< Bisisu 9 >

1 Gidione egefe amo Abimelege (Gidione ea gidisedagi uda ea mano) da Siegeme moilai bai bagadega asi. Ea ame ea sosogo fi da amogawi esalu. E da ilima amane sia: i,
Abimeleki mwana wa Yeru-Baala anapita ku Sekemu kwa abale a amayi ake ndi kukawawuza iwowo ndi fuko lonse la banja la abambo a amayi ake kuti,
2 “Siegeme dunu ilima amane adole ba: ma, ‘Dilima ouligisuwane esaloma: ne dilia da nowa hanabela: ? Gidione egefe70da dilima ouligisu esalumu da defeala: ? O dunu afadafa fawane da defeala: ? Mae gogolema! Abimelege da dilia fidafa dunu. Dilia hu amola maga: me afadafa fawane hamoi galu.’”
“Funsani nzika zonse za ku Sekemu kuno, ‘Chabwino ndi chiyani kwa inu kuti ana onse makumi asanu ndi awiri a Yeru-Baala azikulamulirani, kapena kuti azikulamulirani ndi munthu mmodzi basi?’ Kumbukirani kuti ine ndine mʼbale wanu weniweni.”
3 Abimelege ame ea sosogo fi da amo sia: Siegeme dunuma sia: dasu. Amola Siegeme dunu da Abimelege ema fa: no bobogemusa: dawa: i galu. Bai Abimelege da ilia sosogo fi dunu esalu, ilia ba: i.
Abale a amayi akewo anamuyankhulira mawu amenewa kwa nzika zonse za ku Sekemu, ndipo mitima ya anthu onse inali pa Abimeleki chifukwa anati, “Uyu ndi mʼbale wathu,”
4 Ilia da Ba: ile gousa: su hamoi amo ea debolo diasuga, muni silifa fage 70 agoane lale, Abimelegema i. Abimelege da hamedei wadela: i hamosu dunu e fidima: ne sia: i amola, ilima amo muni i.
Tsono anamupatsa ndalama zasiliva 70 za mʼnyumba ya chipembedzo ya Baala Beriti. Ndi ndalama zimenezi Abimeleki analemba anthu achabechabe ndi osasamala kuti azimutsatira.
5 E da ea ada diasu Ofala moilai bai bagadega dialu amoga asili, igi afae amo da: iya ea yolali (Gidione egefe) 70 agoane huluane medole legei dagoi. Be Youda: me (Gidione ea ufidafa mano) da wamoaligili, esalebe ba: i.
Anapita ku Ofiri ku mudzi kwa abambo ake ndipo anapha abale ake makumi asanu ndi awiri, ana a Yeru-Baala pa mwala umodzi. Koma Yotamu yemwe anali wamngʼono mwa onsewo anapulumuka chifukwa anabisala.
6 Amalalu, Siegeme dunu huluane da gilisili, sema ouge ifa Siegeme sogega lelu amoga asili, Abimelege hina bagade ilegei dagoi.
Tsono nzika za ku Sekemu ndi za ku Beti-Milo zinapita kukasonkhana ku mtengo wa thundu pafupi ndi chipilala cha ku Sekemu kuti akalonge Abimeleki ufumu.
7 Youda: me da amo sia: nababeba: le, asili, Gelesime Goumi amo da: iya gado lelu, amane wele sia: i, “Dilia Siegeme dunu! Na sia: nabima! Amasea, Gode da dilia sia: nabima: bela: ?
Yotamu atamva izi anapita kukayima pamwamba pa phiri la Gerizimu ndipo anafuwula nati, “Tandimverani inu anthu a ku Sekemu, kuti Mulungu akumvereninso.
8 Eso afaega, ifa huluane da gilisili, ilia hina bagade ilegema: ne gilisi. Ilia da olife ifa amoma amane sia: i, ‘Di ninia hina bagade hamoma.’
Tsiku lina mitengo inapita kukadzoza mfumu yawo. Tsono mitengoyo inati kwa mtengo wa olivi, ‘Iwe ukhale mfumu yathu.’”
9 Be olife ifa da bu adole i, ‘Hame mabu! Na fage amoga dunu ilia susuligi amo ‘gode’ amola osobo bagade dunu ilima nodomusa: laha. Be na da dili ouligisia, susuligi bu hamomu da hamedeiwane ba: mu.’
