< Gobele Salasu 7 >

1 Dabe Ima: ne Iasu gobele salasu hou da hadigidafa. Hagudu da ilia hamoma: ne sia: i dedei diala.
“‘Malamulo a nsembe yopepesera kupalamula imene ndi nsembe yopatulika kwambiri ndi awa:
2 Dilia Dabe Ima: ne Iasu ohe amo oloda ea gagoe (north) la: idi (amoga ilia da gobele salasu ohe medole legesa) amoga medole legele, ea maga: me amo oloda ea la: idi la: idi biyaduyale gala amoga sogaga: la: gaganoma: mu.
Nsembe yopepesera machimo iziphedwa pamalo pomwe amaphera nsembe yopsereza ndipo awaze magazi ake mbali zonse za guwa.
3
Tsono apereke mafuta ake onse: mchira wamafuta ndi mafuta amene amakuta matumbo.
4 Amasea, ea sefe huluane amola ea sefe la: go amola dialumagaisa amola ea fogome ganumui amola sefe amoga diala amola habe ea la: idi noga: iwane gala amo dasega: le, oloda da: iya gobesima: mu.
Aperekenso impsyo ziwiri, mafuta ake pamodzi ndi mafuta onse amene ali chamʼchiwuno, ndiponso mafuta onse amene aphimba chiwindi.
5 Gobele salasu dunu da oloda da: iya sefe huluane Hina Godema Dabe Ima: ne Iasu hamoma: ne, gobesima: mu.
Wansembe azitenthe pa guwa kuti zikhale nsembe yotentha pa moto, yoperekedwa kwa Yehova. Imeneyi ndi nsembe yopepesera tchimo lopalamula.
6 Nowa da gobele salasu dunu fi amo ganodini gawali gala da amo manu da defea. Be amo da hadigi sogebi amo ganodini manu da defea. Bai amo iasu da hadigidafa.
Munthu wamwamuna aliyense wa mʼbanja la wansembe angathe kudyako nsembeyo koma adyere ku malo opatulika. Imeneyi ndi nsembe yopatulika kwambiri.
7 Hamoma: ne sia: i afadafa da Dabe Ima: ne Iasu amola Wadela: i Hou Da: be Ima: ne Iasu amoga ouligisa. Amo da nowa gobele salasu dunu da gobele salasu hamoi galea, amo hu da ea:
“‘Nsembe yopepesera tchimo lopalamula ndi yofanana ndi nsembe yoperekedwa chifukwa cha tchimo. Ndipo nsembe ziwiri zonsezi zili ndi lamulo limodzi lokha. Wansembe amene wachita mwambo wa nsembe yopepesera machimo a kupalamula atenge nyamayo ngati yake.
8 Gobele salasu dunu da ohe Hina Godema ima: ne gobele salasea, e da amo ea gadofo lamu.
Wansembe wopereka nsembe yopsereza ya munthu wina aliyense, atenge chikopa cha nsembe yopserezayo kuti chikhale chake.
9 Gala: ine Iasu amola amo da gobele nasu ganodini gobei o ofodo ganodini o agi gobesu agoai da: iya gobei amo ha: i manu huluane da gobele salasu dunu amo da Godema gobele sali, amo ea:
Chopereka chilichonse cha chakudya chophika mu uvuni kapena chokazinga mu mʼphika kapena mu chiwaya ndi cha wansembe amene wapereka nsembezo.
10 Be Gala: ine Iasu hame gobei (susuligi gilisi o hafoga: i) amo huluane da Elane gobele salasu dunu fi ilia: Amo fifili defele ima: mu.
Ndipo chopereka china chilichonse cha chakudya chosakaniza ndi mafuta kapena chowuma, chikhale cha ana onse a Aaroni ndipo anawo achigawane mofanana.
11 Hagudu da Hahawane Gilisili Olofole Iasu Hina Godema ima: ne hamoma: ne sia: i dedei diala.
“‘Malamulo a nsembe ya chiyanjano imene munthu angathe kupereka kwa Yehova ndi awa:
12 Nowa dunu da Godema nodoma: ne amo Iasu imunusa: dawa: sea, e da ohe gobele salimusa: amola agi ga: gi (yisidi hame gilisi) gaguli misa: mu. Amo agi ga: gi da falaua amola olife susuligi amoga hamoi o belowagi amoga olife susuligi da legei o falaua ga: gi amola olife susuligi gilisi amoga hamoi.
“‘Ngati munthuyo apereka chifukwa cha kuthokoza, apereke nsembeyo pamodzi ndi makeke wopanda yisiti, osakaniza ndi mafuta; timitanda ta buledi wopanda yisiti, topyapyala, topaka mafuta, ndiponso makeke a ufa wosalala wophikidwa bwino, wosakaniza ndi mafuta.
13 Amola eno, e da agi ga: gi yisidi hame gilisi amo gobei gaguli misa: mu.
Pamodzi ndi nsembe yachiyanjano yothokozerayo abwerenso ndi makeke opangidwa ndi yisiti ngati chopereka chake.
