< Malasu 28 >

1 Wadela: i hamosu dunu da dunu eno ili hame sefasibi amomane hobeasa. Be moloidafa dunu da laione wa: me agoane hame beda: sa.
Munthu woyipa amathawa ngakhale palibe wina womuthamangitsa, koma wolungama ndi wolimba mtima ngati mkango.
2 Fifi asi gala da wadela: le hamosea, ilia hina bagade da mae aligili hedolo afafadenesa. Be molole dawa: su hina bagade da fifi asi gala noga: le ouligisia, ilia da gasalawane esalumu.
Pamene mʼdziko muli kuwukirana, dzikolo limakhala ndi olamulira ambiri, koma anthu omvetsa ndi odziwa zinthu bwino ndiwo angakhazikitse bata mʼdzikolo nthawi yayitali.
3 Gibu da foga oule masea, ha: i manu sagai da muagia: sa. Amo defele, nimi bagade ouligisu dunu da hame gagui dunu wadela: sa.
Munthu wosauka amene amapondereza osauka anzake ali ngati mvula yamkuntho imene imawononga mbewu mʼmunda.
4 Di da sema nabawane hame hamosea, di da wadela: le hamosu dunu amolalimagale hamosa. Be di da noga: le nabasea, di da amolalima hame gasa.
Amene amakana malamulo amatamanda anthu oyipa, koma amene amasunga malamulo amatsutsana nawo.
5 Wadela: le hamosu dunu da moloidafa fofada: su hou hame dawa: Be nowa da Hina Godema nodone sia: ne gadosea, da amo hou noga: le dawa:
Anthu oyipa samvetsa za chiweruzo cholungama, koma amene amafuna kuchita zimene Yehova afuna amachimvetsetsa bwino.
6 Di da liligi hame gaguiwane, be moloidafa hou hamonanumu da defea. Be bagade gaguiwane, be moloi hame hamosa esalumu da defea hame.
Munthu wosauka wa makhalidwe abwino aposa munthu wolemera wa makhalidwe okhotakhota.
7 Goi ayeligi da sema noga: le nabasea da bagade dawa: su dunu agoai esala. Be dunu da wiwili gala: su dunu ilima gilisisia, da ea edama gogosiasu iaha.
Amene amasunga malamulo ndi mwana wozindikira zinthu, koma amene amayenda ndi anthu adyera amachititsa manyazi abambo ake.
8 Dia da muni molole hame lasea, o dabua baligili legebeba: le, bagade gagui ba: sea, fa: no dia muni huluane da fisi dagoi ba: mu. Haeafui dunu da amo muni lale, hame gagui dunuma imunu.
Amene amachulukitsa chuma chake polandira chiwongoladzanja chochuluka amakundikira chumacho anthu ena, amene adzachitira chifundo anthu osauka.
9 Di da Gode Ea sema higasea, Gode da dia sia: ne gadosu nabimu amola higamu.
Wokana kumvera malamulo ngakhale pemphero lake lomwe limamunyansa Yehova.
10 Di da moloidafa dunuma ogogobeba: le, e da wadela: le hamosea, amo da sani agoane. Be di da dina: saniga sa: imu. Be Gode da moloidafa dunuma bidi imunu.
Amene amatsogolera anthu olungama kuti ayende mʼnjira yoyipa adzagwera mu msampha wake womwe, koma anthu opanda cholakwa adzalandira cholowa chabwino.
11 Liligi bagade gagui dunu da gasa fili, ili da noga: i dawa: su bagadeyale ilila: dawa: lala. Be liligi hame gagui molole dawa: su dunu, ilia liligi bagade gagui dunu ilia giadofabe asigi dawa: su hou noga: le dawa:
Munthu wolemera amadziyesa kuti ndi wanzeru, koma munthu wosauka amene ali ndi nzeru zodziwa zinthu amamutulukira.
12 Moloidafa dunu da ouligisu hou lasea, dunu huluane da nodone gilisili ha: i naha. Be wadela: le hamosu dunu da ouligisu hou lasea, eno dunu da hobeale wamoaligisa.
Pamene olungama apambana pamakhala chikondwerero chachikulu; koma pamene anthu oyipa apatsidwa ulamuliro, anthu amabisala.
13 Di da dia wadela: i hamoi amo wamolegesea, di da hahawane hame esalumu. Be dia wadela: i hou amo fofada: ne, sinidigisia, Gode da dima gogolema: ne olofomu.
Wobisa machimo ake sadzaona mwayi, koma aliyense amene awulula ndi kuleka machimowo, adzalandira chifundo.
14 Eso huluane Hina Godema nabasu hou hamosea, di da hahawane ba: mu. Be di da hihini gasa fili hamosea, dia hou da wadela: lesi dagoi ba: mu.