“Koma mtengo wa olivi uja unayankha kuti, ‘Kodi ndisiye mafuta angawa amene amalemekezera nawo milungu ndi anthu omwe, kuti ndizikalamulira mitengo?’”
10 Amalalu, ifa eno ilia da figi ifa amoma amane sia: i, ‘Di misini, ninia hina bagade hamoma.’
Apo mitengo inawuza mtengo wa mkuyu kuti, “Bwera ndiwe ukhale mfumu yathu.”
11 Be figi ifa da bu adole i, ‘Hame mabu! Na da dili ouligisia, noga: i hedai fage bu legemu da hamedeiwane ba: mu.’
Koma mtengo wa mkuyu unayankha kuti, “Kodi ndisiye chipatso changa chokoma ndi chozunachi kuti ndizikalamulira mitengo?”
12 Amalalu, ifa ilia da waini efe amoma amane sia: i, ‘Di misini, ninia hina bagade hamoma.’
Kenaka mitengo ija inawuza mtengo wamphesa kuti, “Bwera ndiwe kuti ukhale mfumu yathu.”
13 Be waini efe da bu adole i, ‘Hame mabu! Na waini hano da ‘gode’ ili amola osobo bagade dunu amo nasea hahawane ba: sa. Be na da dilia ouligisia, waini hano bu imunu hamedeiwane ba: mu.’
Koma mtengo wamphesa unayankha kuti, “Kodi ine ndisiye vinyo wangayu, amene amasangalatsa milungu ndi anthu omwe kuti ndizikalamulira mitengo?”
14 Amalalu, ifa huluane da aya: gaga: nomei legei ifa fonobahadi amoma amane sia: i, ‘Di misa! Ninia hina bagade hamoma.’
Pomaliza mitengo yonse inawuza mkandankhuku kuti, “Bwera ndipo ukhale mfumu yathu.”
15 Aya: gaga: nomei legei ifa da bu adole i, ‘Defea! Dilia da dafawane na dilia hina bagade hamomu hanai galea, misa amola na ougia hagudua aligima. Dilia agoane hame hamosea, na aya: gaga: nomei legei amoda amoga lalu da gadili nenanebe ba: mu. Amola amo lalu da Lebanone soge dolo ifa huluane nene dagomu.’”
Mkandankhuku uja unayankha kuti, “Ngati mukufunadi kuti mudzoze ine kuti ndikhale mfumu yanu, bwerani mudzabisale mu mthunzi mwangamu, koma ngati simutero, moto utuluka kwa ine ndi kupsereza mikungudza ya ku Lebanoni.”
16 Youda: me da eno amane sia: i, “Dilia da Abimelege hina bagade hamoma: ne ilegebeba: le, noga: i amola moloiwane hamobela: ? Gidione amola ea sosogo fi da hou noga: idafa hamosu. Be dilia da amo nodone dawa: beba: le, amo hou hamobela: ?
Yotamu anatinso, “Kodi mukuti munaonetsadi kuona mtima ndi kukhulupirika podzoza Abimeleki kukhala mfumu? Kodi mukuti munachitira ulemu Yeru-Baala ndi banja lake poganizira ntchito zimene anachita?
17 Na ada da dili gaga: ma: ne fidili gegei dagoi. Amo mae gogolema! E da ea esalusu mae dawa: le, dili Midia: ne dunu ilima gaga: ma: ne fidili gegei.
Kodi suja abambo anga anakumenyerani nkhondo ndi kuyika moyo wawo pa chiswe kuti akupulumutseni mʼmanja mwa Amidiyani?
18 Be wali esoga dilia da na ada sosogo fi amo wadela: lesi dagoi. Dilia da ea mano 70 amo huluane igi afadafa da: iya medole legei dagoi. Abimelege da Gidione ea hawa: hamosu uda amo ea mano. Be e da dilia sosogo fiba: le, dilia da e Isala: ili dunu ouligima: ne, ema ilegei dagoi.
Koma lero inu mwawukira banja la abambo anga. Mwapha ana ake 70 pa mwala umodzi, ndiponso mwalonga ufumu Abimeleki, mwana wa mdzakazi wake kuti akhale wolamulira anthu a ku Sekemu chifukwa ndi mʼbale wanu.
