na da hahawane bagade.
amene awombola moyo wako ku dzenje ndi kukuveka chikondi ndi chifundo chake ngati chipewa chaufumu,
5 E da liligi noga: idafa nama baligili iaha. Amaiba: le, na da buhiba agoai gasa bagade ayeligiwane esalumu.
amene akwaniritsa zokhumba zako ndi zinthu zabwino, kotero kuti umakhala wamphamvu zatsopano ngati mphungu.
6 Hina Gode da enoga banenesi dunu ilima asigiba: le, ilima moloidafa fofada: su hamosa, amola ilima ilia hamobe defele bidi iaha.
Yehova amachita chilungamo ndipo amaweruza molungama onse opsinjika.
7 E da Ea hamomusa: ilegei amo Mousesema olelei. Amola Ea gasa bagade hamobe hou amo Isala: ili fi dunuma olelei.
Iye anadziwitsa Mose njira zake, ntchito zake kwa Aisraeli.
8 Hina Gode da bagadewane asigisa, amola gogolema: ne olofosu hou dawa: E da hedolo hame ougisa. Be E da mae fisili, asigilala.
Yehova ndi wachifundo ndi wokoma mtima, wosakwiya msanga ndi wachikondi chochuluka.
9 E da gagabole sia: sa, be gebewane hame sia: nana. E da wadela: i hou amoma ougili higasa. Be gebewane ougi hame diala.
Iye sadzatsutsa nthawi zonse, kapena kusunga mkwiyo wake kwamuyaya;
10 E da ninia wadela: i hou hamobe amo defele, ninima se dabe hame iaha.
satichitira molingana ndi machimo athu, kapena kutibwezera molingana ndi mphulupulu zathu.
11 Mu amo da osobo bagade badilia gadodafa agoane diala. Amola nowa dunu da Hina Godema nodone dawa: sa, Hina Gode da amo sedade defei defele ilima asigisa.
Pakuti monga kumwamba kuli kutali ndi dziko lapansi, koteronso chikondi chake nʼchachikulu kwa iwo amene amamuopa;
12 Eso mabe gusudili amola eso dabe guma: dini defei, amo defei defele Gode da ninia wadela: i hou hamoi amo ninima fadegale fasisa.
monga kummawa kutalikirana ndi kumadzulo, koteronso Iye watichotsera mphulupulu zathu kuti zikhale kutali nafe.
13 Osobo bagade ada da ea manoma asigibi defele, Gode da Ema nodone dawa: be dunu ilima asigisa.
Monga bambo amachitira chifundo ana ake, choncho Yehova ali ndi chifundo ndi iwo amene amamuopa;
14 E da nini hahamoiba: le, ninia da: i hodo huluane dawa: Nini da osoboga hamoi, amo Hi dawa:
pakuti Iye amadziwa momwe tinawumbidwira, amakumbukira kuti ndife fumbi.
15 Be ninia esalusu da gisi agoai. Ninia da hame nasu sogea agoai heda: le, falegasa.
Kunena za munthu, masiku ake ali ngati udzu, amaphuka ngati duwa la mʼmunda;
16 Amasea, fo da fulabosea, sogea da mini asi dagoi ba: sa. Amola bu hame ba: mu.
koma mphepo imawombapo ndipo silionekanso ndipo malo ake sakumbukirikanso.
17 Be dunu amo da Hina Godema nodone dawa: be, ilia da Ea asigidafa hou eso huluane ba: lalumu. Amola fa: no fifi manebe dunu huluane, amo da Ea Gousa: su hamoi, amola Ea hamoma: ne sia: i, amoma mae fisili fa: no bobogelalebe, ilia da Ea noga: idafa hou ba: lalumu.
Koma kuchokera muyaya mpaka muyaya chikondi cha Yehova chili ndi iwo amene amamuopa, ndi chilungamo chake chili ndi ana a ana awo;
iwo amene amasunga pangano lake ndi kukumbukira kumvera malangizo ake.
19 Hina Gode da Ea Fisu Hebene ganodini ligisi. E liligi huluanedafa amoma Hina Bagadedafa.
Yehova wakhazikitsa mpando wake waufumu mmwamba ndipo ufumu wake umalamulira onse.
20 Dilia gasa bagade a: igele dunu, amo da Ea hamoma: ne sia: be nabawane hamosa! Hina Godema nodoma!
Tamandani Yehova, inu angelo ake, amphamvu inu amene mumachita zimene amalamula, amene mumamvera mawu ake.
21 Dilia Hebene ganodini esalebe hawa: hamosu dunu, amo da Hina Gode Ea hanai defele hamosa! Hina Godema nodoma!
Tamandani Yehova, zolengedwa zonse zakumwamba, inu atumiki ake amene mumachita chifuniro chake.
22 Hina Gode Ea hahamoi esalebe liligi huluane, amo da Ea ouligibi soge huluane amo ganodini esalebe! Dilia Hina Godema nodoma! Na asigi dawa: su! Hina Godema nodoma!
Tamandani Yehova, ntchito yake yonse kulikonse mu ulamuliro wake. Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.

< Gesami Hea:su 103 >