< Gobele Salasu 22 >

1 Hina Gode da Mousesema, e da Elane amola egefela elama amane sia: ma: ne sia: i, “Na Dio mae wadela: ma! Amaiba: le, sema iasu amo da Isala: ili dunu da Nama ima: ne ilegesa, amo nodone dawa: ma. Na da Hina Gode!
Yehova anawuza Mose kuti,
2
“Uza Aaroni ndi ana ake kuti azilemekeza zinthu zopatulika zimene Aisraeli azipereka kwa Ine, kuti asayipitse dzina langa loyera. Ine ndine Yehova.
3 Diligaga fi dunu afae da ledo gala hamoi galea, amola e da sema iasu amo Isala: ili dunu da Nama ima: ne ilegei, amo gadenene masea, e bu oloda hawa: hamosu hamoma: ne hamedafa heda: mu. Amo sema da eso huluane dialumu. Na da Hina Gode!
“Uwawuze kuti ngati wina aliyense mwa zidzukulu zawo mʼmibado yonse imene ikubwera adzayandikira zinthu zopatulika zimene ana a Israeli apereka kwa Yehova, ali wodetsedwa, ameneyo achotsedwe pamaso pa Yehova. Ine ndine Yehova.
4
“Munthu aliyense mwa zidzukulu za Aaroni amene ali ndi khate kapena amatulutsa zoyipa mʼthupi mwake, asadye zinthu zopatulika mpaka atayeretsedwa. Wansembe angakhale wodetsedwa atakhudzana ndi chinthu chimene chadetsedwa ndi chinthu chakufa kapena kukhudza munthu amene wataya umuna,
5 Elane egaga fi dunu da gadofo olo bagade madelasea o ea da: i amoga guhi gadili ahoasea, e da sema iasu ha: i manu amo hame manu. E da ledo gala hamoiba: le, bu ledo hamedei ba: sea fawane bu manu. Gobele salasu dunu da ledo gala liligi (amo da bogoi da: i hodo gadenene dialu) amo digili ba: sea o ea da: iga ami gadili ahoasea, o e da ledo gala ohe o dunu digili ba: sea, e amola da ledo gala hamoi dagoi ba: mu.
kapena kukhudza chilichonse chokwawa chomwe chimadetsa munthu, kapena kukhudza munthu amene angamudetse, kapenanso kukhudza kanthu kena kalikonse kodetsedwa.
6 Gobele salasu dunu da agoai hamosea, e da ledo hamone, daeya doaga: sea fawane bu ledo hamedei ba: mu. Be amogala e da sema ha: i manu iasu manusa: dawa: sea, e da hidadea hano ulimu.
Tsono ngati wansembe angakhudze chilichonse mwa zimenezi ndiye kuti adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo. Asadye chopereka chilichonse chopatulika mpaka atasamba thupi lake lonse.
7 Eso dasea, e da sema dodofei dagoi ba: mu. Amasea, e da sema ha: i manu iasu (amo da ea ha: i manu) amo manu da defea.
Munthuyo adzakhala woyeretsedwa pamene dzuwa lalowa, ndipo angathe kudya chopereka chopatulikacho popeza ndi chakudya chake.
8 E da ohe amo da hisu bogoi o sigua amoga medole legei, amo ea hu hame manu - sema gala. Agoai hamoi ganiaba, e da ledo gala hamona: noba. Na da Hina Gode!
Wansembe sayenera kudya chinthu chofa chokha kapena chojiwa ndi chirombo kuopa kuti angadzidetse ndi chakudyacho. Ine ndine Yehova.
9 Gobele salasu dunu huluane da hamoma: ne sia: i Na iligili i, amo noga: le fa: no bobogema: ma. Agoane hame hamomu ganiaba, ilia da wadela: le hamoiba: le, bogola: loba. Bai ilia da Na hamoma: ne sia: i i, amo hame nabala: loba. Na da Hina Gode amola Na da ili hadigima: ne hamosa.
“‘Choncho ansembe azisunga malamulo angawa kuti asapezeke wolakwa ndi kufa chifukwa chopeputsa malamulowa. Ine ndine Yehova, amene ndimawayeretsa.
10 Gobele salasu fi dunu fawane da sema ha: i manu iasu manu da defea. Eno dunu huluane (amola nowa da gobele salasu dunu ea diasu ganodini esala o ea hawa: hamosu dunu), ilia da hamedafa manu - sema bagade.