19 Amaiba: le amo hou dilia da Gidione amola ea sosogo fi ilima wali eso hamoi, amo da hou noga: i amola moloi ba: sea, defea, dilia Abimelege ema hahawane galoma. Amola e da dilima hahawane ganumu da defea.
Tsono ngati mukuti zimene mwachitira Yeru-Baala ndi banja lake mwazichita moona mtima ndiponso mokhulupirika, ndiye mukondwere ndi Abimeleki, nayenso akondwere nanu!
20 Be amai hame galea, defea, lalu da Abimelege amoga nene, Siegeme dunu amola Bedemilou dunu nene dagoi ba: mu da defea. Amola lalu da Siegeme dunu amola Bedemilou dunu amoga nene, Abimelege amola nei dagoi ba: mu da defea.”
Koma ngati sichoncho moto utuluke mwa Abimeleki ndi kupsereza anthu a ku Sekemu ndi Beti-Milo, ndipo moto utulukenso mwa anthu a ku Sekemu ndi Beti-Milo, ndi kupsereza Abimeleki!”
21 Amalalu, Youda: me da ea ola Abimelege ema beda: iba: le, hobeale, asili, Bie sogega doaga: le, esalu.
Kenaka Yotamu anathawira ku Beeri nakakhala komweko chifukwa ankaopa Abimeleki mʼbale wake.
22 Abimelege da ode udiana amoga Isala: ili soge ouligisu.
Abimeleki atalamulira Israeli zaka zitatu,
23 Amalalu, Gode da Abimelege amola Siegeme dunu ela da sia: ga gegema: ne hamoi. Ilia da Abimelege fisili, ema ha laiwane ba: i.
Mulungu anayika chidani pakati pa Abimelekiyo ndi anthu a ku Sekemu, motero kuti anthu a ku Sekemu anawukira Abimeleki.
24 Abimelege amola Siegeme dunu (ilia da Abimelege fidi amola ea dogo denesi) ilia da Gidione ea manoni 70 agoane fufuga: i. Ilia da amo wadela: i hou se iasu dabe lama: ne, Gode da ilima afafasu hou i.
Mulungu anachita zimenezi kuti zoyipa zimene anachitira ana aamuna 70 a Yeru-Baala aja zimubwerere, ndi kuti magazi awo akhale pa Abimeleki mʼbale wawo ndi pa anthu a ku Sekemu amene anamulimbikitsa mtima kuti aphe abale akewo.
25 Siegeme dunu da goumi gadodili Abimelege fuga: ma: ne logo la: ididili wamoaligisu. Nowa dunu da logoga ahoanoba, ilia da amo dunu ilia liligi wamolasu. Eno dunu da amo hou Abimelegema olelei.
Choncho anthu a ku Sekemu anayika anthu omubisalira pamwamba pa mapiri. Tsono iwo ankalanda anthu odutsa mʼnjira imeneyo zinthu zawo ndipo Abimeleki anamva zimenezi.
26 Amalalu, Ga: ile (Ebede ea egefe) amola yolalali da Siegeme sogega misi. Siegeme dunu da ema fa: no bobogei.
Gaali mwana wa Ebedi anasamukira ku Sekemu ndi abale ake, ndipo anthu a ku Sekemuko anamukhulupirira iye.
27 Ilia huluane da ilia waini sagai amoga asili, waini fage faili, waini hano hamone, lolo nasu gilisisu hamoi. Ilia da ilia ogogosu ‘gode’ ea debolo diasu amo ganodini golili sa: ili, ha: i mai, waini hano mai amola Abimelege ea hou gadele sia: dasu.
Anthuwo anapita ku munda kukathyola mphesa ndi kuzifinya, ndipo anachita chikondwerero mʼnyumba ya milungu yawo. Anthuwo akudya ndi kumwa, ankatemberera Abimeleki.
28 Ga: ile da amane sia: i, “Ninia hou da adi houla: ? Ninia abuliba: le Abimelege ea hawa: hamosala: ? E da nowala: ? E da Gidione ea mano fawane. Sibale da ea sia: naba, be ninia da abuliba: le ema fa: no bobogesala: ? Dilia aowalalia eda amo Ha: imo da dilia fi muni hemosu. Ema fa: no bobogemu da defea.
