< Bisisu 5 >

1 Amo esohaga, Debola amola Bela: ge (Abinoa: me egefe) da amo gesami hea: i.
“Tsiku limenelo Debora ndi Baraki mwana wa Abinoamu anayimba nyimbo iyi:
2 “Hina Godema nodoma! Isala: ili dunu da gegemusa: dawa: iou, ilia da gegesu hahawane fidimu sia: i.
“Popeza kuti atsogoleri anatsogoleradi mʼdziko la Israeli; ndipo anthu anadzipereka okha mwa ufulu, tamandani Yehova:
3 Dilia hina bagade nabima! Noga: le dawa: ma! Na da ninia Isala: ili Hina Godema gesami hea: mu amola gesami hea: su liligi dumu.
“Imvani inu mafumu! Tcherani khutu, atsogoleri inu! Ndidzayimba nyimbo, ndidzayimbira Yehova, Mulungu wa Israeli nyimbo yokoma.
4 Hina Gode! Di da Sie goumi fisili, amola Idome soge amoga ahoanoba, osobo bagade da fofogolalu yagugui amola gibu da muagadodili sa: i. Dafawane, hano da mu mobi amo ganodini dialu, osobo bagadega sa: i.
“Inu Yehova, pamene munkatuluka mu Seiri, pamene mumayenda kuchokera mʼdziko la Edomu, dziko linagwedezeka, mitambo inasungunuka nigwetsa madzi.
5 Sainai Hina Gode da manebeba: le, goumi huluane da fofogoi. Hina Gode! Isala: ili dunu ilia Gode!
Mapiri anagwedezeka pamaso pa Yehova, Mulungu wa Israeli.
6 Sia: maga (Anade egefe) amola Ya: iele da esalea, dunu amola ga: mele amola bidi lasu dunu da Isala: ili sogega hame misi. Ilia da logo fonobahadi la: ididili asi.
“Pa nthawi ya Samugara mwana wa Anati, pa nthawi ya Yaeli, misewu inasiyidwa; alendo ankangoyenda mʼtinjira takumbali.
7 Debola! Isala: ili moilai gilisisu da dunu hame esalebe agoane ba: i. Amalalu, di da misi. Di da Isala: ili fi ilia ame defele misi dagoi.
Anthu a ku midzi anathawa; mu Israeli munalibe midzi mpaka pamene iwe Debora unafika; unafika ngati mayi ku Israeli.
8 Isala: ili dunu da gaheabolo ogogosu ‘gode’ liligi ilima fa: no bobogebeba: le, gegesu bagade ilia soge ganodini ba: i. Isala: ili dunu 40,000 agoane gilisi amo ganodini, lobo danoma: ne gala: su goge agei amola da: igene gaga: su liligi hame ba: i.
Pamene anasankha milungu ina, nkhondo inabwera ku zipata za mzinda, ndipo chishango kapena mkondo sizinapezeke pakati pa anthu 40,000 mu Israeli.
9 Na da Isala: ili ouligisu dunu ilima bagade asigisa. Amola dunu da mae hihini hahawane fidimusa: misi, na da ilima bagade asigisa. Hina Godema nodoma!
Mtima wanga uli ndi atsogoleri a Israeli, uli ndi anthu amene anadzipereka okha mwaufulu pakati pa anthu. Tamandani Yehova!
10 Dilia! Dunu da ahea: iya: i dougi amoga fila heda: su dunu! Amo sia: olelema! Amola dili emoga fawane ahoasu dunu! Dilia sia: ma!
“Inu okwera pa abulu oyera, okhala pa zishalo, ndi inu oyenda pa msewu, yankhulani.
11 Nabima! Dunu bagohame da gu hano amogai gilisili wele sia: nana. Ilia da Hina Gode Ea hasalasu hou amola Isala: ili dunu ilia hasalasu hou olelesa. Amalalu, Hina Gode Ea fi dunu da ilia moilai fisili, mogodigili gudu sa: i.
Ku zitsime, kutali ndi phokoso la a mauta; kumeneko akusimba za kuti Yehova wapambana; akusimba kuti Yehova walipsira anthu ake mu Israeli. “Choncho anthu a Yehova anasonkhana ku zipata za mzinda.
12 Debola! Bisima! Bisima! Gesami hea: ma! Bisima! Bela: ge, Abinoa: me egefe di! Ba: le gaidi godiwane masa! Dia ha lai dunu di afugili lai, amo oule masa!