“‘Aliyense amene si wabanja la wansembe, kaya ndi mlendo wa wansembe, kapena wantchito wake, asadye chopereka chopatulika.
11 Be gobele salasu dunu ea udigili hawa: hamosu dunu (ea muniga bidi lai o ea diasu ganodini lalelegei), ilia da ha: i manu gobele salasu dunuma i, amo manu da defea.
Koma kapolo amene wagulidwa ndi ndalama kapena kubadwira mʼbanja la wansembe angathe kudya chakudya cha wansembeyo.
12 Gobele salasu dunu ea idiwi amo da hame gobele salasu dunu amoma fisia, da sema ha: i manu iasu amo hame manu.
Mwana wamkazi wa wansembe amene wakwatiwa ndi munthu amene si wansembe, asadyeko nsembe zopatulikazo.
13 Be gobele salasu dunu ea idiwi amo da didalo hamoi o dunuga fisiagai, amo da mano hame amola ea eda bu ouligima: ne ea diasuga bu masea, e da sema ha: i manu ea gobele salasu eda hi iabe amo manu da defea.
Koma mwana wamkazi wa wansembe amene ali wamasiye kapena wosudzulidwa, ndipo alibe mwana, komanso anabwerera ku nyumba ya abambo ake monga pa nthawi ya utsikana wake, angathe kudya chakudya cha abambo ake. Mlendo asadye chakudya chopatulika.
14 Be dunu eno (amo da gobele salasu dunu ea sosogo fi dunu hame) amo da mae dawa: le, sema ha: i manu iasu mogili nasea, e da amo ea bidi lasu idi defele amola20% eno amo gobele salasu dunuma bu dabe imunu.
“‘Ngati munthu wina aliyense adya chopereka chopatulika mosadziwa, munthuyo amubwezere wansembe chinthu chopatulikacho ndipo awonjezerepo limodzi la magawo asanu a chinthucho.
Choncho ansembe asayipitse zopereka zopatulika za Aisraeli zimene apereka kwa Yehova
16 Gobele salasu dunu da sema ha: i manu iasu amo ledo gala hamosa: besa: le, ilia da eno hame ilegei dunu amo moma: ne, logo hame doasima: mu. Bai amo hame ilegei dunu da wadela: i hou hamomu ganiaba, se iasu ba: mu ganuma: loba. Na da Hina Gode amola Na da gobele salasu iasu liligi hadigi hamoma: ne hamosa.
ndipo asachimwitse ndi kupalamulitsa Aisraeli powalola kudya zakudya zawo zopatulika. Ine ndine Yehova amene ndimawayeretsa.’”
Yehova anawuza Mose kuti,
18 Hina Gode da Mousesema e da Elane, egefela amola Isala: ili dunu huluane ilima hamoma: ne sia: i hagudu dedei ilima olelema: ne sia: i. “Isala: ili dunu o ga fi Isala: ili soge ganodini esala, amo da Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu gobele salasu iasea (e da amo ima: ne ilegei o Godema hahawaneba: le udigili iaha) e da ohe noga: idafa wadela: i hame gala fawane ima: ne sia: ma.
“Yankhula ndi Aaroni, ana ake pamodzi ndi Aisraeli onse, ndipo uwawuze kuti, ‘Ngati wina aliyense wa inu, Mwisraeli kapena mlendo amene akukhala mu Israeli abwera ndi mphatso ya nsembe yopsereza kwa Yehova, kupereka chimene analumbira kapena kuti ikhale nsembe yaufulu,
19 Ohe amo da gawali amola wadela: i hamedafa gala, amo fawane imunu.
ndiye kuti abwere ndi ngʼombe yayimuna, nkhosa yayimuna kapena mbuzi yayimuna. Izi zikhale zopanda chilema kuti zilandiridwe.
20 Be dilia da wadela: i gala ohe amo imunusa: dawa: sea, Hina Gode da amo iasu hame lamu.
Musapereke nyama iliyonse yokhala ndi chilema chifukwa sidzalandiridwa mʼmalo mwanu.
21 Nowa da Hahawane Gilisili Olofole Iasu Hina Godema imunusa: dawa: sea, (e da amo imunusa: ilegei o Godema hahawaneba: le, udigili iaha) amo ohe amola da wadela: i hame gala liligi fawane ima.
Pamene wina aliyense abweretsa ngʼombe kapena nkhosa kuti ikhale nsembe yachiyanjano kwa Yehova, kukwaniritsa zimene analumbira kapena kuti ikhale nsembe yaufulu, nyamayo iyenera kukhala yangwiro ndi yopanda chilema kuti ilandiridwe.
