< Gobele Salasu 25 >

1 Hina Gode da Sainai Goumia, Mousesema amane sia: i,
Yehova anawuza Mose pa phiri la Sinai kuti,
2 “Isala: ili fi dunuma amane sia: ma, ‘Dilia soge amo Hina Gode da dilima iabe, amo ganodini golili dasea, dilia Hina Gode Ea nodoma: ne, ode fesuga osobo mae gidinama.
“Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Mukadzalowa mʼdziko limene ndikukupatsani, nthakayo iyenera kumakasunga Sabata la Yehova.
3 Dilia ode gafeyale ganodini osoboga hawa: bugima, dilia waini sagai amoda damuni fasima, amola ha: i manu faima.
Pa zaka zisanu ndi chimodzi muzikalima minda yanu, ndipo kwa zaka zisanu ndi chimodzi muzikasadza mitengo yanu ya mpesa ndi kuthyola zipatso zake.
4 Be ode fesuga, dilia soge hedofasima. Amo ode da Hina Gode Ea nodoma: ne ilegei dagoi. Dilia ifabia hawa: mae sagama amola dilia waini efe amoda mae damuni fasima.
Koma chaka chachisanu ndi chiwiri ndi chaka choti nthaka ipume, chaka cha Sabata la Yehova. Musalime mʼminda yanu kapena kusadza mitengo yanu ya mpesa.
5 Gagoma da hisu heda: sea, amo mae faima. Amola dilia waini sagai (amoda hame damuni fasi) amoga waini fage mae faima. Bai amo ode da helefisudafa ode.
Musakolole zimene zinamera zokha mʼmunda mwanu. Musakakolole kapena kuthyola mphesa za mʼmitengo imene simunasadze. Chaka chimenechi nʼchoti nthaka ipumule.
6
Chaka chimene nthakayo ipumula mudzakhala ndi chakudya chokwanira inuyo, akapolo anu aamuna ndi aakazi, antchito ndi alendo okhala nanu.
7 Amo ode ganodini, osobo da hame dogoi ba: mu. Be dilia amola dilia udigili hawa: hamosu dunu amola bidi lamusa: hawa: hamosu dunu amola ga fi dunu dilima gilisili esala, amola dilia lai gebo amola sigua ohe amo da dilia sogega ha: i manu defele ba: mu. Ha: i manu liligi huluane dilia sogega heda: lebe, amo manu da defea.
Ziweto zanu pamodzi ndi nyama za mʼdziko lanu zizidzadya zipatso za mʼnthaka.
8 Dilia da ode fesuale amo idili, amo fesuale agoane asili, ode49 asi dagoi ba: mu.
“‘Muzichotsera Masabata asanu ndi awiri a zaka, ndi kuchulukitsa zaka zisanu ndi ziwiri kasanu ndi kawirinso kuti Masabata asanu ndi awiri a zakawo akwane zaka 49.
9 Amo odega (ode50) eso nabu oubi fesuga, Bu Gousa: su Esoga, dunu amo da soge huluane ganodini ‘dalabede’ duma: ne asunasima.
Ndipo pa tsiku la khumi la mwezi wachisanu ndi chiwiri mulize lipenga mofuwula. Tsiku lochita mwambo wopepesera machimo muziliza lipenga mʼdziko lanu lonse.
10 Dilia agoane hamosea, ode50amoga hahawane udigili ahoasu hou, sogega esalebe dunu huluane ilima ilegemu. Amo ode ganodini, soge huluane amo da eno dunuma bidi lai galea, amo soge ea musa: ada o egaga fi ilima bu ima: ne sia: ma. Amola nowa da udigili hawa: hamomusa: enoga bidi lai esalea, amo da ea fidafama buhagima: ne, logo doasima.
Mupatule chaka cha makumi asanu, ndipo mulengeze kuti pakhale ufulu mʼdziko lonse kwa onse amene ali mʼmenemo. Kwa inu chakachi chidzakhala choyimba lipenga la chikondwerero. Aliyense wa inu adzayenera kubwerera pa munda wake, ndipo aliyense wa inu adzabwerera ku fuko lake.
11 Dilia amo ode ganodini, dilia sogega hawa: mae bugima, gagoma hisu heda: lebe, amo mae faima, amola dilia waini sagai (amoda hame damuni fasi) amoga fage mae faima.
