< Gobele Salasu 8 >

1 Hina Gode da Mousesema amane sia: i,
Yehova anawuza Mose kuti,
2 “Dia Elane amola egefelali amo Na Abula Diasu logo holeiga oule misa. Gobele salasu abula amola ligiagasu susuligi, bulamagau mano (gawali) Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne Iasu gobele salasu hamoma: ne, sibi gawali aduna amola daba yisidi hame sali agi ga: gi amoga nabai, gaguli misa.
“Tenga Aaroni ndi ana ake, zovala zawo, mafuta wodzozera, ngʼombe yayimuna kuti ikhale nsembe yopepesera machimo, nkhosa ziwiri zazimuna ndi dengu la buledi wopanda yisiti,
3 Amasea, dunu fi huluane amogawi gilisima: ne sia: ma.”
ndipo usonkhanitse gulu la anthu pa khomo la tenti ya msonkhano.”
4 Mousese da Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i defele hamoi. Amasea, fi dunu huluane da gilisi dagosea,
Mose anachita zomwe Yehova anamulamula ndipo gulu la anthu linasonkhana pa khomo la tenti ya msonkhano.
5 e da ilima amane sia: i, “Na da wali Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i liligi amo hamomu.”
Mose anawuza gulu la anthuwo kuti, “Izi ndi zimene Yehova walamulira kuti zichitike.”
6 Mousese da Elane amola egefelali ba: le gaidiga oule misini, ilima ilia da sema defele hanoga ulima: ne sia: i.
Pamenepo Mose anabwera ndi Aaroni ndi ana ake nawasambitsa ndi madzi.
7 E da Elanema da: i salasu amola abula gasisa: li. Amola abula eno bululisi. Amola e da ea bidegiga Ifode gasisa: li, amola amo ea nodomei bulu amoga ga: si.
Anamuveka Aaroni mwinjiro, ndi kumumanga lamba mʼchiwuno. Anamuvekanso mkanjo wa efodi ndi efodiyo. Anamangira lamba efodiyo amene analukidwa mwaluso uja, motero efodiyo analimba mʼchiwunomo.
8 E da bidegi ea dedebosu gasisa: lili, amo ganodini Ulimi amola Damini sali.
Anamuvekanso chovala chapachifuwa ndipo mʼchovalacho anayikamo Urimu ndi Tumimu.
9 E da ea dialumaga habuga figisi amola amo ea midadi gouliga nina: hamosu mogili gagasu dawa: digima: ne olelesu sema liligi amo la: gi. E da Hina Gode ea hamoma: ne sia: i defele hamoi dagoi.
Kenaka anamuveka Aaroniyo nduwira kumutu ndipo patsogolo pa nduwirayo anayikapo duwa lagolide, chizindikiro chopatulika monga momwe Yehova analamulira Mose.
10 Amasea, Mousese da ligiagasu susuligi lale, Hina Gode Ea Abula Diasu amola liligi huluane amo ganodini dialu amoga legei dagoi. Amasea, liligi huluane da Hina Godema momodale ligiagai dagoi ba: i.
Pamenepo Mose anatenga mafuta wodzozera nadzoza tenti ya msonkhano pamodzi ndi zonse zimene zinali mʼmenemo, ndipo potero anazipatula.
11 Amasea e da susuligi mogili lale, fesuale agoane oloda amola ea liligi amola ofodo bagade amola ea bai amoga Hina Godema momodale ligiagama: ne, foga: gagala: i.
Anawaza mafuta ena pa guwa kasanu ndi kawiri, nalidzoza guwalo pamodzi ndi ziwiya zake zonse. Anadzozanso beseni ndi tsinde lake, nazipatula.
12 E da Elane mogili gagamusa: , susuligi mogili ea dialuma amo da: iya, sogadigi.
Anathira mafuta wodzozera ena pamutu pa Aaroni ndipo anamudzoza ndi kumupatula.
13 Amasea, Mousese da Elane egefelali oule misini, ilima da: i salasu amola abula bulu gasisali, amola ilia dialumaga habuga figisi-Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i defele hamoi.
Kenaka anabwera ndi ana a Aaroni. Anawaveka minjiro, ndi kuwamanga malamba mʼchiwuno ndi kuwaveka nduwira kumutu monga momwe Yehova analamulira Mose.
14 Amasea, Mousese da Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne Iasu gobele salasu hamoma: ne, bulamagau mano gawali amo oule misini, Elane amola egefelali da ilia lobo ea dialuma da: iya ligisi.
Kenaka Mose anabwera ndi ngʼombe yayimuna ya nsembe yopepesera machimo, ndipo Aaroni ndi ana ake anasanjika manja awo pamutu pa ngʼombeyo.