Anati, ‘Tsogolera ndiwe, Debora, tsogolera; tsogolera ndiwe, tsogolera, imba nyimbo. Iwe Baraki! nyamuka Tsogolera akapolo ako, iwe mwana wa Abinoamu.’
13 Amalalu, fa: no noga: le bobogesu dunu da ilia ouligisu dunuma gagadomusa: gudu sa: i. Ilia da gegemusa: momagele, Hina Godema gilisi.
“Kenaka anthu okhulupirika anatsatira atsogoleri awo; anthu a Yehova anapita kukamenyera Yehova nkhondo kulimbana ndi adani amphamvu.
14 Ilia da Ifala: ime soge fisili, fagoa gudu misi. Ilia da Bediamini fi dunu ilima fa: no bobogei. Dadi gagui ouligisu dunu da Ma: igie soge fisili misi. Amola, ilia fidisu ouligisu dunu da Sebiula: ne sogega misi.
Anakalowa mʼchigwa kuchokera ku Efereimu; akutsatira iwe Benjamini ndi abale ako. Akulu a ankhondo anachokera ku Makiri, ndipo onyamula ndodo ya udindo anachokera ku Zebuloni.
15 Isaga fi ouligisu dunu da Debola amo sigi misi. Dafawane! Isaga fi da misi dagoi. Bela: ge da misiba: le, ilia da ema fa: no bobogele, fagoa gudu doaga: i. Be Liubene fi dunu da afafai. Ilia da misunu o hame misunu, hame dawa: i galu.
Olamulira a Isakara anali pamodzi ndi Debora; inde, anthu ochokera ku Isakara anatsatanso Baraki, ndipo anathamangira ku chigwa akumutsatira. Koma pakati pa mafuko a Rubeni panali kusinkhasinkha mtima kwambiri osadziwa chenicheni choyenera kuchita.
16 Ilia da abuliba: le mae misini, sibi ouligima: ne ouesalula: ? Ilia abuliba: le, sibi ouligisu dunu sibima wele sia: su amo nabima: ne, ouesalula: ? Ma! Liubene fi da afafai dagoi ba: i. Ilia da misunu o hame misunu, hame dawa: i galu.
Chifukwa chiyani munangokhala ku makola a nkhosa nʼkumangomvetsera zitoliro zoyitanira nkhosa? Pakati pa anthu a fuko la Rubeni panali kusinkhasinkha mtima kwambiri osadziwa chenicheni choyenera kuti achite.
17 Ga: de fi dunu da Yodane Hano eso mabe la: ididili esalebe ba: i. Da: ne fi dunu da ilia dusagai ouligima: ne esalebe ba: i. A: sie fi dunu da hano bagade bega: ouesalebe ba: i.
Agiliyadi anatsala pa tsidya la Yorodani. Ndipo nʼchifukwa chiyani anthu afuko la Dani anatsarira mʼsitima za pa madzi? Aseri anali pa gombe la Nyanja; anangokhala mʼmadooko mwawo.
18 Be Sebiula: ne fi dunu amola Na: fadalai dunu da bogosa: besa: le mae dawa: le, gegesu amoga gilisi.
Azebuloni ndi anthu amene anayika moyo wawo mʼzoopsa. Nawonso anthu a fuko la Nafutali anayika miyoyo yawo pa chiswe pomenya nkhondo pamwamba pa mapiri.
19 Hina bagade dunu da Da: ina: ge moilai bai bagade, Megido Hano bega: dialu, amoga gegemusa: misi. Ga: ina: ne hina bagade dunu da gegei, be hame hasalasiba: le, silifa noga: i liligi hame gaguli asi.
“Mafumu anabwera, anachita nkhondo; mafumu Akanaani anachita nkhondo ku Tanaki pafupi ndi madzi a ku Megido, koma sanatengeko zofunkha zasiliva.
20 Fedege sia: agoane, gasumuni da muagado asili, amoga gegei. Ilia da hina bagade Sisela ema gegei.
Ngakhalenso nyenyezi zakumwamba zinachita nkhondo, zinathira nkhondo Sisera, zikuyenda mʼnjira zake.
21 Gaisione Hano da filigala: le neda: le, amo dunu huluane mini asili, gaguli asi. Na da gasawane mogodigili masunu!
Mtsinje wa Kisoni unawakokolola, chigumula cha mtsinje wa Kisoni chinawakokolola. Mtima wanga, yenda mwamphamvu, limbika!
