< Malagai 3 >
1 Hina Gode Bagadedafa da agoane adole iaha, “Na da Na sia: sia: na ahoasu dunu, Na logo fodoma: ne, amo asunasimu. Amasea, Hina Gode amo dilia hogoi helesa, E da hedolodafa Ea Debolo diasuga doaga: mu. Amo sia: sia: na ahoasu dunu dilia ba: mu hanai gala, amo da misini, Na gousa: su amo dilima sisia: mu.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ine ndidzatuma mthenga wanga amene adzakonza njira pamaso panga. Kenaka mwadzidzidzi Ambuye amene mukumufunafuna adzafika ku Nyumba yake. Mthenga wapangano amene mukumuyembekezera adzabwera.”
2 Be e da masea, nowa da moloiwane leloma: bela: ? E da aliaguda: lalebe ba: sea, nowa da mae bogole esaloma: bela: ? E da nigima: doga: su liligi gasa bagade agoai ba: mu, amola lalu bagade amo da silifa amola gouli ledo fadegasu agoane ba: mu.
Koma ndani adzatha kupirira pa tsiku la kubwera kwake? Ndani adzatha kuyima pamene Iye wafika? Pakuti adzakhala ngati moto wa mmisiri wa pa ngʼanjo, kapenanso ngati sopo wa munthu wochapa.
3 E da dunu amo da silifa amola gouli amoga ledo doga: su, amo defele e da fofada: musa: misunu. Amo silifa amola gouli hahamosu dunu da silifa amola gouli amoga ledo doga: sa, amo defele Hina Gode Ea sia: sia: na ahoasu dunu da gobele salasu dunu ilima ledo doga: sea, ilia da gobele salasu noga: idafa bu gaguli misunu.
Iye adzachita kukhalira pansi ngati mmisiri woyenga ndi woyeretsa siliva. Iye adzayeretsa Alevi ndi kuwayenga ngati golide ndi siliva. Pamenepo Yehova adzakhala ndi anthu amene azidzabweretsa zopereka mwachilungamo,
4 Amasea, Yelusaleme moilai bai bagade dunu amola Yuda fi dunu huluane da Hina Godema gobele salasu liligi gaguli masea, Hina Gode da musa: agoane iasu amoma hahawane ba: mu.
ndipo Yehova adzalandira zopereka za Yuda ndi Yerusalemu, ngati masiku akale, masiku amakedzana.
5 Hina Gode Bagadedafa da amane sia: sa, “Na da dilima aliaguda: lalebe ba: sea, fofada: mu galebe. Na da wadela: i hamosu dunuma fofada: mu amo fefedoasu dunu, inia uda adole lasu dunu, ogogosu dunu, nowa da ea hawa: hamosu dunuma ea bidi imunu sia: i amo hame iaha, nowa da didalo, guluba: mano amola ga fi ilima wadela: le hamosu dunu amola Nama hame nodosu dunu, amo huluane ilima Na da fofada: mu,” Hina Gode da amane sia: sa.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Tsono ndidzakuyandikirani kuti ndikuweruzeni. Mosataya nthawi ndidzanena mawu otsutsa mfiti, achigololo, a umboni wonama, amene salipira bwino antchito awo, amene amazunza akazi ndi ana amasiye, amene saweruza alendo mwachilungamo, komanso amene sandiopa Ine.”
6 “Na da Hina Godedafa! Na da hame afadenesa. Amaiba: le, dilia Ya: igobe egaga fi mogili da hame fisi, esalebe ba: sa.
“Ine ndine Yehova, ndipo sindisintha. Choncho inu zidzukulu za Yakobo, simunawonongedwe.
7 Dilia da dilia aowalali defele, Na Sema amo higabeba: le, wadela: lesi dagoi. Be wali dilia Nama sinidigima. Amasea, Na amola da dilima sinidigimu. Be dilia da Nama adole ba: sa, ‘Ninia da habodane Dima sinidigima: bela: ?’
Kuyambira nthawi ya makolo anu mwakhala mukuphwanya malamulo anga ndipo simunawatsatire. Bwererani kwa Ine, ndipo Ine ndidzabwerera kwa inu,” akutero Yehova Wamphamvuzonse. “Koma inu mukufunsa kuti, ‘Tibwerere motani kwa Yehova?’
8 Na da dilima agoane adole ba: sa, ‘Godema ogogosu hamomu da defeala: ?’ Hame mabu! Amo da defea hame galebe. Be dilia da Nama ogogosu hou hamonana. Be dilia da Nama adole ba: sa, ‘Ninia da Dima habodane ogogosu hou hamosala: ?’ Na da dilima bu adole iaha, ‘Dilia Nama iabe, amo ‘daide’ (dilia gagui nabuane momogili, afae Nama iaha), amola hahawane udigili iasu hou amo ganodini Nama ogogosa.’
“Kodi munthu angathe kuba za Mulungu? Komatu inu mumandibera. “Koma inu mukufunsa kuti, ‘Kodi timakuberani motani?’ “Pa zakhumi ndi pa zopereka.