Kwa inu chakachi chidzakhaladi chaka choyimba lipenga kukondwerera zaka makumi asanu. Pa chaka chimenechi musadzale kanthu ndipo musakolole mbewu zomera zokha kapenanso kuthyola mphesa pa mitengo yosasadzira.
12 Amo ode huluane da sema hamoi dagoi ode. Ha: i manu da dilia sogega hisu heda: beba: le, amo fawane moma.
Chimenechi ndi chaka chokondwerera zaka makumi asanu. Choncho chikhale chaka chopatulika kwa inu. Muzidya zokhazo zimene zakololedwa mʼminda.
13 Amo ode ganodini, soge huluane amo da eno dunuma bidi lai galea, ea musa: ada ema ima.
“‘Chaka chimenechi ndi choliza lipenga, kukondwerera zaka makumi asanu, ndipo aliyense abwerere pa malo ake.
14 Amaiba: le, dilia da dilia Isala: ili na: iyado ilima osobo bidi lasea, moloiwane hamoma.
“‘Ngati unagulitsa kapena kugula malo ako kwa mnzako wa mʼdzikomo, pasakhale kuchenjeretsana.
15 Bidi lasu defei amo da ode asili Bu Sagosu Ode amoga doaga: su idi amo defele ilegemu da defea.
Ugule kwa mnzako potsata chiwerengero cha zaka zimene zatha kuyambira pa chikondwerero cha chaka cha makumi asanu chapita. Ndipo mnzakoyo akugulitse potsata chiwerengero cha zaka zokolola zomwe zatsala.
16 Bu Sagosu Ode doaga: ma: ne, ode bagohame gala ba: sea, bidi lasu defei da bagade hamoma. Be ode bagahame fawane gala ba: sea, bidi lasu defei da fonobahadi ba: mu. Bai ode amoga ha: i manu faimu gala, amo ea idi amoga dilia bidi laha.
Zaka zikakhala zochuluka, uwonjezere mtengo, ndipo zaka zikakhala zochepa, uchepetse mtengo, pakuti chimene iye akukugulitsa ndi zaka zokolola.
17 Dilia Isala: ili na: iyado dunu ilima mae ogogoma. Be dilia Hina Godema beda: ma!”
Musachenjeretsane koma muope Mulungu wanu. Ine ndine Yehova Mulungu wanu.
18 “Dilia soge amo ganodini gaga: iwane esaloma: ne, Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i liligi amola sema huluane noga: le nabima.
“‘Tsatirani malangizo anga ndipo mverani mosamala malamulo anga ndipo mudzakhala mʼdzikomo mwamtendere.
19 Dilia soge da ha: i manu noga: le legemu. Dilia hanai defele, dilia da ha: i manu lamu amola soge ganodini gaga: iwane esalumu.
Ndipo nthaka idzakupatsani zipatso zake. Mudzadya mpaka kukhuta ndiponso mudzakhala mʼdzikomo mwamtendere.
20 Be dunu afae da agoane adole ba: ma: bela: le, ‘Ninia da ode fesu amoga ha: i manu hame bugisia amola hame faisia, adi moma: bela: ?
Mwina nʼkafunsa kuti, ‘Kodi chaka chachisanu ndi chiwiri tidzadya chiyani ngati sitidzala kapena kukolola mbewu zathu?’
21 ‘Na, Hina Gode, da ode gafe amoga dilia soge amo ganodini hahawane hamomuba: le, dilia sogega ha: i manu ode adunaga moma: ne defele da heda: mu.
Ine ndidzatumiza madalitso ambiri chaka chachisanu ndi chimodzi moti nthaka yanu idzabala zinthu zokwanira kudya zaka zitatu.
22 Dilia ode godo ganodini ha: i manu bu bugisia, dilia ha: i manu ode gafe ganodini fai, amo nanebe ba: mu. Amola amo ha: i manu da mae dagole, dilia da ode godo bugi liligi faili manu.
Pamene mukudzala chaka chachisanu ndi chitatu, muzidzadya chakudya chogonera ndipo mudzapitirira kudya mpaka nthawi yokolola mʼchaka chachisanu ndi chinayi.
23 Dilia soge da dilia sogedafa hame. Amaiba: le, eno dunu amoma bidi lamudafa da hamedei. Dilia soge da Gode Ea soge. Dilia da amo sogega ouligisu dunu fawane.
“‘Malo asagulitsidwe mpaka muyaya chifukwa dzikolo ndi langa. Inu ndinu alendo okhala ndi Ine.
