< Nihemaia 6 >
1 Sa: naba: la: de, Doubaia, Giseme amola eno ninima ha lai dunu ilia nabi da moilai gagoi da gagole dagoi amola gelabo afae hamedafa gala. Be ninia logo ga: su amo logo holeiga hame sagai.
Pamenepo Sanibalati, Tobiya, Gesemu Mwarabu ndi adani athu anamva kuti ndatsiriza ntchito yomanganso khoma ndi kuti palibe mpata umene watsala ngakhale kuti pa nthawi imeneyi ndinali ndisanayike zitseko pa zipata.
2 Amaiba: le, Sa: naba: la: de amola Giseme ela da nama sia: adole iasi. Amo da na da ela amola sia: sa: imusa: , ilia moilai afae Ounou Umi ganodini dialu amoga misa: ne sia: i. Be ilia da na fane legemusa: ogogole misa: ne sia: i.
Sanibalati ndi Gesemu, ananditumizira uthenga uwu: “Bwerani tidzakumane pa mudzi wina ku chigwa cha Ono.” Koma iwo anakonzekera kuti akandichite chiwembu kumeneko.
3 Na da ilima sia: alofele ia ahoasu dunu asunasili, ilima amane sia: i, “Na da hawa: hamosu bagadedafa hamonana. Na da dia sogega gudu sa: imu da hamedei. Na da dilima misa: ne, hawa: hamosu fisimu da noga: i hame galebe,” na sia: i.
Choncho ine ndinatuma amithenga ndi yankho ili: “Ine ndikugwira ntchito yayikulu kuno ndipo sindingathe kubwera kumeneko. Kodi ntchito iyime pofuna kuti ndibwere kumeneko?”
4 Ilia da amo sia: eso biyaduyale agoane adole guda: beba: le, na da ilima na musa: sia: i defele adole ia gudui.
Ananditumizira uthenga umodzimodzi omwewu kanayi ndipo ndinawayankha chimodzimodzi.
5 Amalalu, Sa: naba: la: de da ea sia: biyale amo nama adosi. Amo sia: da meloa dedei, gobele legesu amoga hame ga: su. Ea hawa: hamosu dunu afae da amo meloa dedei nama gaguli misi.
Tsono kachisanu, Sanibalati anatumiza wantchito wake ndi kalata yosamata.
6 Sia: dedei da agoane ba: i, “Na da Sa: naba: la: de. Giseme da nama adoi amo na: iyado dunu fi da di amola Yu fi dunu da Besia eagene amo fisimusa: dawa: sa, amola di fawane da eagene ouligisu dunu aligimusa: dawa: , na: iyado dunu fi da amane sia: daha.
Mu kalatamo munali mawu akuti, “Pali mphekesera pakati pa mitundu ya anthu, ndiponso Gesemu akunena zomwezo kuti inu ndi Ayuda onse mufuna kuwukira boma. Nʼchifukwa chake mukumanga khoma. Mphekeserazo zikutinso inu mukufuna kudzakhala mfumu yawo.
7 Ilia eno sia: daha amane, di da balofede (Gode Sia: alofesu dunu) ilima ilia da Yelusaleme moilai amo ganodini di da Yuda hina bagade hamoi dagoi, amo sia: ma: ne sia: i. Besia hina bagade da amo sia: nabimu. Amaiba: le, di amola na da amo sia: sa: imusa: , gilisimu da defea,” e amane dedei.
Mwayikanso kale aneneri amene adzalengeza za iwe mu Yerusalemu kuti ‘Mu Yuda muli mfumu!’ Tsono nkhani iyi imveka ndithu kwa mfumu. Choncho bwerani kuti tidzakambirane.”
8 Na da ema bu dedene i, amane, “Sia: dia meloa dedene i amo huluane da ogogosa. Amo sia: da di fawane lafia lale sia: i galebe.”
Ine ndinatumiza yankho ili: “Pa zimene mukunenazo, palibe chimene chinachitikapo. Inu mukungozipeka mʼmutu mwanu.”
9 Ilia da nini beda: ma: ne, amola hawa: hamosu yolema: ne, amo hou hamoi. Be na Godema sia: ne gadobeba: le, Gode da nama gasa i.
Apa adani athu onsewa ankangofuna kutiopseza. Iwo ankaganiza kuti “Tichita mantha ndi kuleka kugwira ntchito.” Tsono ndinapemphera kuti, “Inu Mulungu ndilimbitseni mtima.”
10 Amo esoga, na da Siema: iya (Dila: iya egefe amola Mehedabele ea aowa) amo ba: musa: asi. Bai e da ea diasu fisili gadili masunu da hamedei galu. E da nama amane sia: i, “Di amola na ania da Hadigi Malei Sesei amo Debolo diasu ganodini heda: le, logo ga: sili wamoaligimu. Bai dilima ha lai da di fane legemusa: , udigili gasia misini fane legemu.”
