< Malasu 4 >

1 Nagofelali! Dilia ada adi olelesea noga: le nabima! Amasea dili da Bagade Dawa: su Hou ida: iwane gala dawa: mu.
Ananu, mverani malangizo a abambo anu; tcherani khutu kuti mupeze nzeru zodziwira zinthu.
2 Na adi olelebe amo da moloi houdafa. Amaiba: le, dili da eso huluane dawa: laloma.
Zimene ndikukuphunzitsani ndi zabwino. Choncho musasiye malangizo anga.
3 Amola na mano fonobahadiga na da na ada ea mano afadafa galu.
Paja ndinalinso mwana mʼnyumba mwa abambo anga; mwana mmodzi yekha wapamtima pa amayi anga.
4 Amola na ada e da nama moloidafa hou olelesu. E da amane sia: su, “Dawa: ma! Amola na sia: mae gogolema amola na sia: defele hamoma. Amasea, dili da esalusu lamu.
Ndipo abambo anandiphunzitsa ndi mawu akuti, “Ugwiritse mawu anga pa mtima pako, usunge malamulo anga kuti ukhale ndi moyo.
5 Bagade Dawa: su Hou hogoi helema. Na sia: mae gogolema amola mae higama!
Upeze nzeru, upeze nzeru zomvetsa zinthu; usayiwale mawu anga kapena kutayana nawo.
6 Dili da Bagade Dawa: su Hou ida: iwane gala amoma mae higama. Amasea, amo hou da dilia gaga: su agoane ba: mu. Bagade Dawa: su Hou asigiwane ba: ma. Amasea, amo hou da dili gaga: mu.
Usasiye nzeru ndipo idzakusunga. Uziyikonda ndipo idzakuteteza.
7 Amola Bagade Dawa: su Hou lamu amo hou da ida: iwanedafa gala. Amola liligi oda amoga Bagade Dawa: su Hou da baligi dagoi.
Fundo yayikulu pa za nzeru ndi iyi: upeze nzeru. Kaya pali china chilichonse chimene ungapeze, koma upeze nzeru yomvetsa bwino zinthu.
8 Bagade Dawa: su Hou amoma hanama amola amane hou hamosea, dili da dunu hahawanedafa esalumu amola asigi dawa: su bagade dawa: su lamu.
Uyilemekeze nzeruyo ndipo idzakukweza; ikumbatire nzeruyo ndipo idzakupatsa ulemu.
9 Amo Bagade Dawa: su Hou da dunu huluane ba: ma: ne hamoma, amo hou ida: iwane gala amo ea dilia hou bagade dawa: su ba: mu.
Idzayika sangamutu yokongola yamaluwa pamutu pako; idzakupatsa chipewa chaufumu chaulemu.”
10 Nagofe! Noga: le nabima amola dafawane sia: sa noga: le lalegaguma. Amasea di da osobo bagadega fifi masunu.
Mwana wanga, umvere ndi kuvomereza zimene ndikunena, ndipo zaka za moyo wako zidzakhala zochuluka.
11 Na Bagade Dawa: su Hou olelei amo noga: le dawa: ma. Amasea, di da fifi asi helemu amo logo ganodini.
Ndakuphunzitsa njira yake ya nzeru. Ndakutsogolera mʼnjira zolungama.
12 Dima eno hou hame doaga: mu di moloi ahoanea da. Amola dia hehenasea da hame dafamu.
Pamene ukuyenda, mapazi ako sadzawombana; ukamadzathamanga, sudzapunthwa.
13 Eso huluane dima hou olelei amoma dawa: ma amola amo da maedafa gogolema amoga dia esalalasu fidimu amola noga: le ouligima.
Ugwiritse zimene ndikukuphunzitsazi osazitaya ayi. Uwasamale bwino pakuti moyo wako wagona pamenepa.
14 Wadela: le hamosu dunu ilia ahoabe amoga mae masa. Amola wadela: le hamosu dunu ilia hou amoga mae lama.
Usayende mʼnjira za anthu oyipa kapena kuyenda mʼnjira ya anthu ochimwa.
15 Amane mae hamoma wadela: i hou amoma gasigama. Amola amoma higale amola dia moloi logoga masa.
Pewa njira zawo, usayende mʼmenemo; uzilambalala nʼkumangopita.
16 Wadela: le hamosu dunu ilia da wadela: le hame hamosea, hamedafa golasa. Ilia da wadela: le hamomusa: nedigili ouesala amola eno dunuma wadela: le hamonanu fawane golasa.
Pakuti iwo sagona mpaka atachita zoyipa; tulo salipeza mpaka atapunthwitsa munthu wina.
17 Wadela: i hou amola gegesu hou da ilia ha: i manu amola hano nasu agoai gala.
Paja chakudya chawo ndicho kuchita zoyipa basi ndipo chakumwa chawo ndi chiwawa.
18 Moloidafa dunu ilia logo da eso mabe defele ba: sa, hahawane bagade. Amola hadigi da misini, dialea, eso dogoa defele ba: sa.
Koma njira ya anthu olungama ili ngati kuwala kwa mʼbandakucha kumene kumanka kuwalirawalira mpaka dzuwa litafika pa mutu.
19 Be wadela: le hamosu dunu ilia logo da gasi bagade ba: sa amola hedolo dafasa amola ili soi amo da ili hame ba: sa.
Koma njira ya anthu oyipa ili ngati mdima wandiweyani; iwo sadziwa chomwe chimawapunthwitsa.
20 Nagofe! Na sia: dia noga: le nabima.
Mwana wanga, mvetsetsa zimene ndikunena; tchera khutu ku mawu anga.
21 Amo dia maedafa gogolema, eso huluane dawa: loma, dia dogo ganodini.
Usayiwale malangizo angawa, koma uwasunge mu mtima mwako.
22 Na sia: da nowa dunu da amo noga: le dawa: sea, amo da esalusu imunu, amola ea da: i fidimu.
Pakuti amapatsa moyo kwa aliyense amene awapeza ndipo amachiritsa thupi lake lonse.
23 Dawa: ma! Dia asigiga dawa: su noga: le ouligima. Bai dia esalusu da dia asigi dawa: su dawa: i liligi amo defele ba: mu.
Ndipotu mtima wako uziwuyangʼanira bwino ndithu pakuti ndiwo magwero a moyo.
24 Sia: dafawane hame, ogogole maedafa sia: ma. Amola ogogosu hou amoma mae gilisima.
Usiyiretu kuyankhula zokhotakhota; ndipo ulekeretu kuyankhula zinthu zonyansa.
25 Mae beda: iwane molole ba: le gusuma! Dia da hou moloiwane hamobeba: le, dia dialuma da gogosiane fili sa: imu da defea hame.
Maso ako ayangʼane patsogolo; uziyangʼana kutsogolo molunjika.
26 Dia adi hamosea, noga: le dawa: lu hamoma amola adi hou dia hamobe amo da bu sinidigili hahawane ba: mu.
Uzilingalira bwino kumene kupita mapazi ako ndipo njira zako zonse zidzakhala zosakayikitsa.
27 Wadela: i hou dawa: ma! Moloiwane ahoanoma! Amola sadena: ne dafasa: besa: le dawa: ma.
Usapatukire kumanja kapena kumanzere; usapite kumene kuli zoyipa.

< Malasu 4 >