< Malagai 4 >

1 Hina Gode Bagadedafa da amane sia: sa, “Eso da mana, amoga wadela: i hamosu dunu amola hidale gasa fi dunu huluane da gilisili gisi agoane laluga nenanebe ba: mu. Amo esoga ili da laluga nene dagole, susei hamedafa ba: mu.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ndithu tsiku likubwera; lidzayaka ngati ngʼanjo. Anthu onse odzikuza, ndi aliyense ochita zoyipa adzapsa ngati chiputu, ndipo pa tsiku limene likubweralo adzapserera ndi moto. Sipadzatsalira muzu kapena nthambi.
2 Be dilia, Nama nabasu dunu, dilia da Na gaga: su gasa bagade hou dili gaga: ma: ne, eso ea heda: su hou defele dilima heda: lebe ba: mu. Amola eso ea digagala: su defele, dilia uhinisisu houdafa ba: mu. Bulamagau mano da ea gagoi logo doasi dagoi ba: sea, hahawane gadili lala, amo defele dilia da hahawane halegale lalumu.
Koma inu amene mumaopa dzina langa, dzuwa lachilungamo lidzakutulukirani lili ndi kuwala kokuchiritsani. Ndipo inu mudzatuluka ndi kulumphalumpha ngati ana angʼombe amene atulutsidwa mʼkhola.
3 Amo eso bagadega Na da gasa bagade hamosea, dilia da wadela: i hamosu dunu ilima osa: le heda: le, ilia da dilia emo hagudu osobo gulu agoane ba: mu.
Tsiku limenelo inu mudzapondereza anthu oyipa; adzakhala phulusa ku mapazi anu pa tsiku limene Ine ndidzachite zinthu zimenezi,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
4 Dilia da olelesu, amo Na da Na hawa: hamosu dunu Mousesema olelei, amo bu dawa: ma. Amo sema amola hamoma: ne sia: i Na da Sainai Goumia, Isala: ili dunu huluane ilima nabawane fa: no bobogema: ne, Mousesema i.
Kumbukirani zophunzitsa za mtumiki wanga Mose, malamulo ndi malangizo amene ndinamupatsa pa Horebu kuti awuze Aisraeli onse.
5 Amo eso bagadedafa Na da hamosea, osobo bagade fifi asi gala dunu huluane da bagadewane beda: mu. Be hidadea, Na da balofede dunu Ilaidia amo dilima asunasimu.
“Taonani, ndidzakutumizirani mneneri Eliya lisanafike tsiku lalikulu ndi loopsa la Yehova.
6 E da eda amola mano huluane gilisilisimu. Be agoane hame ilegei ganiaba, Na da dilia soge wadela: lesila: loba.” Sia: ama dagoi
Iye adzabweza mitima ya makolo kwa ana awo, ndi mitima ya ana kwa makolo awo. Kupanda kutero ndidzabwera kudzakantha dziko lanu ndi temberero.”

< Malagai 4 >