Tsiku lina ndinapita ku nyumba ya Semaya mwana wa Delaya mwana wa Mehatabeli. Tsono anandiwuza kuti, “Tiyeni tikakumanire ku Nyumba ya Mulungu. Tikabisale mʼmenemo ndi kutseka zitseko chifukwa akubwera kudzakuphani. Ndithu usiku uno akubwera kudzakuphani.”
11 Na da ema bu adole i, “Na da dunu amo da hobeale, wamoaligisa, agoai dunu hame. Na mae medole legema: ne amola na esalusu mae fisima: ne, na da Debolo diasua wamo aligima: ne dawa: bela: , dia da na wamo aligima: beale dawa: bela: ? Hame mabu! Na da amane hame hamomu!”
Koma ndinayankha kuti, “Kodi munthu ngati ine nʼkuthawa? Kapena munthu wofanana ndi ine nʼkupita ku Nyumba ya Mulungu kuti apulumutse moyo wake? Ayi, ine sindipita!”
12 Amo sia: na da bu dadawa: loba, na amane dawa: i. Gode da Siema: iyama hame adoi. Be Doubaia amola Sa: naba: la: de ela da amo sia: adoma: ne ema muni i.
Ndinazindikira kuti Mulungu sanamutume koma kuti anayankhula mawu oloserawa motsutsana nane chifukwa Tobiya ndi Sanibalati anamulemba ntchitoyi.
13 Ilia da na amo sia: nabaloba, beda: iba: le wadela: i hamomu, ilia da dawa: i galu. Amola na dio wadela: lesi dagoi ba: mu, amola na da bagadewane gogosiamu, ilia dawa: i galu.
Iye analembedwa ntchitoyi ndi cholinga choti ine ndichite mantha, ndithawe. Ndikanatero ndiye kuti ndikanachimwira Yehova ndiponso iwowo akanandiyipitsira mbiri yanga ndi kumandinyoza.
14 Na da Godema sia: ne gadoi, amane, “Gode dawa: ma! Doubaia amola Sa: naba: la: de elea hou dawa: le, elama se dabe bagade ima. Amola uda Nouadaia amola ogogosu balofede dunu eno da na beda: ma: ne hamoi, amo huluane ilima se dabe bagade ima,” na amane sia: ne gadoi.
Tsono ndinapemphera kuti, “Inu Mulungu wanga, kumbukirani Tobiya ndi Sanibalati chifukwa cha zimene achita. Kumbukiraninso mneneri wamkazi Nowadiya ndi aneneri amene akhala akufuna kundiopseza.”
15 Ninia da eso 52 amoga hawa: hamonanu, musa: mugului gagoi da bu gagoi dagoi ba: i. Dagosu eso da eso 25 amo oubi ea dio Eloule amoga ba: i.
Ndipo khoma linatsirizidwa kumanga pa tsiku la 25 la mwezi wa Eluli. Linamangidwa pa masiku okwana 52.
16 Amola ninia ha lai dunu, na: iyado gadenene ga fi amo ganodini esalu, ilia amo sia: naba: beba: le gogosia: i. Bai dunu huluane, Gode da amo gagoi hawa: hamosu fidibiba: le dagoi, dunu hulu da dawa: i galu.
Adani athu onse atamva izi, mitundu yonse ya anthu yozungulira inachita mantha ndi kuchita manyazi. Iwo anazindikira kuti ntchitoyo inachitika ndi thandizo la Mulungu wathu.
17 Be hawa: hamosu eso huluane amoga, Yu ouligisu dunu mogili da Doubaiama meloa dedene iasu.
Komanso masiku amenewo anthu olemekezeka a ku Yuda ankalemberana naye makalata ambiri ndi Tobiyayo,
18 Dunu bagohame Yuda soge ganodini da Doubaia fuligala: su. Bai esoa: amo Sieganaia (A: ila egefe) da Yu dunudafa. Amola bai eno da Doubaia egefe Youha: ina: ne da Misiala: me (Belegaia egefe) amo ea idiwi lai dagoi.
pakuti anthu ambiri a ku Yuda anali atalumbira kale kuti adzagwira naye ntchito popeza anali mkamwini wa Sekaniya mwana wa Ara, ndipo mwana wake Yehohanani anakwatira mwana wamkazi wa Mesulamu mwana wa Berekiya.
19 Dunu mogili da na nabima: ne, Doubaia ea fidisu hou ida: iwane hamobe, sia: dalu. Amola na sia: i liligi huluane, ilia da ema bu sia: su. Amola, e da na beda: ma: ne, eso huluane nama dedene iasu.
Kuwonjezera apo, anthu ankasimba za ntchito zake zabwino ine ndili pomwepo ndipo anakamuwululira mawu anga. Choncho Tobiyayo ankatumiza makalata ondiopseza.