15 Mousese da amo bulamagau medole legele, ea maga: me mogili lale, ea lobo sogo amoga ‘hono’ oloda ea hegomaiga diala amoga sema modale ligiagama: ne ilegei. Amasea, eno maga: me dialu amo e da oloda ea baiga sogadigi-oloda modale ligiagama: ne amola ledo fadegama: ne.
Mose anapha ngʼombeyo, ndi kutenga magazi ena angʼombeyo ndi kupaka ndi chala chake pa nyanga zaguwa lansembe, naliyeretsa. Magazi otsalawo anawakhuthulira pa tsinde laguwalo. Motero anachita mwambo wopepesera machimo.
16 Mousese da dialumagaisa, habe ea la: idi noga: i, fogome ganumui amola sefe amoga diala amo lale, oloda da: iya gobesi.
Mose anatenganso mafuta onse okuta matumbo, mafuta ophimba chiwindi, ndiponso impsyo zonse ziwiri pamodzi ndi mafuta ake, nazitentha pa guwapo.
17 E da bulamagau ea da: i hodo eno dialu, - ea gadofo, ea hu amola ea iga huluane - amo lale, Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i defele, abula diasu gilisisu gadili gobesi dagoi.
Koma nyama yangʼombeyo, chikopa chake ndi matumbo ake anaziwotcha kunja kwa msasa monga momwe Yehova analamulira Mose.
18 Amasea, Mousese da sibi gawali amo Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu gobele salimusa: oule misini, Elane amola egefelali da ilia lobo ea dialuma da: iya ligisi.
Kenaka anabwera ndi nkhosa yayimuna ya nsembe yopsereza, ndipo Aaroni ndi ana ake aamuna anasanjika manja awo pamutu pake.
19 Mousese da amo sibi gawali medole legele, ea maga: me amo oloda ea afo biyaduyale gala amoga sogaga: la: gaganoi.
Ndipo Mose anapha nkhosayo ndi kuwaza magazi ake mbali zonse zaguwalo.
Anayidula nkhosayo nthulinthuli ndipo anatentha mutu wake, nthulizo ndi mafuta.
21 E da sibi gawali amo dadega: le, ea iga amola emo hanoga dodofele, amola sefe amola sibi gawali ea da: i hodo huluane, Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i defele, gobesi. Amo Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu gobele salasu da Ha: i Manu Iasu agoane ba: i, amola ea gabusiga: amo Hina Gode da hahawane nabi.
Anatsuka matumbo ake ndi miyendo yake, ndi kutentha nkhosa yonseyo pa guwa lansembe kuti ikhale nsembe yopsereza, fungo lokoma, nsembe yachakudya yoperekedwa kwa Yehova monga Yehovayo analamulira Mose.
22 Amasea, Mousese da sibi gawali eno, gobele salasu dunu ili momogili gagama: ne, (amo da Ligiagasu Iasu) amo oule misini, Elane amola egefelali da ilia lobo amo ea dialuma da: iya ligisi.
Kenaka Mose anapereka nkhosa yayimuna ina pamwambo wodzoza ansembe, ndipo Aaroni ndi ana ake aamuna anasanjika manja awo pamutu pake.
23 Mousese da amo sibi gawali medole legele, ea maga: me mogili lale, amo Elane ea lobodafadi ge gehahaya amola ea lobodafadi bi amola ea emodafadi bi amoga legei.
Mose anayipha nkhosayo ndipo anatenga magazi ake ena ndi kupaka ndewere za khutu la kudzanja lamanja la Aaroni, pa chala chake chachikulu cha kudzanja lamanja, ndi pa chala chake chachikulu cha phazi lakumanja.
24 Amasea, Mousese da Elane egefelali amo oule misini, maga: me mogili lale, ilia lobodafa la: idi ge gehahaya amola ilia lobodafa bi amola ilia emodafa bi amoga legei. Amasea, e da maga: me eno dialu amo oloda ea afo biyaduyale amoga sogaga: la: gaganoi.
Pambuyo pake Mose anabwera ndi ana aamuna a Aaroni ndi kupaka magazi pa ndewere za makutu awo akumanja, pa zala zawo zazikulu za dzanja lamanja, ndiponso pa zala zawo zazikulu za kuphazi lakumanja. Kenaka iye anawaza magazi otsalawo mbali zonse za guwalo.
25 E da sefe huluane, la: go bai, dialumagaisa, habe ea la: idi noga: i, fogome ganumui amola ela sefe amola emodafa amo lai.
Anatenganso mafuta ake, mafuta a ku mchira wake, mafuta okuta matumbo, mafuta okuta chiwindi, impsyo zonse ziwiri ndi mafuta ake ndiponso ntchafu yakumanja.