Ndipo Gaali mwana wa Ebedi anati “Kodi Abimeleki ndi ndani, ndipo nʼchifukwa chiyani akutilamulira ife Asekemu? Kodi iyeyu si mwana wa Yeru-Baala ndipo womuthandiza wake si Zebuli? Tiyeni titumikire anthu a ku Hamori, kholo la fuko la Sekemu! Nanga nʼchifukwa chiyani tikutumikira Abimeleki?
29 Na da dilia fi ilima ouligisu ganiaba, na da Abimelege amo sefasila: loba. Na da ema, ‘Dia dadi gagui gilisisu hahamoma! Gadili asili ninima gegema!’ na da ema sia: na: noba.”
Anthu a mu mzindawo akanakhala pansi pa ulamuliro wanga, ndikanamuchotsa Abimelekiyu. Ndikanamuwuza Abimeleki kuti, ‘Wonjeza ankhondo ako ndipo ubwere tidzamenyane!’”
30 Siegeme moilai bai bagade ouligisu dunu amo Sibale, da Ga: ile ea sia: nababeba: le, mi hanai galu.
Zebuli amene ankalamulira mzindawo atamva zimene Gaali mwana wa Ebadi ananena, anakwiya kwambiri.
31 Abimelege da Aluma sogega esalu. Sibale da ema adola ahoasu dunu asunasi. Ilia da ema amane sia: i, “Ga: ile (Ebede egefe) amola yolali da Siegeme moilai bai bagadega doaga: i. Ilia da di Siegeme golili sa: imu logo ga: simu.
Anatumiza amithenga kwa Abimeleki, kukanena kuti, “Gaali mwana wa Ebedi ndi abale ake abwera ku Sekemu ndipo akuwutsa mitima ya anthu a mu mzindawo kuti akuwukireni inu.
32 Amaiba: le, di amola dima fa: no bobogesu dunu amo gasia wa: legadole, moifufu ganodini wamoaligima.
Nʼchifukwa chake usiku womwe uno inu ndi anthu anu mupite, mukabisale mʼminda.
33 Aya hahabe, eso mabe amoga wa: legadole amola moilai bai bagadega doagala: ma. Amasea, Ga: ile amola ea dunu da dilima gegemusa: gadili ahoasea, dia ha: giwane ili fama.”
Mmawa dzuwa likutuluka, mudzuke ndi kukathira nkhondo mzindawo. Gaali ndi anthu amene ali naye akamadzabwera kuti alimbane ndi inu, inu mudzathane nawo monga mmene mungachitire.”
34 Amaiba: le, Abimelege amola ea dunu huluane da gasia asili, Siegeme moilai bai bagadega gadili wamoaligi. Ilia da gilisisu biyadu gala hamoi.
Choncho Abimeleki ndi ankhondo ake onse anadzuka usiku nakabisalira mzinda wa Sekemu mʼmagulu anayi.
35 Abimelege amola ea dunu da Ga: ile gadili misini moilai bai bagade logo ga: su amoga lelebe ba: loba, ilia da ilia wamoaligisu sogebi fisili, wa: legadoi.
Gaali mwana wa Ebedi anatuluka nakayima pa khomo pa chipata cha mzinda pamene Abimeleki ndi ankhondo ake anatuluka ku malo kumene anabisala kuja.
36 Ga: ile da amo dunu ba: le, Sibalema amane sia: i, “Hodoma! Dunu da goumi gado fisili manebe goea!” Sibale da bu adole i, “Amo da dunu hame. Amo da baba goumia digaga: la: i fawane.”
Gaaliyo atawaona, anawuza Zebuli kuti, “Taona anthu akutsika kuchoka pamwamba pa mapiri.” Koma Zebuli anayankha kuti, “Zimene mukuonazo ndi zithunzi za mapiri chabe osati anthu.”
37 Be Ga: ile da bu sia: i, “Hodoma! Dunu da goumi felea gado manebegoea. Amola gilisisu eno da logo amo da ba: la: lusu dunu ilia ouge ifa amoga maha amoga manebe na ba: sa.”
