< Nihemaia 4 >
1 Sa: naba: la: de da ninia Yu dunu da moilai gagosu gagobe amo nababeba: le, e da ninima ougili bagadewane lasogole oufesega: su.
Sanibalati atamva kuti tikumanganso khoma anapsa mtima nayamba kuseka ndi kunyogodola Ayuda kwambiri.
2 E da ea dogolegei dunu odagiaba, amola Samelia dadi gagui dunu odagiaba, amane sia: i, “Goe Yu hahaninisi dunu da adi hamosala: ? Ilia da moilai bu hahamomusa: dawa: bela: ? Ilia Godema gobele salasu hamobeba: le, eso afae amoga hawa: hamosu dagomusa: dawa: bela: ? Amola, ilia da isu laluga nei amoga diasu gagusu gele noga: i hamomusa: dawa: bela: ?”
Ndipo anayankhula pamaso pa abale ake ndi asilikali a Samariya kuti, “Kodi Ayuda ofowokawa akuchita chiyani? Kodi iwo nʼkumanganso khoma? Kodi adzaperekanso nsembe? Kodi adzatsiriza ntchitoyi tsiku limodzi? Kodi adzachita kutenga miyala yakale ija ndi mmene inapseramo?”
3 Doubaia amola da Sa: naba: la: de dafulili lelu. E amane sia: i, “Mae dawa: ma! Ilia gagoi noga: i gagomu da hamedei! Fogisi fonobahadi da ilia gagoi amo fuli fasimusa: defele ba: mu,” e oufesega: ne amane sia: i.
Tobiya wa ku Amoni, amene anali naye anati, “Chimene akumangacho ngati nkhandwe itakwerapo, itha kugwetsa khoma lawolo!”
4 Amo sia: nababeba: le, na da Godema sia: ne gadoi amane, “Gode! Dia ilia oufesega: su nabima! Ilia oufesega: su amo ilima sinidigima! Di da eno dunu ilia liligi wamolama: ne yolesima. Amola ha lai dunu da ili se dabe hamoma: ne, sedaga sogega oule masa: ma.
Tsono ndinayamba kupemphera kuti, “Timvereni, Inu Mulungu wathu, mmene akutinyozera. Mulole kuti mawu awo onyoza awabwerere, ndipo atengedwe ukapolo ku dziko lachilendo.
5 Ilia wadela: i hou mae gogolema: ne olofoma. Bai ilia da ninia moilai gagosu hawa: hamonanoba, ilia da ninima lasogole oufesega: lala.”
Musawakhululukire mphulupulu zawo kapena kufafaniza machimo awo pamaso panu popeza aputa ukali wanu pamaso pa anthu omanga khoma.”
6 Amalalu, ninia da gagoi amo bu gagolalu. Fonobahadi hedolowane ninia da gagolalu damana yolei defei amoga doaga: i. Bai dunu ilia da hawa: hamomu hanai galu.
Choncho ife tinamangabe khomalo kufikira lonse litafika theka la msinkhu wake, chifukwa chakuti anthu anagwira ntchitoyo ndi mtima wawo wonse.
7 Sa: naba: la: de, Doubaia, A:la: be soge dunu, A:mone soge dunu amola A: siedode soge dunu da ninia hehenane Yelusaleme gagoi gagolalebe amola dibi amo gagoi ganodini nini ga: simusa: ahoanebe amo nababeba: le, ilia da ougi bagade ba: i.
Koma pamene Sanibalati, Tobiya, Aarabu, Aamoni ndi anthu a ku Asidodi anamva kuti ntchito yokonzanso makoma a Yerusalemu ikupitirirabe ndipo kuti mipata ikutsekedwa, anapsa mtima kwambiri.
8 Amaiba: le, ilia da Yelusaleme amoga doagala: musa: amola ninia hawa: hamoi wadela: musa: sia: dasu.
Tsono onse anapangana za chiwembu kuti abwere ndi kudzathira nkhondo anthu a ku Yerusalemu ndi kuyambitsa mapokoso pakati pawo.
9 Be ninia da ninia Godema sia: ne gadosu. Amola ninia da eso amola gasi ganodini, sosodo aligisu dunu ili liligi noga: le ouligima: ne, ilegei dagoi.
Koma ife tinapemphera kwa Mulungu wathu ndipo tinayika alonda otiteteza kwa adaniwo usiku ndi usana.
10 Yuda dunu da agoane gesami hea: su, “Ninia gisasu liligi da dioi bagade, amola gisabeba: le ninia da gasa hamedesa. Wadela: i isu ninia gisawene, gaguli ahoa da gilisidafa. Amaiba: le, ninia da moilai gagoi wali eso habodane gaguma: bela: ?”
Pa nthawi yomweyi anthu a ku Yuda anati, “Mphamvu za anthu onyamula zinyalala zikutha ndipo pali zinyalala zambiri. Choncho ife sititha kumanga khomali.”
11 Ninima ha lai dunu da sia: dasu amo ninia Yu dunu da ilia hamobe da hame dawa: iyale ilia dawa: i. Ilia da ninima hedolo doagala: loba, nini huluane medole legele amola ninia hawa: hamosu hedofamusa: dawa: i.
Adani athunso anati, “Iwo asanadziwe izi, kapena kutiona, tidzakhala tili pakati pawo ndipo tidzawapha ndi kuyimitsa ntchitoyo.”
12 Be eso bagohame amoga, Yu dunu amo da ninia ha lai dunu gilisisu ganodini esalu, amo da ninima misini, amo ha lai sia: dasu ninima sisasu olelei.