26 Amasea, e da agi ga: gi amoga yisidi hame sali Godema iasu, daba ganodini sali, amoga e da agi ga: gi afadafa lale, amola ga: gi eno susuligi amoga hamoi amola belowagi afae lale, amo sefe huluane amola emodafa amo da: iya ligisi.
Ndipo mʼdengu la buledi wopanda yisiti limene linali pamaso pa Yehova, anatengamo buledi mmodzi, buledi mmodzi wokhala ndi mafuta a olivi, ndi buledi wopyapyala mmodzi. Zonsezi anaziyika pa mafuta aja ndi pa ntchafu ya ku dzanja lamanja ija.
27 E da amo ha: i manu huluane Elane amola egefelalia loboga ligisili, ilia da amo hahawane iasudafa agoane, Hina Godema ima: ne olelei.
Mose anapereka zonsezi mʼmanja mwa Aaroni ndi ana ake amene anazipereka kwa Yehova kuti zikhale nsembe yoweyula.
28 Amasea, Mousese da ilima amo ha: i manu bu lale, oloda da: iya, Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu gadodili, ili momogili gagama: ne, gobesi dagoi. Amo da ha: i manu iasu, amola ea gabusiga: amo Hina Gode da hahawane nabi.
Kenaka Mose anazitenga mʼmanja mwawo ndipo anazipsereza pa guwa lansembe pamwamba penipeni pamodzi ndi nsembe yopsereza ija kuti ikhale nsembe yopereka pamwambo wodzoza ansembe, kuti ipereke fungo lokoma, chopereka chachakudya kwa Yehova.
29 Amasea, Mousese da sibi gawali ea sogogea lale, Hina Godema i dagoi. Amo sogogea da ligiagasu gobele salasu sibi gawali, amo Mousese hi iabe gala. Mousese da hou huluane Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i defele hamoi.
Mose anatenga chidale cha nkhosa yayimuna, chomwe ndi gawo lake pamwambo wodzoza ansembe, ndipo anachiweyula pamaso pa Yehova kuti chikhale nsembe yoweyula monga momwe Yehova analamulira Mose.
30 Amola, Mousese da ligiagasu susuligi mogili amola maga: me oloda da: iya dialu mogili amo lale, Elane amola egefelalia abula amoga fogaga: gala: i. E da amo hou amoga ili Godema momogili gagai dagoi.
Kenaka Mose anatenga mafuta wodzozera ansembe ndi magazi amene anali pa guwa nawaza pa Aaroni ndi zovala zake ndiponso ana ake aja ndi zovala zawo. Motero Mose anapatula Aaroni ndi zovala zake, ndiponso ana ake ndi zovala zawo.
31 Mousese da Elanema amane sia: i, “Hu amo Hina Gode Ea Abula Diasu logo holeiga gaguli masa. Amoga gobele moma! Amola agi ga: gi amo da ligiagasu iasu daba ganodini diala, Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i defele, moma.
Mose anawuza Aaroni ndi ana ake kuti, “Phikani nyamayo pa khomo la tenti ya msonkhano, ndipo mudyere pomwepo pamodzi ndi buledi amene ali mʼdengu la zopereka za pamwambo wodzoza ansembe monga Yehova analamulira kuti, ‘Aaroni ndi ana ake azidya zimenezi.’
32 Hu o agi ga: gi hame mai galea, amo laluga gobesima.
Ndipo nyama ndi buledi zotsalazo, muziwotche.
33 Dilia da Abula Diasu logo holeiga eso fesuale gala, amogawi esalu, ligiagasu sema hou huluane hamoi dagosea fawane yolesimu.
Musatuluke kunja kwa tenti ya msonkhano kwa masiku asanu ndi awiri mpaka masiku amwambo wokudzozani unsembe atatha, pakuti mwambowu ndi wa masiku asanu ndi awiri.
34 Hina Gode da dilia wali eso hou hamobe amo hamoma: ne sia: i. Bai dilia wadela: i hou fadegamusa:
Zimene zachitika lerozi analamula ndi Yehova kuti zichitike ngati nsembe yopepesera machimo anu.
35 Dilia mae yolesili, Abula Diasu ea logo holeiga eso amola gasi, fesuale agoane ouesaloma. Amane hame hamosea, dilia da bogosu ba: mu. Hina Gode da amo hou hamoma: ne, nama sia: i dagoi.
Muzikhala pa khomo la tenti ya msonkhano usana ndi usiku kwa masiku asanu ndi awiri. Ndipo muzichita zimene Yehova wakulamulani kuti musafe, pakuti zimenezi ndi zomwe Yehova wandilamulira.”
36 Amaiba: le, Elane amola egefelali da Hina Gode Ea Mousesema sia: i liligi huluane hamoi dagoi.
Choncho Aaroni ndi ana ake anachita zonse zimene Yehova analamula kudzera mwa Mose.

< Gobele Salasu 8 >