14 E da agi ga: gi hisu hisu amo fifili, Hina Godema dawa: ma: ne Ema imunu. Amo agi ga: gi da gobele salasu dunu amo da ohe ea maga: me lale, oloda la: idiga sogaga: la: gaganosa, amo dunu ea:
Munthuyo atenge mtanda umodzi pa mtanda wa buledi wa mtundu uliwonse kuti ukhale nsembe yopereka kwa Yehova. Tsono mtanda umenewo ndi wake wa wansembe amene awaze magazi a nsembe yachiyanjano.
15 Ohe ea hu da eso amoga e da gobele sali amo mai dagoi ba: ma: mu. Golale, hahabe, eno hu hame mai dialumu da sema bagade.
Nyama ya nsembe yachiyanjano yothokozera idyedwe pa tsiku lomwe nsembeyo yaperekedwa ndipo isatsaleko mpaka mmawa.
16 Be dunu da ea sia: ilegei dafawaneyale ba: ma: ne o udigili hahawane ima: ne, Hahawane Gilisili Olofole Iasu gaguli masea, amo esoga ha: i manu hame mai diala, amo aya esoga manu da defea.
“‘Koma ngati nsembe yakeyo apereka chifukwa cha lumbiro kapena mwaufulu, nsembeyo adye tsiku lomwe yaperekedwalo. Koma yotsala angathe kuyidya mmawa mwake.
17 Be hu da eso osodayale dialebe ba: sea, amo gobesima: mu.
Ngati nyama ina ya nsembe yatsalabe mpaka tsiku lachitatu, imeneyo itenthedwe pa moto.
18 Be dunu da eso osodayale amoga hu nasea, Gode da iabe dunu ea iasu hame lamu. Hina Gode da ea wadela: i hou hame gogolema: ne olofomu. Be E da amo iasu ledo hamoi dagoi ba: mu. Amola nowa dunu da amo nasea, se nabimu.
Ngati munthu adya nyama yachiyanjano pa tsiku lachitatu, nsembeyo sidzalandiridwa. Amene wayipereka nsembeyo Mulungu sadzamulandira ndipo nsembeyo idzakhala yonyansa pamaso pa Mulungu, yosamupindulira kanthu woperekayo.
19 Be ledo hamoi liligi da Godema Iasu hu amo digili ba: sea, amo hu mae moma: ne sia: ma. Amo hu gobesima: mu. Nowa dunu da Hina Gode Ea sema defele dodofei dagoi ba: sea, da Godema Iasu bu manu defele ba: mu.
“‘Nyama imene yakhudza chilichonse chodetsedwa, munthu asayidye, koma itenthedwe pa moto. Aliyense amene ali woyeretsedwa angathe kudya nyama inayo.
20 Be nowa da ledo gala hame dodofei ba: sea, amo hu nasea, e da Gode Ea Fidafa amoga afafai dagoi ba: mu.
Koma ngati munthu wina amene ndi wosayeretsedwa adya nyama ya nsembe yachiyanjano imene ndi ya Yehova, ameneyo achotsedwe pakati pa anthu a mtundu wake.
21 Amola, nowa da ledo hamoi liligi (dunuga o ohega hamoi) digili ba: lu, amo hu udigili nasea, e amola da Gode Ea Fidafa amoga afafai dagoi ba: mu.
Ndipo ngati munthu wina akhudza chinthu chodetsedwa, kaya chonyansa cha munthu kapena cha nyama, kapenanso chonyansa china chilichonse, ndipo kenaka nʼkudya nyama ya nsembe yachiyanjano imene ndi ya Yehova, munthu ameneyo achotsedwe pakati anthu a mtundu wake.’”
22 Hina Gode da Mousesema (Isala: ili fi dunuma alofele ima: ne) hagudu dedei hamoma: ne sia: i olelei.
Yehova anayankhula ndi Mose kuti,
23 Bulamagau, sibi amola goudi, ilia sefe maedafa moma: ne sia: ma.
“Awuze Aisraeli kuti, ‘Musadye mafuta a ngʼombe, nkhosa kapenanso mbuzi.
24 Ohe amo da hisu bogoi o sigua ohega medole legei, amo ea sefe mae moma: ne sia: ma. Be ea sefe eno hou hamomusa: lamu da defea.
Mafuta a nyama yofa yokha, kapena mafuta a nyama yophedwa ndi zirombo akhoza kuwagwiritsa ntchito iliyonse, koma inu musadye mafuta amenewo.
25 Nowa da ohe amo Hina Godema ha: i manu iasu imunusa: ilegei galu, amo ea sefe nasea da Gode Ea Fidafa amoga afafai dagoi ba: mu.
Pakuti munthu wakudya mafuta a nyama yoperekedwa kwa Yehova ngati nsembe yotentha pa moto, ayenera kuchotsedwa pakati pa anthu a mtundu wake.