Koma Gaaliyo anayankhulanso kuti, “Taona anthu akutsika kuchokera pakati pa phiri, ndipo gulu lina likubwera kuchokera ku mtengo wa thundu wa owombeza mawula.”
38 Amalalu, Sibale da ema amane sia: i, “Defea! Dia gasa fi sia: da wali habila: ? Dia gasa fili, ninia abuliba: le amo dunu Abimelege ea hawa: hamosala: ? sia: i dagoi. Amo dunu wali manebe da dunu dia hihini lasogoi dagoi. Di gadili asili, ilima gegema.”
Ndipo Zebuli anamufunsa iye kuti, “Pakamwa pako paja pali kuti tsopano, iwe amene umanena kuti, Abimeleki ndaninso kuti ife timutumikire? Kodi amenewa si anthu aja umawanyozawa? Tsopano tuluka ukamenyane nawo.”
39 Ga: ile da Siegeme dunu gadili oule asili, Abimelege amoma gegei.
Choncho Gaaliyo anatuluka akutsogolera anthu a ku Sekemu kukamenyana ndi Abimeleki.
40 Ga: ile hobea: i amola Abimelege da e sefasi. Dunu bagohame da moilai logo ga: su amoga fa: faginisi bagade ba: i.
Koma Abimeleki anamuthamangitsa ndipo Gaala anathawa. Ambiri a ankhondo ake anagwa napwetekeka njira yonse mpaka ku chipata cha mzinda.
41 Abimelege da Aluma moilaiga esalu. Amola Sibale da Ga: ile amola yolali gadili sefasi. Amaiba: le, ilia bu Siegeme moilai amo ganodini esalumu hamedeiwane ba: i.
Abimeleki anakhala ku Aruma, ndipo Zebuli anathamangitsa Gaali pamodzi ndi abale ake, kuwatulutsa mu Sekemu.
42 Aya amoha, Abimelege da Siegeme dunu da ilia ifabi amoga masusa: dawa: i, e da amane nabi.
Mmawa mwake anthu a ku Sekemu anapangana zopita ku minda, ndipo Abimeleki anamva zimenezi.
43 Amaiba: le, e da ea dunu afafane, gilisisu udiana hamone, ifabi ganodini wamoaligili, ouesalu. E da Siegeme dunu moilaiga gadili manebe ba: loba, e da ea wamoaligisu fisili, ili medomusa: misi.
Tsono Abimeleki anatenga anthu ake, nawagawa magulu atatu ndi kukabisala mʼminda. Ataona anthu akutuluka mu mzindawo, iye anapita kukalimbana nawo ndipo onsewo anawapha.
44 Abimelege amola ea gilisisu da hehenane, moilai bai bagade logo ga: su amo ouligimusa: ahoanoba, ea eno gilisisu aduna da Siegeme dunu ifabia esalu amoga doagala: le, huluane medole legei dagoi.
Abimeleki pamodzi ndi magulu ake anathamangira kutsogolo nakawakhalira pa chipata cha mzinda. Ndipo magulu awiri ena aja anathamangira anthu amene anali mʼminda ndi kuwapha onse.
45 Amo esoga ilia mae fisili gegenanu. Abimelege da Siegeme moilai amo lai dagoi. E da dunu huluane medole legele, diasu huluane mugululi, osobo amo deme amoga dedeboi.
Abimeleki anawuthira nkhondo mzindawo tsiku lonse. Kenaka anawulanda ndi kupha nzika zonse za mu mzindamo. Anawuwonongeratu mzindawo nawuwaza mchere.
46 Be Siegeme ouligisu dunu da gasa bagade diasu amo ganodini gagili sali ba: i. Ilia da amo hou nababeba: le, hehenane gasa bagade ‘Ba: ile da Gousa: su Hamoi’ ea debolo diasu ganodini gagili sali.
Anthu a mu nsanja ya Sekemu atamva zimenezi, anakalowa mu linga la nyumba yopembedzeramo Baala-Beriti.
47 Ilia da amo debolo diasu ganodini gagili sali amo nababeba: le, Abimelege da Sa: lamoune Goumi amoga ea dunu oule asi. Amalalu, e da goaha: i lale, ifa amoda damuni, amo gisa asi. Ea dunu da amo defele hedolo hamoma: ne, e sia: i.