Ndipo Ayuda amene ankhala pafupi ndi adani athuwo anabwera kakhumi konse kuchokera konse kumene ankakhala kudzatiwuza kuti tibwereko ku ntchito.
13 Amaiba: le na da dunu ilima gegesu gobihei, goge agei amola dadi, amo gegesu liligi ilima i. Amola ilia fi afae afae amo gagoi hame gagoi dagoi sogebi amoga sosodo aligima: ne sia: i.
Choncho kumbuyo kwa khoma, cha mʼmunsi mwake komanso malo amene anali asanathe ndinayikamo anthu mʼmabanja atatenga malupanga, mikondo ndi mauta awo.
14 Na ba: loba da dunu da bagadewane da: i dioi. Amaiba: le, na da ilia ouligisu dunu amola ouligisu hina dunu ilima amane sia: i, “Dilia ha lai dunu amoba: le mae beda: ma. Hina Gode da gasa bagadedafa amola osobo bagade dunu huluane da ema beda: sa. Amo dawa: sea, dilia fi dunu, dilia mano, dilia uda amola dilia diasu amo gaga: ma: ne gegema.”
Popeza anthu ankachita mantha, tsono ndinawawuza anthu olemekezeka, akuluakulu ndiponso anthu onse kuti, “Musawaope. Kumbukirani kuti Ambuye ndi wamkulu ndipo ndi woopsa. Choncho menyerani nkhondo abale anu, ana aamuna ndi aakazi, akazi anu ndi nyumba zanu.”
15 Fa: no, ninia ha lai dunu da ninia da ilia doagala: musa: sia: dasu nabi dagoi, amo ilia da nabi. Gode da ilia wadela: i logo ga: i dagoi, amo ilia da dawa: i. Amalalu, ninia huluane da gagoi bu gagomusa: , amoga buhagi.
Adani athu atamva kuti ife tadziwa za chiwembu chawo, anadziwanso kuti Yehova walepheretsa zimene ankafuna kutichita. Choncho tinabwerera aliyense ku ntchito yake yomanga khoma.
16 Amo esoga amola fa: no, na hawa: hamosu dunu eno dogoa mogili da gegesu liligi gaguli amola da: igene ga: ne, ninia ha lai dunu mabeale sosodo ouligili oulelu, amola eno mogili da gagoi gagomusa: hawa: hamosu. Amola ouligisu dunu da dunu huluane bagadewane fuligala: su.
Kuyambira tsiku limenelo mpaka mʼtsogolo mwake, theka la antchito anga linkagwira ntchito, pamene theka linalo limatenga mikondo, zishango, mauta ndi kuvala malaya azitsulo. Akuluakulu ankalimbikitsa Ayuda onse
17 Be hawa: hamonanu dunu amola liligi gaguli ahoasu dunu da agoane hamosu. Ilia da lobo la: idi amoga dadi gagui amola lobo eno la: idi amoga hawa: hamosu.
amene ankamanga khoma. Anthu onyamula zinyalala aja ankagwira ntchito ndi dzanja limodzi, dzanja linali atanyamula chida chankhondo.
18 Amola dunu da gagosu hawa: hamonoba, ilia huluane gegesu gobihei bagade bulua salawane hawa: hamonanu. Amola dunu amo da “biugale” wele sia: su liligi ouligisu da ani dafulili aligi.
Mʼmisiri aliyense ankamangirira lupanga lake mʼchiwuno mwake akamagwira ntchito. Koma munthu woyimba lipenga anali pambali panga nthawi zonse.
19 Na da dunu amola ilia ouligisu dunu ilima amane sia: i, “Dilia hawa: hamosu sogebi da bagadedafa amola dilia hisu hisuya hawa: hamonana.
Ndipo ine ndinati kwa anthu olemekezeka ndi anthu ena onse, “Ntchitoyi ndi yayikulu ndipo ili padera lalikulu ndipo ifeyo takhala motayanatayana kwambiri pa khoma.
20 Dilia ‘biugale’ wele sia: su nabasea, nama gilisila misa. Amola ninia Gode da nini fidili gegemu,” na amane sia: i.
Tsono kulikonse kumene muliko, mukamva kulira kwa lipenga bwerani mudzasonkhane kumene kuli ine kuno. Mulungu wathu adzatimenyera nkhondo.”
21 Amaiba: le, eso huluane hadigibi galu, dunu mogili da hawa: hamonanea, mogili da gegemusa: oulelu. Amalalu, daeya gasili gasumuni aligibiba: le fisi.
Choncho enafe tinapitiriza kugwira ntchito, pamene theka lina linkanyamula mikondo kuyambira mʼbandakucha mpaka nyenyezi zitaoneka.
22 Amo esoga, ouligisu dunu amo da Yelusaleme moilai amo ganodini ouligilaleawane hadigima: ne na da sia: i dagoi. Bai ninia da gilisili esoga hawa: hamomu amola gasia moilai amo sosodo aligimusa: dawa: i.
Pa nthawi imeneyo ndinawuzanso anthuwo kuti, “Aliyense pamodzi ndi wantchito wake agone mu Yerusalemu kuti tikhale ndi otilondera usiku ndi kuti masana tizigwira ntchito.”
23 Na, na ouligisu dunu, dadi gagui dunu amola hawa: hamosu dunu, ninia golaloba, abula sali mae gisa: le amowane golasu amola ninia dadi amola gegesu liligi loboga gaguiwane golasu.
Choncho ine, anzanga, antchito anga, ndi anthu otiteteza amene ankanditsata panalibe ndi mmodzi yemwe anavula zovala zake pogona. Aliyense anasunga chida chake chankhondo pambali pake.