< Nihemaia 5 >

1 Fa: no, eso afaega, dunu amola uda bagohame da ilia Yu na: iyado dunu ilima ougili fofada: su.
Tsono anthu ena ndi akazi awo anayamba kudandaula kwambiri chifukwa cha Ayuda anzawo.
2 Mogili da amane sia: i, “Ninia da sosogo fi bagade. Amaiba: le, ninima ha: i manu gagoma moma: ne imunu da defea.”
Ena ankanena kuti, “Ife ndi ana athu aamuna ndi aakazi, tilipo ochuluka kwambiri. Choncho tikufuna tirigu kuti tidye ndi kukhala ndi moyo.”
3 Eno mogili da amane sia: i, “Ninia da ha: i mae nawene bogosa: besa: le, ninia ifabi, waini sagai amola gagoma bidi lama: ne, amoga ninia eno dunuma muni lai. Be amo muni lai fa: no dabema: ne iasu dabe hame iasea, ilia da ninia ifabi amola waini sagai huluane samogemu.”
Panali ena amene ankanena kuti, “Ife tikuchita kupereka minda yathu, mitengo yathu ya mphesa ndi nyumba zathu ngati chikole kuti tipeze tirigu chifukwa njala yakula.”
4 Eno mogili da amane sia: i, “Ninia da eagene soge su (da: gisi) ima: ne muni hame gala. Amaiba: le, amo muni ima: ne, ninia da eno dunu amoga muni amo fa: no dabe ima: ne, ilima lai.
Panalinso ena amene ankanena kuti, “ife tinachita kukongola ndalama zoti tipereke msonkho wa minda ndi mitengo yathu ya mphesa kwa mfumu.
5 Ninia amola da Yu dunudafa. Ninia mano da eno Yu dunu ilia mano defele esala. Be ninia da muni hameba: le, ninia mano da udigili se dabe hawa: hamoma: ne, ninia da enoma bidi lasa. Ninia uda mano mogili amo ninia bidi lai dagoi. Ninia ifabi amola waini sagai da ilia samogeiba: le, ninia da gasa hame ba: sa.”
Ngakhale kuti ndife amodzi ndi abale athuwa, ndipo ngakhalenso ana athu ndi ofanana ndi ana awo, ife tikukakamiza ana athu kuti akhale akapolo. Ena mwa ana athu aakazi atengedwa kale ukapolo. Ife tilibe mphamvu yochitapo kanthu popeza anthu ena anatenga kale minda yathu ndi mitengo yathu ya mphesa.”
6 Na da ilia sia: gesu nababeba: le, ougi bagade ba: i.
Nditamva madandawulo awo ndi zimene amanenazi ndinapsa mtima kwambiri.
7 Na da amo hou hahamomusa: ilegei. Na da dunu fi ouligisu hina dunu amola ouligisu dunu eno ilima gagabole sia: i, “Dilia da dilia diolalali amo banenesilala,” na amane sia: i. Na da dunu huluane amo hou sia: sa: imusa: gilisima: ne sia: i.
Nditalingalira bwino ndinatsimikiza zoti ndichitepo kanthu ndipo kenaka ndinawadzudzula anthu olemekezeka ndi akuluakuluwo. Ndinawawuza kuti, “Zoona ndithu inu nʼkumalipiritsana chiwongoladzanja chachikulu anthu apachibale nokhanokha!” Choncho ndinayitanitsa msonkhano waukulu kuti ndiwazenge mlandu
8 Na da amane sia: i, “Musa: ninia olalali Yu fi da muni hameba: le, ilisu da ilia da: i hodo amo ga fi dunuma bidi lasu. Be ninia da wali ninia gasa defele, amo dunu bu bidilala. Be wali dilia ouligisu dunu da hame gagui dunu banenesibiba: le, dilia Yu yolalali da ilisu ga fi dunuma hame, be eno Yu dunuma ilia da: i hodo udigili se dabe hawa: hamoma: ne bidi lasa,” na amane gagabole sia: i. Yu ouligisu dunu ilia bu adole imunu gogoleiba: le, ouiya: i.
ndipo ndinati, “Monga zakhaliramu ife tikutha kuwombola abale anthu amene anagulitsidwa ukapolo kwa anthu ena. Kodi tsopano inu mukugulitsanso abale anu kwa anzawo kuti ife tiwumirizidwe kuwawombola?” Iwo anakhala chete, chifukwa sanapeze mawu oti anene.
9 Amalalu, na amane sia: i, “Dilia hou wali hamosu da wadela: i. Dilia Gode Ea sia: nabimu amola moloidafa hou hamomu da defea galu. Amasea, ninima ha lai Dienadaile dunu, ninima oufesega: ma: ne bai hame ba: mu galu.
Kotero ndinapitiriza kunena kuti, “Zimene mukuchitazi si zabwino. Kodi inu simungakhale ndi moyo woopa Mulungu wathu kuti tipewe kunyoza kwa adani athu, anthu a mitunda inayi?
10 Na da eno dunuma muni amola gagoma amo fa: no dabe bu hame lama: ne i dagoi. Amola na sama amola gilisili hawa: hamosu dunu da amo defele hamoi. Na hanai da ninia bu fa: no dabe lama: ne sia: su yolemu.
Ine ndi abale anga ndiponso antchito anga tikuwakongozanso anthuwa ndalama ndi tirigu. Ndipo tiyeni tilekeretu zolandira chiwongoladzanja!
11 Ilia da dilima dabe imunu hou-amo muni o gagoma o waini o olife susuligi-amo huluane yolesima. Amola ilia liligi dabe dilia lai huluane ilima bu ima. Wahadafa amo ifabi, waini sagai, olife ifa sagai amola diasu huluane ilima bu ima,” na sia: i.