24 Dilia da soge amo bidi lasea, musa: soge eda amo hi lamu defele gala. Amo noga: le dawa: ma!
Malo onse amene ali mʼmanja mwanu mudzalole kuti amene anakugulitsani awawombole.
25 Isala: ili dunu da hame gaguiba: le, ili esaloma: ne ea soge bidi lamu amo fawane da logo galea, e gadenenedafa sosogo fi dunu fawane lamu da defea.
“‘Ngati Mwisraeli mnzanu wasauka nagulitsako gawo lina la malo ake, mʼbale wake wapaphata abwere kudzawombola malo amene mʼbale wakeyo wagulitsa.
26 Be dunu da gadenene sosogo fi dunu hame galea, e da fa: no muni eno lasea, hi bu lamu defele agoane ba: mu.
Koma ngati munthuyo alibe wachibale woti nʼkuwombola malowo koma pambuyo pake iye mwini nʼkulemera ndi kupeza zokwanira kuwombolera, awombole malowo.
27 Amai galea, e da ea musa: soge lai dunuma dabe amo ode da asili Bu Sagosu Ode amoga doaga: mu amo ea idi defele ima: ne sia: ma. Bai e da soge bu hame bidi lai ganiaba, e da Bu Sagosu Ode amoga udigili lala: loba.
Awerengerane zaka kuyambira pamene anagulitsa mundawo ndipo amubwezere amene anagulayo ndalama zimene akanayenera kuzipereka mpaka chaka chokondwerera zaka makumi asanu. Atatero angathe kubwerera pa malo ake.
28 Be e da ea soge bu bidi lamu defele hame ba: sea, soge bidi lai dunu da amo soge gagulaligimu. Amola Bu Sagosu Ode amoga, e da udigili musa: gagui dunuma imunu.
Koma ngati sakhala nazo zokwanira kuti amubwezere amene anagula malowo, gawo limene anagulitsalo lidzakhala mʼmanja mwa munthu amene anagulayo mpaka chaka chokondwerera zaka makumi asanu. Malowo adzabwezedwa chaka chimenechi, ndipo iye adzatha kubwerera pa malo ake.
29 Dunu da diasu gagili sali moilai amo ganodini gala, amo bidi lasea, e da ode afae amoga bu bidi lamusa: dawa: sea, bu bidi lamu da defea.
“‘Ngati munthu agulitsa nyumba ya mu mzinda umene uli mu linga, angathe kuyiwombola nyumbayo chisanathe chaka chathunthu chigulitsire. Mu nthawi imeneyi wogulitsayo atha kuyiwombola.
30 Be amo ode ganodini, e da ea diasu bu hame bidi lasea, amo diasu da gaheabolo gagui dunu amola egaga fi dunu ilia diasudafa ba: ma: mu. Musa: gagui dunu da Bu Sagosu Ode amoga, amo diasu bu hame samogemu.
Ngati nyumbayo siwomboledwa chisanathe chaka chimodzicho, nyumbayo idzakhala ya amene anagulayo ndi zidzukulu zake mpaka muyaya. Sidzabwezedwanso kwa mwini wake mʼchaka chokondwerera zaka makumi asanu.
31 Be hou amo diasu hame gagili sali moilai ganodini dialebe da bugili nasu sogebi ea hou defele ba: mu. Musa: eda da bu bidi lamusa: dawa: sea, e da bu bidi lamu da defea, amola Bu Sagosu Ode amoga, gagui dunu da amo diasu ea musa: eda ema udigili bu imunu.
Koma nyumba za mʼmizinda yosazingidwa ndi linga ziwomboledwe monga mmene achitira ndi minda ya mʼdzikomo.
32 Be Lifai dunu da moilai bai bagade ilima ilegei amo ganodini ilia soge o diasu enoga lai amo bu samogene bidi lamusa: dawa: sea, ilia bu bidi lamu da defea.
“‘Alevi ali ndi ufulu owombola nyumba zawo za mʼmidzi yawo nthawi ina iliyonse.
33 Amo moilai ganodini, Lifai dunu da diasu bidi lasea amola bu samogene hame bidi lasea, amo diasu Bu Sagosu Ode ganodini, Lifai dunuma bu udigili ima: mu. Bai diasu amo da Lifai dunu ilia moilai ganodini gagubi amo da Lifai dunu ilia: fawane.