Ndi wodala munthu amene amaopa Yehova nthawi zonse, koma amene aumitsa mtima wake adzagwa mʼmavuto.
15 Wadela: le hamosu ouligisu dunu da nimi bagade gesenenanebe laione wa: me o gogoli ahoanebe ‘bea’ agoane. Agoaiwane dunu da dunu fi ouligisia, hame gagui dunu da gasa hameba: le, se nabala.
Ngati mkango wobuma kapena chimbalangondo cholusa ndi mmenenso amakhalira munthu woyipa akamalamulira anthu osauka.
16 Ouligisu dunu da dawa: su noga: i hame galea, e da ea fi ilima gasa fili, nimi bagadewane ouligimu. Be moloidafa ouligisu dunu da ode bagohame ea fi ouligimu.
Wolamulira amene samvetsa zinthu ndiye amakhala wankhanza koma amene amadana ndi phindu lopeza mwachinyengo adzakhala ndi moyo wautali.
17 Nowa dunu da fane legesu hou hamosea, e da fedege agoane hina: bogoi uli dogosa. Amaiba: le, amo logo di mae hedofama.
Munthu amene wapalamula mlandu wopha munthu adzakhala wothawathawa mpaka imfa yake; wina aliyense asamuthandize.
18 Di da moloidafa hou hamosea, dia esalusu da gaga: i dagoi ba: mu. Be di da hou moloi hame hamosea, hedolo dafamu.
Amene amayenda mokhulupirika adzapulumutsidwa koma amene njira zake ndi zokhotakhota adzagwa mʼdzenje.
19 Dogolole bugili nasu dunu da ha: i manu gilisi ba: sa. Be dunu da mae hawa: hamone, udigili esalea, ha: bagade ba: mu.
Amene amalima mʼmunda mwake adzakhala ndi chakudya chochuluka, koma amene amangosewera adzakhala mʼmphawi.
20 Moloidafa dunu da hahawane ganumu. Be nowa da hedolodafa bagade gaguiwane esalomusa: dawa: sea da se dabe iasu ba: mu.
Munthu wokhulupirika adzadalitsika kwambiri, koma wofuna kulemera mofulumira adzalangidwa.
21 Afamagasu hou da wadela: idafa. Be wadela: i fofada: su dunu da hano suligisu lasea, hedolowane afamagasa.
Kukondera si kwabwino, ena amachita zolakwazo chifukwa cha kachidutswa ka buledi.
22 Uasu dunu da hedolowane liligi bagade lamusa: dawa: beba: le, e da fa: no liligi hame gaguiwane esalumu amo hi hame dawa: sa.
Munthu wowumira amafunitsitsa kulemera koma sazindikira kuti umphawi udzamugwera.
23 Mae wamolegele, hima hou hahamoma: ne gagabole odagia sia: mu da defea. Agoane hame hamosea, di da ema hame asigisa. E da se lamu be fa: no amo sia: da dabua hahaeafuli sia: baligisa dawa: mu.
Amene amadzudzula mnzake potsiriza pake mnzakeyo adzamukonda kwambiri, kupambana amene amanena mawu oshashalika.
24 Nowa dunu da ea ada amola ame amo elea liligi wamolasea, amo ea hou da gugunufinisisu dunu ea hou defele gala.
Amene amabera abambo ake kapena amayi ake namanena kuti “kumeneko sikulakwa,” ndi mnzake wa munthu amene amasakaza.
25 Uasu hou hamosea, fa: no bidi doaga: mu. Be di da Hina Godema dafawaneyale dawa: mu da defea.
Munthu wadyera amayambitsa mikangano, koma amene amadalira Yehova adzalemera.
26 Di da dia hanai amoga fawane fa: no bobogesea, amo da gagaoui hou agoai galebe. Be noga: le dawa: su dunu ilia olelesuma fa: no bobogesea, di da gaga: i ba: mu.
Amene amadzidalira yekha ndi chitsiru, koma amene amatsata nzeru za ena adzapulumuka.
27 Dia liligi amo hame gagui dunu iligili iasea, di da eso huluane dia esaloma: ne lamu liligi defele ganabe ba: mu. Be di da hame gagui dunu, ilima hame asigi agoai lalea, dunu bagohame ilia da di gagabui aligima: ne sia: mu.
Amene amapereka kwa osauka sadzasowa kanthu, koma amene amatsinzina maso ake adzatembereredwa kwambiri.
28 Wadela: le hamosu dunu da ouligisu hou lasea, ea fi dunu da ilia wamo aligisu soge hame yolesisa. Be wadela: le ouligisu dunu da dafasea, moloidafa dunu da ilia fi bu ouligimu.
Pamene anthu oyipa apatsidwa ulamuliro anthu amabisala, koma anthu oyipa akawonongeka olungama amapeza bwino.

< Malasu 28 >