< Nihemaia 1 >

1 Amo sia: da Nihemaia (Ha: galaia egefe) amo ea hawa: hamosu olelesa. Adasegesisi da Besia soge amoga hina bagade esalu. Ea ouligisu hou ode20 amola oubi ea dio Gisilefe amoga, na, Nihemaia, na da Besia bisili moilai bai bagade amo Susa, amo ganodini esalebe ba: i.
Awa ndi mawu a Nehemiya mwana wa Hakaliya: Pa mwezi wa Kisilevi, chaka cha makumi awiri, pamene ndinali mu mzinda wa Susa,
2 Na olalali afae amo ea dio Hana: inai, e amola eno dunu gilisili da Yuda soge fisili, nama doaga: i. Na da Yelusaleme moilai bai bagade ea hou, amola ninia Yu fi musa: mugululi asi, Yuda sogega buhagi, amo ilia hou ilima adole ba: i.
Hanani mmodzi mwa abale anga, anabwera ndi anthu ena kuchokera ku Yuda, ndipo ine ndinawafunsa za Ayuda otsala amene sanatengedwe ukapolo, ndiponso za mzinda wa Yerusalemu.
3 Ilia da amo hou nama adole i. Musa: mugululi asi dunu mogili da bogoi dagoi. Be mogili da buhagili, Yuda soge ganodini esala, da se bagade nabawane esala. Ga fi dunu gadenene esala da Yu dunu amo higale ba: sa, ilia sia: i. Yelusaleme gagoi dobea amo musa: mugululi sa: i dagoi, amo da bu hame gagoi. Amola logo ga: su musa: laluga nei, amo da bu hame ga: si.
Anandiyankha kuti, “Amene sanatengedwe ukapolo aja ali pa mavuto aakulu ndipo ali ndi manyazi. Khoma la Yerusalemu ndilogamukagamuka ndipo zipata zake zinatenthedwa ndi moto.”
4 Na da amo sia: nababeba: le, fila sa: ili amola bagadewane dinanu. Eso didia amoga, na da dinanuwane, ha: i mae nawane Godema sia: ne gadolalu.
Nditamva zimenezi, ndinakhala pansi ndi kuyamba kulira. Ndinalira kwa masiku angapo. Ndinkasala zakudya ndi kumapemphera pamaso pa Mulungu Wakumwamba.
5 Na da amane sia: ne gadoi, “Hina Gode Hebene ganodini esala! Di da bagadedafa amola ninia Diba: le beda: i bagade. Dia gousa: su, amo Di da Dima asigi amola nabasu dunu amo fidima: ne hamoi, amo Di da mae fisili dawa: lala.
Ndinkati: “Inu Yehova, Mulungu wakumwamba, Mulungu wamkulu ndi woopsa. Mumasunga pangano ndi kuonetsa chikondi chosasinthika kwa onse amene amakukondani ndi kumvera malamulo anu.
6 Hina Gode! Na hou ba: ma amola na sia: ne gadosu nabima! Na da dia fi dunu amo Isala: ili fi dunu amola uda, na da gasi huluane amola eso huluane amoga ili fidima: ne, Dima sia: ne gadolala. Dafawane! Ninia Isala: ili dunu da wadela: le hamoi dagoi. Na amola na aowalali dunu da wadela: i hou hamoi dagoi.
Tcherani khutu lanu ndi kutsekula maso anu kuti mumve pemphero la mtumiki wanune limene ndikupemphera usana ndi usiku pamaso panu kupempherera Aisraeli, atumiki anu. Ndikuvomereza machimo a Aisraeli amene tinakuchimwirani. Ndithu, ine ndi banja la makolo anga tinakuchimwirani.
7 Ninia da Dima wadela: i hou hamosu, amola Dia sia: hame nabasu. Ninia Dia sema amo Di da dia hawa: hamosu dunu Mousese ea lafidili ninima i, amoma hame fa: no bobogesu.
Ife tinakuchitirani zoyipa zambiri. Sitinamvere mawu anu, malamulo ndi malangizo anu amene munapereka kwa mtumiki wanu Mose.
8 Dia da Mousesema sia: i liligi bu dawa: ma, amane, ‘Dilia Isala: ili dunu da Na sia: hame nabasea, Na da dilia fi afagogole, ga fi dunu amo ganodini esaloma: ne sefasimu.
“Kumbukirani mawu amene munawuza mtumiki wanu Mose akuti, ‘Ngati mukhala osakhulupirika, ndidzakubalalitsani pakati pa mitundu ina.
9 Be amasea, dilia da Nama, Na dilima hamoma: ne sia: i defele Nama bu sinidigisia, Na da dili soge amoga Nama nodone sia: ne gadomusa: Na da ilegei, amo sogega Na da dili bu oule misunu,’ Di da amane sia: i dagoi.
Koma mukabwerera kwa Ine, mukamvera malamulo anga ndi kuwatsatadi, ndiye kuti ngakhale anthu anu atabalalika kutali chotani, Ine ndidzawasonkhanitsa kuchokera kumeneko ndi kubwera nawo ku malo amene ndinasankha kuti azidzayitanira dzina langa.’
10 Hina Gode! Amo dunu da Dia hawa: hamosu dunu! Ilia da Dia ilegei fi dunu! Di da Dia gasa bagade amoga, amo fi dunu gaga: i dagoi.
“Iwo ndi atumiki anu ndi anthu anu, amene munawawombola ndi mphamvu yanu yayikulu ndi dzanja lanu lamphamvu.
11 Amaiba: le, na sia: ne gadosu amola Dia hawa: hamosu dunu eno ilia Dima nodomusa: dawa: , ilia sia: ne gadosu amola nabima. Hina bagade da na sia: noga: le nabima: ne, Di da ea dogo ganodini hawa: hamoma!” na amane sia: ne gadoi. Amo esoga na da Besia hina bagade amo ea waini hano iasu dunu esalu.
Inu Ambuye tcherani khutu lanu kuti mumve pemphero la mtumiki wanune ndiponso pemphero la atumiki anu amene amakondwera kuchitira ulemu dzina lanu. Lolani kuti mtumiki wanune zinthu zindiyendere bwino lero ndi kuti mfumu indichitire chifundo.” Nthawi imeneyi nʼkuti ndili woperekera zakumwa kwa mfumu.

< Nihemaia 1 >