Koma ngati Mlevi sawombola nyumba imene inagulitsidwa mʼmudzi mwake, ndiye kuti idzabwezedwe mʼchaka choliza lipenga pokondwerera zaka makumi asanu, popeza nyumba zimenezi zili mʼmidzi ya Alevi ndi yawo pakati pa Aisraeli.
34 Be ohe ha: i nasu soge, Lifai dunu ilia moilai sisiga: le diala, amo da hamedafa bidi lamu. Bai amo soge da Lifai dunu ilia eso huluane gaguma: ne dialumu.
Koma malo owetera ziweto a mʼmidzi yawoyo sayenera kugulitsidwa. Awa ndi malo awo mpaka muyaya.
35 Dilia Isala: ili na: iyado dunu dili gadenene esala da hame gaguiwane hamosea amola ea labe lamu hamedei ba: sea, dilia bidi lamusa: hawa: hamosu dunu defele, e da dilima gadenene esaloma: ne, ema ima.
“‘Ngati mʼbale wako akhala wosauka kuti sangathe kudzisamalira yekha, umuthandize. Ukhale naye ngati mlendo kapena ngati munthu amene ukhala naye kwa kanthawi.
36 Bidi bu ima: ne iabeba: le, amoga dabe eno mae lama. Be Gode Ea sia: nabima amola e da dilima bu gadenene esaloma: ne, logo doasima.
Usalandire chiwongoladzanja chilichonse kuchokera kwa iye kapena kuwonjezerapo kanthu kena, koma uziopa Mulungu kuti mʼbale wakoyo akhale nawe.
37 Dilia ema bidi bu ima: ne iasea, amoga dabe eno mae lama amola ema ha: i manu bidi lasea, amo ha: i manu ea lasu ilegei defele fawane lama.
Musakongoze mnzanu ndalama kuti mulandire chiwongoladzanja, kapena kumugulitsa chakudya kuti mupeze phindu.
38 Bai amo da dilia Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i gala. Hina Gode da dilima Ga: ina: ne soge ima: ne, amola dilia Hina Gode esaloma: ne, dili Idibidi sogega fisili masa: ne asunasi dagoi.
Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndinakutulutsani mʼdziko la Igupto kuti ndikupatseni dziko la Kanaani ndi kuti ndikhale Mulungu wanu.
39 Dilia Isala: ili na: iyado dunu dilia fi amo ganodini esala da ea bidi fisili, hame gagui hamoiba: le, dilia udigili hawa: hamomusa: gini dilima ea da: i bidi lasea, ema udigili hawa: hamosu dunu defele hamoma: ne mae sia: ma.
“‘Ngati mʼbale wanu asauka ndipo adzigulitsa yekha kwa inu, musamugwiritse ntchito ngati kapolo.
40 E da dia bidiga hawa: hamosu dunu defele dia hawa: hamonanu, Bu Sagosu Ode amoga yolesimu.
Akhale ngati wantchito kapena ngati mlendo. Akugwirireni ntchito mpaka chaka chokondwerera zaka makumi asanu.
41 Amo odega, e amola ea mano da di yolesili, ea fidafa amola ea aowalali ilia soge amoga buhagima: ne yolesima.
Kenaka iye ndi ana ake achoke, ndipo apite ku fuko lake ndi kubwerera ku malo a makolo ake.
42 Isala: ili dunu ilia da Hina Gode Ea udigili hawa: hamosu dunu. E da ili Idibidi sogega guiguda: oule misi. Amaiba: le, Isala: ili fi dunu amo eno dunuma ea udigili hawa: hamomusa: bidi lamu da sema gala.
Chifukwa Aisraeli ndi atumiki anga amene ndinawatulutsa mʼdziko la Igupto, asagulitsidwe ngati akapolo.
43 Ilima ougiliwane mae hamoma. Be Godema beda: ma.
Musawalamulire mwankhanza koma wopani Mulungu wanu.
44 Dilia da udigili hawa: hamosu dunu lamu hanai galea, fifi asi gala dilima sisiga: le esala amoga bidi lama.
“‘Kunena za akapolo aamuna ndi aakazi, amenewa mungathe kuwagula kuchokera kwa mitundu ya anthu imene yakuzungulirani.
45 Amola ga fi dunu dilima gilisili esalea, ilia mano amo dilia udigili hawa: hamomusa: gini lamu da defea. Amo mano dilia sogega lalelegei, amo dilia gagui liligi hamoma: ne lamu da defea.