22 Amalalu, hosi da hehenane misini, osoboga ha: giwane osa: i.
Ndipo ziboda za ngʼombe zazimuna zinachita phokoso lalikulu, akavalo ali pa liwiro, akuthamanga kwambiri.
23 Hina Gode Ea a: igele dunu da amane sia: sa, “Milose soge amo aligima: ne gagabuma. Dunu huluane amogawi esala, amo aligima: ne gagabuma. Ilia da Hina Godemagale gegemusa: hame misi.”
Mngelo wa Yehova anati ‘Tembererani Merozi.’ ‘Tembererani nzika zake mwaukali, chifukwa sanabwere kudzathandiza Yehova, kulimbana ndi adani ake amphamvu.’
24 Hibe (Ginaide dunu) amo ea uda da hahawane bagade. E da uda huluane abula diasu amo ganodini esalebe uda, amo ilia hahawane hou baligisa.
“Akhale wodala kupambana akazi onse, Yaeli mkazi wa Heberi Mkeni; inde mwa akazi onse okhala mʼdziko, akhale wodala iyeyu.
25 Sisela da ema hano edegei. Be e da dodo maga: me ema i. E da gebo sefe gugu, yaeya noga: iwane amo ganodini sali, gaguli misini ema i.
Munthu uja anapempha madzi akumwa, koma iye anamupatsa mkaka; anamupatsa chambiko mʼchikho cha wolemekezeka.
26 E da abula diasu goge agei, lobo afae amo ganodini gaguli, hawa: hamosu dunu ea ha: ma, lobo eno amo ganodini gagui. E da Sisela fane, ea dialuma goudai. E da ea dialuma amo abula goge agei amoga soi dagoi.
Anatenga chikhomo cha tenti mʼdzanja lake, anatenganso nyundo ndi dzanja lake lamanja. Ndipo anakhoma nacho Sisera, anamuphwanya mutu wake, ndi kumubowola mu litsipa mwake.
27 E da muguni bugili, diasa: ili, amo uda ea emo gadenene osoboga sa: ili, bogoi dagoi.
Anathifukira ku mapazi a mkaziyo nagwa, anagwa; iye anagona pamenepo. Anagwera pa mapazi a mkaziyo, iye anagwa; pamene anagwera, pamenepo anaferapo.
28 Sisela ea ame da fo misa: ne agenesi amoga ba: i. E da ifa gigiadomai hobea: ga gadili ba: lalu. E amane adole ba: i, “Ea sa: liode da abuliba: le hedolo hame maha? Ea hosi da abuliba: le hedolo hame buhagisala: ?”
“Amayi ake a Sisera anasuzumira pa zenera; nafuwula mokweza kuti, ‘Nʼchifukwa chiyani galeta lake lachedwa kufika? Nʼchifukwa chiyani phokoso la magaleta ake silikumveka?’
29 Ea bagade dawa: su fidisu uda ilia da ema amane adole i, amola e da hisu hima adole ialala, amane,
Amayi ake anzeru kwambiri anamuyankha, ndithudi, mwiniwake anadziyankha yekha kuti,
30 “Ilia da liligi lama: ne amola afafane ima: ne hogolala. Dadi gagui dunu da afae afae a: fini afae o aduna lamu. Sisela da abula ida: iwane lamu. Amola abula ida: iwane amuni liligi, ea uda galogoa gisa: gima: ne, amo lamusa: hogolala.”
‘Kodi iwo sakufunafuna zofunkha kuti agawane; akugawana wankhondo aliyense mtsikana mmodzi kapena awiri. Sisera akumupatsa zofunkha: zovala zonyikidwa mu utoto, zoti ndizivala mʼkhosi zovala zopeta zonyika mu utoto, ndi zopeta zomavala mʼkhosi?’
31 Hina Gode! Dima ha lai dunu huluane da Sisela ea bogoi defele bogomu da defea. Be Dima dogolegei dunu da eso mabe ea diga: i defele diga: mu da defea.” Amalalu, Isala: ili soge ganodini da ode 40 amoga olofosu fawane ba: i.
“Choncho Yehova! adani anu onse awonongeke, koma iwo amene amakukondani inu akhale ngati dzuwa pamene lituluka ndi mphamvu zake.” Ndipo dziko linakhala pa mtendere zaka makumi anayi.

< Bisisu 5 >