22 Ohe amo da si dofoi o emo gasuga: igi o fofa: gi o aiya o baho gala, agoai ohe Hina Godema mae ima. Amola agoai ohe amo ha: i manu iasu oloda da: iya mae gobesima.
Musapereke kwa Yehova nyama zakhungu, zovulala kapena zolumala, kapena nyama zimene zikutulutsa mafinya mʼthupi mwake, kapena zimene zili ndi nthenda yonyerenyetsa, kapena zimene zili ndi mphere. Nyama zotere musaziyike pa guwa kuti zikhale nsembe yopsereza kwa Yehova.
23 Dilia ohe amo da noga: le hame alei o fonobahadi wadela: i amo hahawane udigili iasu agoane imunu da defea, be gobele salasu ilegei agoane mae ima.
Koma mungathe kupereka ngʼombe yayimuna kapena nkhosa imene ili ndi chiwalo chachitali kapena chachifupi kukhala nsembe yaufulu. Koma simungayipereke ngati nsembe yoperekera zimene munalumbirira chifukwa sidzalandiridwa.
24 Amola ohe amo ea gulusu da lologoi o fa: ginisi o fofonomai o danai, agoai ohe Hina Godema mae ima. Isala: ili soge ganodini, amo iasu hou da sema bagade.
Nyama iliyonse imene mavalo ake ndi onyuka kapena ophwanyika, ongʼambika kapena oduka, musamayipereke kwa Yehova mʼdziko lanu.
25 Dilia ha: i manu iasu imunusa: , ohe amo dilia da ga fi amoga lai mae ima. Hina Gode da amo ohe da wadela: i ba: mu, amola e da amo hame lamu.
Ndipo musalandire nyama zotere kuchokera kwa mlendo ndi kuzipereka kukhala zakudya za Mulungu wanu. Zimenezi sizidzalandiridwa mʼmalo mwanu chifukwa zili ndi chilema ndipo ndi zolumala.’”
Yehova anawuza Mose kuti,
27 Bulamagau mano o sibi mano o goudi mano da lalelegesea, e da ea ame amola gilisili eso fesuale esalumu. Amalalu, amo lale, ha: i manu gobele iasu hamoma: ne imunu da defea.
“Pamene mwana wangʼombe, mwana wankhosa kapena mwana wambuzi wabadwa, akhale ndi make kwa masiku asanu ndi awiri. Kuyambira tsiku lachisanu ndi chitatu mpaka mʼtsogolo mwake, angathe kulandiridwa kuti akhale nsembe yopsereza ya kwa Yehova.
28 Bulamagau amola ea mano o sibi amola ea mano o goudi amola ea mano amo eso afaega gilisili gobele salasu hamomusa: mae hamoma.
Musaphe ngʼombe kapena nkhosa pamodzi ndi mwana wake tsiku limodzi. Muyidye pa tsiku lomwelo; musasiyeko ina mpaka mmawa. Ine ndine Yehova.
29 Hina Gode da dili hahawane gousa: ma: ne, dilia Ema nodomusa: gobele salasu iasea, sema hamoi amo noga: le fa: no bobogema.
“Pamene mupereka nsembe yoyamika kwa Yehova, muyipereke mwakufuna kwanu mu njira yoti ilandiridwe mʼmalo mwanu.
30 Amo ha: i manu iabe goe, eso amoga dilima i, amoga fawane moma. Golale hahabe manusa: , mae yolesima.
Muyidye pa tsiku lomwelo, wosasiyako ina mpaka mmawa. Ine ndine Yehova.
31 Hina Gode da amane sia: i, “Na sema amo nabawane hamoma! Na da Hina Gode!
“Choncho sungani malamulo anga ndi kuwatsatira. Ine ndine Yehova.
32 Na Hadigi Dio amo mae wadela: ma. Isala: ili dunu huluane da Na Hadigi amo sia: ma: mu. Na da Hina Gode amola Na da dilia hadigi hamoma: ne hamosa.
Musanyoze dzina langa loyera. Koma lilemekezedwe pakati pa Aisraeli. Ine ndine Yehova amene ndimakuyeretsani
33 Na da dilia Gode esaloma: ne, dili Idibidi sogega fisili masa: ne asunasi. Na da Hina Gode!
ndipo ndine amene ndinakutulutsani mu Igupto kuti ndikhale Mulungu wanu. Ine ndine Yehova.”

< Gobele Salasu 22 >