Mungathenso kugula akapolo kuchokera kwa alendo amene akukhala nanu kapena kuchokera ku mabanja amene mukukhala nawo amene ndi mbadwa za mʼdziko lanu. Iwowa akhoza kukhala akapolo anu.
46 Amola dilia bogosea, dilia mano da amo udigili hawa: hamosu dunu lama: ne sia: ma. Be dilia Isala: ili na: iyado dunu ilima ougili mae hamoma.
Akapolowo mungathe kuwasiya mʼmanja mwa ana anu inu mutafa kuti akhale cholowa chawo moyo wawo wonse. Koma musawalamulire mwankhanza Aisraeli anzanu.
47 Ga fi dunu dili amola gilisili esalebe da bagade gaguiwane ba: sea, amola dilia Isala: ili na: iyado dunu da hame gaguiba: le, ea da: i amo ga fi dunu o ea sosogo fi dunu ilima bidi lasea,
“‘Ngati mlendo kapena munthu amene akukhala nanu kwa kanthawi kochepa alemera ndipo mmodzi wa abale anu amene akukhala naye pafupi nʼkusauka, nadzigulitsa yekha kwa mlendo amene akukhala pakati panuyo kapena kwa mmodzi wa fuko la munthu wongokhala pafupi nayeyo,
wodzigulitsayo ali ndi ufulu wowomboledwa. Mmodzi mwa abale ake angathe kumuwombola:
49 fa: no ea ola o eya ea adabi amola daiya o ea gawia o ea fidafa dunu da e bu bidi lamusa: dawa: sea, amo da e bu samogene lama: ne logo doasima: mu. O hi da bidi lale bu hi da: i bidi lamu da defea.
amalume ake kapena mwana wa amalume ake, kapena wachibale wa mu fuko lake. Kapena ngati iye mwini alemera, atha kudziwombola yekha.
50 E da ga fi dunu ea da: i bidi lai, ema fada: i fofada: ma: mu. Amasea, ela da ode amoga ea bidi lai ode asili Bu Sagosu Ode amoga doaga: ma: ne idimu. Amola e bu yolesima: ne, dabe da bidiga hawa: hamosu dunuma iasu defele ilegemu.
Iye pamodzi ndi munthu amene anamugulayo awerengerane kuyambira chaka chimene anadzigulitsa kwa iyeyo mpaka chaka chokondwerera zaka makumi asanu. Mtengo wodziwombolera ukhale wofanana ndi zakazo. Ndipo nthawi imene anali ndi mbuye wakeyo iwerengedwe ngati nthawi ya munthu wantchito.
51 Dunu da dunu fi enoga bidiga lai, be ea fi dunu ili da e bu bidiga lamu hanai. Amaiba: le, ilia da Bu Sagosu Ode doaga: ma: ne, ea hawa: hamosu esalumu ode fisiagai amo fawane idilalu, bidi imunu. Amo bidi defei da dunu ea odega hawa: hamosu bidi defele ba: mu, amola ea hina da ema ougiliwane hamomu da sema bagade.
Ngati patsala zaka zambiri, iye ayenera kulipira mtengo woposera umene anamugulira.
Ngati kwatsala zaka zochepa kuti ifike nthawi ya chaka chokondwerera zaka makumi asanu, iye awerengerane ndi mbuye wake, ndipo apereke ndalama za zowomboledwera molingana ndi zaka zotsalazo.
Azikhala naye ngati wantchito wolembedwa chaka ndi chaka. Ndipo muonetsetse kuti mbuye wakeyo sakumulamulira mwankhanza.
54 Be e da amo hou defele ea udigili hawa: hamosu hame yolesea, e da Bu Sagosu Ode amoga hahawane yolesima: ne logo doasima: ne sia: ma.
“‘Ngakhale munthuyo atapanda kuwomboledwa mwa njira zimenezi, iye ndi ana ake ayenera kumasulidwa mʼchaka chokondwerera zaka makumi asanu,
55 Isala: ili dunu da eso huluane udigili hawa: hamosu dunu esalumu da hamedei. Bai ilia da Hina Gode Ea udigili hawa: hamosu dunu esala. E da ili Idibidi sogega fisili masa: ne guiguda: oule misi. E da ilia Hina Gode!
pakuti Aisraeli ndi atumiki anga. Iwo ndi atumiki anga amene ndinawatulutsa mʼdziko la Igupto. Ine ndine Yehova Mulungu wanu.

< Gobele Salasu 25 >