Abwezereni lero lomwe minda yawo, mitengo ya mphesa, mitengo ya olivi ndiponso nyumba zawo. Muwabwezerenso chiwongoladzanja cha ndalama, tirigu, vinyo ndi mafuta zimene munatenga.”
12 Ouligisu dunu ilia bu adole i, “Defea! Dia sia: ninia nabi dagoi. Ninia da liligi lai bu ianu, dabe lamu galea amo dabe hame lamu.” Na da gobele salasu dunu misa: ne sia: i. Amola gobele salasu dunu ba: ma: ne, ouligisu dunu da amo hou dafawane hamoma: ne, Hina Gode Ea Dio: ba: le ilegele sia: musa: , na da sia: i.
Iwo anayankha kuti, “Ife tidzawabwezera zimenezi popanda kupemphapo kanthu kalikonse kwa iwo. Tidzachita monga mwanena.” Pambuyo pake ndinayitanitsa ansembe ndipo pamaso pawo ndinawalumbiritsa atsogoleriwo ndi akuluakuluwo kuti adzachitadi zomwe analonjezazo.
13 Amalalu, na da abula beano fonobahadi buluyale idinigi amo fadegale fasili, duduli fasi. Na da amane sia: i, “Nowa dunu da ea dafawane waha sia: i liligi hame hamosea, Gode da amo defele duduli fasimu. Gode da dilia diasu amola dilia gagui liligi huluane samogele, dilia da da: i nabado agoane ba: mu,” na amane sia: i. Dunu huluane gilisili esalu da “Ama” sia: i amola Godema nodoi. Amola Yu ouligisu dunu da ilia dafawane ilegele sia: i defele hamosu.
Ndipo inenso ndinakutumula chovala changa ndi kuti, “Chimodzimodzinso Mulungu akutumule munthu wosasunga malonjezano ake. Amulande nyumba yake ndi katundu wake ndi kumusandutsa mʼmphawi!” Apo msonkhano wonse unati, “Ameni” natamanda Yehova. Ndipo anthu aja anachita monga analonjezera.
14 Ode fagoyale gala, amo da Adasegesisi da Besia sogega hina bagade esalu ea ouligisu hou da ode 20 gidigi amo ode mui asili Adasegesisi ea ouligisu ode 32 gidigi, ode fagoyale amoga na da Yu sogega eagene ouligisudafa dunu esalu. Na amola na sosogo fi da ha: i manu amo eagene ouligisu ilima ilegei, amo manu da defea galu. Be ninia da hame nasu.
Ndiponso kuyambira nthawi imene anandisankha kuti ndikhale bwanamkubwa wa dziko la Yuda, kuchokera chaka cha makumi awiri mpaka chaka cha 32 muulamuliro wa ufumu wa Aritasasita, ndiye kuti kwa zaka zokwana 12, ine ngakhale abale anga sitinalandire chakudya choyenerera bwanamkubwa.
15 Eagene ouligisu dunu musa: na mae aligili, ilia hou hamoiba: le, Yu dunu da da: i dioi bagade nabi. Ilia da Yu dunuma eso huluane silifa muni fage 40 agoane ilia ha: i manu amola waini lamusa: edegesu. Ilia hawa: hamosu dunu amola da Yu dunu banenisisu. Be na hou da hisu hamoi. Bai na da Godema nodone fa: no bobogei.
Koma abwanamkubwa akale ankasautsa anthu. Iwo ankalanda anthu chakudya ndi vinyo ndi kuwalipiritsanso masekeli asiliva makumi anayi. Ngakhalenso antchito awo amavutitsa anthu kwambiri. Koma ine sindinachite zimenezo chifukwa ndimaopa Mulungu.
16 Na da gagoi mugului amo bu gagomusa: fawane dawa: i galu. Na da soge lamu hame dawa: i galu. Na hawa: hamosu dunu amola da moilai gagoi fidi.
Ndiponso ndinadzipereka kugwira ntchito yomanga khoma la mzinda wa Yerusalemu popanda ngakhale kugulapo munda. Antchito anganso anasonkhana komweko kuti agwire ntchito ndipo sitinafunenso malo ena.
17 Eso huluane, Yu dunu 150 amola ilia ouligisu dunu da na diasuga ha: i namasu. Amola, ninia na: iyado ga fi dunu bagohame da misini, na diasuga ha: i nasu.
Kuwonjezera apa, ndinkadyetsa Ayuda, akuluakulu kuphatikizanso anthu amene ankabwera kwa ife kuchokera kwa mitundu ya anthu otizungulira okwanira 150.
18 Eso huluane, na da bulamagau afae, sibi noga: idafa gafeyale amola gagala bagohame gobele moma: ne iasu. Be na da dunu ilia da: i diomu amo dawa: beba: le, eagene muni nama ilegei amo hame lasu.
Tsiku lililonse pamaphikidwa ngʼombe imodzi, nkhosa zabwino zisanu ndi imodzi pamodzi ndi nkhuku. Ndipo pakutha pa masiku khumi aliwonse pankakhala matumba achikopa ochuluka a vinyo wa mitundu yonse. Ngakhale zinali choncho, Ine sindinatenge chakudya choperekedwa kwa bwanamkubwa, chifukwa izi zinali zosautsa anthu.
19 Gode! Na da dima sia: ne gadosa. Na da dunu huluane fidima: ne hawa: hamosu amo mae gogolema. Amola nama hahawane ima.
Kuti zinthu zindiyendere bwino, kumbukirani Yehova Mulungu wanga pa zonse zimene ndachitira anthu awa.

< Nihemaia 5 >