26 Isala: ili dunu da habodili esalea, sio o ohe ilia maga: me manu da sema bagade.
Ndipo kulikonse kumene mukakhale musakadye magazi a mbalame iliyonse kapena magazi a nyama iliyonse.
27 Nowa da amo sema wadela: sea, da Gode Ea Fidafa amoga afafai dagoi ba: mu.
Ngati munthu aliyense adya magazi achotsedwe pakati pa anthu a mtundu wake.’”
28 Amola Hina Gode da Mousesema Isala: ili fi dunuma alofele ima: ne amo hagudu dedei hamoma: ne sia: i olelei.
Yehova anayankhula ndi Mose kuti,
29 Nowa da Hahawane Gilisili Olofole Iasu imunusa: dawa: sea, e da amo fifilalu, fifi afae Hina Godema imunusa: gaguli misa: mu.
“Awuze Aisraeli kuti, Aliyense amene apereka nsembe yachiyanjano kwa Yehova, abwere ndi gawo la nsembeyo kwa Yehova.
30 E da amo hi loboga ha: i manu iasu gaguli misa: mu. E da amo ohe ea sefe amola ea bidegi gaguli misini, Hina Godema ima: ne sia: ma.
Atenge ndi manja ake zigawo za chopereka zoyenera kuzitentha pa moto ngati chopereka kwa Yehova. Abweretse mafuta, pamodzi ndi chidale chomwe, ndipo chidalecho achiweyule kuti chikhale chopereka choweyula kwa Yehova.
31 Gobele salasu dunu da sefe amo oloda da: iya gobesimu. Be bidegi amo da gobele salasu dunu ea:
Wansembe atenthe mafutawo pa guwa koma chidalecho chikhale cha Aaroni ndi ana ake.
Mumupatse wansembe ntchafu ya kumanja ya nsembe yanu yachiyanjano kuti ikhale chopereka chanu kwa iye.
33 Amo ohe ea emodafa e da gobele salasu dunu amo da maga: me amola sefe Hahawane Gilisili Olofole Ima: ne iaha, amo ema imunu.
Mwana wa Aaroni amene amapereka magazi ndi mafuta a nsembe yachiyanjano, adzitenga ntchafu ya kumanja kukhala gawo lake.
34 Ohe ea bidegi amola emodafa amo ele da iasu noga: idafa amo Hina Gode da Isala: ili fi dunu ilima lale, gobele salasu fi dunu ilima iaha. Amo hou da mae yolesili, dialumu.
Choncho pa zopereka zachiyanjano za Aisraeli, Ine ndatengapo chidale chomwe amaweyula ndi ntchafu zimene amapereka nsembe ndipo ndazipereka kwa wansembe Aaroni ndi ana ake. Izi ndizo gawo lawo nthawi zonse pa zopereka za Aisraeli.”
35 Amo da ha: i manu Hina Godema iasu, amo fifili, Elane amola egefelali, amo ilia gobele salasu dunu ilegesu eso amoga iasu.
Zimenezi ndi chigawo cha Aaroni ndi ana ake chotapidwa pa zopereka kwa Yehova zoti zitenthedwe pa moto zimene zinaperekedwa pa tsiku limene anapatulidwa kuti akhale ansembe otumikira Yehova.
36 Amo esoga, Hina Gode da Isala: ili dunu ilima ilia da iasu fifili, amo fifi gobele salasu dunuma ima: ne sia: i. Amo hamoma: ne sia: i da Isala: ili dunu ilima fa: no eso huluane mae yolesili, ouligima: ne sia: ma
Yehova ndiye analamulira kuti pa zopereka za Aisraeli azitapapo zimenezi ndi kuwapatsa ansembe ngati gawo lawo. Yehovayo analamula zimenezi pa tsiku limene ansembewo anapatulidwa ndipo anachikhazikitsa ngati lamulo la nthawi zonse.
37 Defea! Amo da Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu, Gala: ine Iasu, Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne Iasu, Mae Dawa: le Wadela: i Hamoi Iasu, Dabe Ima: ne Iasu amola Hahawane Gilisili Olofole Iasu ilia hamoma: ne sia: i huluane dedei diala.
Awa ndi malamulo a nsembe izi: nsembe yopsereza, nsembe yachakudya, nsembe yopepesera machimo, nsembe yopepesera kupalamula, nsembe ya mwambo wodzoza ndi nsembe yachiyanjano.
38 Sainai Goumi, hafoga: i soge ganodini, amogawi Hina Gode da amo hamoma: ne sia: i huluane Mousesema i dagoi. Eso amoga E da Isala: ili dunu ilia iasu ima: ne sia: i, E da amo hamoma: ne sia: i Mousesema i.
Malamulo amenewa Yehova anapereka kwa Mose pa Phiri la Sinai pa tsiku limene Yehova analamulira Aisraeli kuti abwere ndi zopereka za kwa Yehova, ku chipululu cha Sinai kuja.

< Gobele Salasu 7 >