9 Isala: ili dunu fi huluanedafa da Nama ogogole hedebeba: le, Na gagabusu da ilima aligisa.
Mtundu wanu wonse ndinu otembereredwa, chifukwa mukundibera.
10 Be dilia ogogosu hedesu fisili, “daide” liligi huluanedafa amo Debolo diasuga gaguli misa. Amasea, Debolo diasu ganodini, ha: i manu defele agoane da ba: mu. Nama adoba: le ba: ma. Amasea, Na da Hebene logo doasili, hahawane dogolegesu hou bagadedafa amo dilima gugudili sogadigimu. Amasea, dilia da liligi noga: idafa labeba: le, lelegesu diasu da baligili nabaidafa ba: mu.
Bweretsani chakhumi chathunthu ku nyumba yosungira, kuti mukhale chakudya mʼnyumba mwanga.” Akutero Yehova Wamphamvuzonse, “Tandiyesani, ndipo muone ngati sindidzatsekula zipata zakumwamba, ndi kukugwetserani madalitso ochuluka amene mudzasowe malo owayikamo.
11 Na da sia: beba: le, danuba: da dilia ha: i manu bugi amo hame wadela: lesimu. Amola dilia waini efe da waini fage bagohame legebe ba: mu.
Ndidzaletsa tizirombo kuti tisawononge mbewu zanu, ndipo mpesa wa mʼminda mwanu zipatso zake sizidzayoyoka,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
12 Amasea, osobo bagade fifi asi gala dunu huluane da dilia da Gode Ea hahawane dogolegei fi amo sia: mu. Bai dilia soge da fimu noga: i soge ba: mu.
“Motero anthu amitundu yonse adzakutchulani odala, pakuti dziko lanu lidzakhala lokondweretsa,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
13 Hina Gode da amane sia: sa, “Dilia da Na hou amoma lasogole bagadewane sia: su. Be dilia da agoane adole ba: sa, ‘Ninia da Dia hou olelema: ne adi sia: bela: ?’
Yehova akuti, “Mwayankhula mawu owawa onena za Ine. “Komabe inu mukufunsa kuti, ‘Kodi tanena chiyani chotsutsana nanu?’
14 Dilia da amane sia: su, ‘Gode Ea hawa: hamosu hamomu da hamedei. Ninia Hina Gode Bagadedafa Ea sia: amoga fa: no bobogemu amola Ema sinidigima: ne fofada: ne, asigi sia: sia: mu da hamedei liligi agoai galebe.
“Mwanena kuti, ‘Kutumikira Mulungu nʼkosapindulitsa. Kodi timapindulanji pochita zofuna zake, ndi kumayenda ngati anamfedwa pamaso pa Yehova Wamphamvuzonse?
15 Ninia ba: loba, gasa fi dunu ilia fawane da hahawane esala. Wadela: i dunu da hahawane liligi bagade gagusa. Amola, ilia da Godema wadela: i adoba: su hou hamonana, amola Gode da ilima se hame iaha,’ dilia da agoane sia: sa.”
Koma tsono ife timati anthu odzikuza ndiye odalitsika. Kunena zoona anthu oyipa ndiye amapeza bwino, ngakhale amene amanyoza Mulungu amapulumuka.’”
16 Amasea, Hina Godema beda: iwane dawa: su dunu da gilisili sia: dasu. Amola Hina Gode da ilia sia: dasu nabi dagoi. Amola E ba: ma: ne, a:igele dunu da buga ganodini, dunu amola uda huluane da Hina Godema beda: iwane dawa: su amola Ema nodosu, ilia dio huluane dedei dagoi.
Ndipo woopa Yehova anayamba kukambirana, ndipo Yehova anamvetsera. Buku la chikumbutso linalembedwa pamaso pake, lonena za amene amaopa Yehova ndi kulemekeza dzina lake.
17 Amola Hina Gode Bagadedafa da amane sia: i, “Amo dunu amola uda da Na fidafa esalumu. Na eso Bagadedafa da doaga: sea, ilia da Na dunudafa esalebe ba: mu. Osobo bagade ada da ea mano amo da ea hawa: hamosa, ilima asigiba: le gogolema: ne olofosa, amo defele Na da amo dunu ilima asigimu amola gogolema: ne olofomu.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu amenewo adzakhala anga, tsiku limene Ine ndidzachita izi, adzakhala angaanga. Ndidzawaleka osawalanga monga mmene munthu amachitira chifundo mwana wake amene amamutumikira.
18 Amola Na fi dunu da Na houdafa bu ba: mu. Amola hou da fa: no moloidafa dunu amoga doaga: mu da hou hisu amola hou da wadela: i hamosu dunu amoma doaga: mu da hou hisu, amo ilia da ba: mu. Amola Nama hawa: hamosu dunu ilia da hou hisu ba: mu, amola Nama fa: no bobogemu higa: i dunu ilia da hou hisu ba: mu, amo ilia da dawa: mu.
Pamenepo mudzaonanso kusiyana pakati pa anthu olungama ndi oyipa, pakati pa amene amatumikira Mulungu ndi amene satumikira Mulungu.”