Abimeleki anamva kuti anthu ena asonkhana kumeneko.
Choncho Abimeleki pamodzi ndi anthu ake onse anapita ku phiri la Zalimoni. Kumeneko anatenga nkhwangwa nadula nthambi za mitengo. Ananyamula nthambi zija pa phewa pake. Tsono anawuza anthu aja kuti, “Zimene mwaona ine ndikuchita, inunso mufulumire kuchita monga ndachitiramu.”
49 Amaiba: le, dunu huluane da ifa amoda damui. Amalalu, ilia da Abimelege amoma fa: no bobogele, ifa huluane amo Ba: ile gasa bagade diasu amo ea baiga ligisili, lalu didi. Lalu da amo diasu nene dagoi. Dunu amola uda (1,000 agoane) huluane amo diasu ganodini esalu da bogogia: i dagoi.
Tsono aliyense anadula nthambi zake, natsatira Abimeleki. Anakawunjika nthambi zija pa linga paja, kenaka ndi kuliyatsa moto. Choncho anthu onse a ku nsanja ya Sekemu anafa. Analipo anthu pafupifupi 1,000, amuna ndi akazi.
50 Amalalu, Abimelege da Dibese moilai bai bagadega asili, sisiga: le, lai dagoi.
Kenaka Abimeleki anapita ku Tebezi. Anakawuzungulira mzindawo ndi kuwulanda.
51 Amo moilai ganodini, gasa bagade diasu sedade gado gagagula heda: lebe ba: i. Dibese dunu, uda amola ilia ouligisu dunu da amoga hehenai. Ilia da golili sa: ili, logo ga: le, diasu figisu gadodafa amoga asi.
Koma mu mzindamo munali nsanja yolimba. Anthu onse a mu mzindamo amuna ndi akazi anathawira mu nsanjayo, nadzitsekera mʼkati. Ndipo anakwera ku denga la nsanjayo.
52 Abimelege da amo sedade diasu gado gagagula heda: i doagala: musa: misini, e da amo logo ga: suga laluga ulagimusa: asi.
Abimeleki anapita ku nsanjayo nathira nkhondo. Anafika pafupi ndi chitseko cha nsanja ija kuti ayitenthe.
53 Be uda afae da igi bagade (amoga ilia da widi goudasu) amo gududili sanasili, Abimelege ea dialuma gasa goudai.
Koma mkazi wina anaponya mwala wa mphero pa mutu wa Abimeleki ndi kuswa chibade cha mutuwo.
54 Amalalu, Abimelege da goi dunu (amo da Abimelege ea gegesu liligi gaguli ahoasu) amo ema misa: ne sia: ne, amane adoi, “Dia gegesu gobihei bagade duga: le gadole, na medole legemu. Dunu eno ilia da Abimelege udaga medole legei amo sia: mu na higa: i gala mabu.” Amaiba: le, amo goi da Abimelege gegesu gobiheiga sone, e bogoi.
Mwamsanga Abimeleki anayitana mnyamata womunyamulira zida za nkhondo namuwuza kuti, “Solola lupanga lako undiphe kuti anthu asadzanene kuti, ‘Mkazi ndiye anamupha.’” Choncho wantchito wake anamubayadi mpaka kutulukira kunja lupangalo ndipo anafa.
55 Isala: ili dunu da Abimelege bogoi dagoi ba: beba: le, ilia diasuga buhagi.
Aisraeli ataona kuti Abimeleki wafa, anapita kwawo.
56 Gode da agoaiwane Abimelegema dabe i. Bai e da ea yolalali 70 amo medole legeiba: le, ea ada Gidionema wadela: i bagade hamosu.
Mmenemu ndi mmene Mulungu analipsirira tchimo la Abimeleki limene anachitira abambo ake pakupha abale ake 70 aja.
57 Amola Siegeme dunu da wadela: i bagade hamobeba: le, Gode da ilima se iasu. Gidione egefe amo Youda: me da ilima gagabusu aligima: ne i, amo defele ba: i dagoi.
Mulungu anawalanganso anthu a ku Sekemu chifukwa cha kuyipa kwawo konse. Ndipo matemberero a Yotamu mwana wa Yeru-Baala anawagweradi.

< Bisisu 9 >