< Bisisu 16 >
1 Eso afaega, Sa: masane da Filisidini moilai bai bagade ea dio Ga: isa amoga asili, wadela: i hamosu uda gousa: i. E da amo uda gilisili golai.
Tsiku lina Samsoni anapita ku Gaza. Kumeneko anaonako mkazi wachiwerewere, ndipo analowa mu nyumba yake.
2 Ga: isa dunu fi da Sa: masane da esalebe nababeba: le, ilia da amo moilai bai bagade sisiga: le, moilai logo ga: su amoga e gagumusa: oulelu. Ilia da gasi ganodini ouiya: le lelu. Ilia agoane dawa: iou, “Ninia da oulelu, hahabedafa Sa: masane medole legemu.”
Anthu a ku Gaza anawuzidwa kuti, “Samsoni ali kuno!” Choncho anthuwo anazungulira malowo, kumubisalira usiku wonse ku chipata cha mzindawo. Iwo anakhala chete usiku wonse namanena kuti, “Tidzamupha mmamawa.”
3 Be Sa: masane da golale, gasimogoa wa: legadole, e da moilai logo ga: su bagade (ga: su huluane, ifa amola logo huluane) amo mugululi fasili, gisawane, agolo amoga dunu da Hibalone moilai bai bagade ba: su, amoga gaguli asi.
Koma Samsoni anangogonako mpaka pakati pa usiku. Kenaka pakati pa usiku anadzuka nagwira zitseko za chipata cha mzinda ndi maferemu ake awiri, ndipo anazizula zonse pamodzi ndi mpiringidzo womwe. Anazisenza pa mapewa pake napita nazo pamwamba pa phiri loyangʼanana ndi Hebroni.
4 Amalalu, Sa: masane da uda Solege fago amo ganodini esalu ea dio amo Dilaila, ema asigiba: le, lamusa: dawa: iou.
Pambuyo pake, Samsoni anayamba kukonda mtsikana wina wa ku chigwa cha Soreki dzina lake Delila.
5 Filisidini hina bagade biyale gala da Dilaila ema misini, amane sia: i, “Di Sa: masane hohonoma. Ninia da habodane e lale, la: gima: ne amola ea hou amoga hasalasima: ne, amo hogoi helema. Amalalu, ninia afae afae dima 1,100 silifa fage imunu.”
Olamulira Afilisti anapita kwa mkaziyo ndipo anati, “Umunyengerere Samsoni kuti udziwe chinsinsi cha mphamvu zake zoopsazi, komanso ndi mmene ife tingamupambanire kuti timumange ndi kumugonjetsa. Ukatero aliyense wa ife adzakupatsa ndalama zasiliva 1,100.”
6 Amaiba: le, Dilaila da Sa: masanema amane sia: i, “Na da dima edegesa. Dia gasa bagade hou da habidili mahabela: ? Dunu da di la: gili, dia gasa hedofamusa: da habodane hamoma: bela: ?”
Choncho Delila anati kwa Samsoni, “Inu tandiwuzani pamene pagona mphamvu zanu zoopsazi ndi mmene anthu akhoza kukumangirani kuti akugonjetseni.”
7 Sa: masane da bu adole i, “Ilia da gahe hame bioi gaheabolo dadi gosalo fesuale gala amoga na la: gisia, na da dunu eno defele gasa hame ba: mu.”
Samsoni anamuyankha kuti, “Ngati wina atandimanga ndi zingwe zisanu ndi ziwiri zatsopano zosawuma, ndidzafowoka ndi kusanduka ngati munthu wina aliyense.”
8 Amaiba: le, Filisidini hina bagade da Dilaila ema gahe hame bioi gaheabolo dadi gosalo fesuale gaguli misi. Amoga, e da Sa: masane la: gi dagoi.
Tsono atsogoleri a Afilisti aja anapita kwa mkazi uja namupatsa zingwe zisanu ndi ziwiri zatsopano zosawuma, ndipo mkaziyo anamanga nazo Samsoni.
9 Dilaila da sia: beba: le, dunu eno da diasu la: ididili sesei ganodini wamo ouesalebe ba: i. E gasa bagade wele sia: i, “Sa: masane! Filisidini dunu da manebe goea!” Be Sa: masane da amo dadi gosalo hedolo fi. Ilia da gobea ha: i laluga nei dibi agoane hedolowane fi. Amaiba: le, Filisidini dunu da ea gasa bagade wamolegei bai hame dawa: i.
Nthawi imeneyo nʼkuti mkazi uja atayika anthu omubisalira mʼchipinda. Tsono anati kwa mwamuna wake, “Amuna anga, Afilisti aja afika!” Koma iye anangodula zingwe zija ngati mmene imadukira nkhosi ya chingwe ikamapsa. Choncho chinsinsi cha mphamvu zake sichinadziwike.
10 Dilaila da Sa: masane ema amane sia: i, “Di da nama ogogoiba: le, na da gagaoui dunu agoai ba: sa. Nama moloiwane adoma. Dia gasa hedofama: ne, dunu da habodane di la: gima: bela: ?”
Kenaka Delila anati kwa Samsoni, “Inu mwandipusitsa ndi kundiwuza zabodza. Chonde tandiwuzani mmene munthu angakumangireni.”
11 E bu adole i, “Ilia da efe gaheabolo (amoga liligi da musa: hame la: gi) amoga na la: gisia, na da eno dunu defele, gasa hame ba: mu.”
Iye anati, “Ngati aliyense atandimanga ine ndi zingwe zatsopano zimene sanazigwiritseko ntchito, ndidzasanduka wofowoka ndi kukhala monga munthu wina aliyense.”
12 Amaiba: le, Dilaila da efe gaheabolo lale, Sa: masane la: gi dagoi. Amalalu, e da gasa bagade wele sia: i, “Sa: masane! Filisidini dunu da manebe!” Dunu eno da diasu la: ididili wamo ouesalebe ba: i. Be Sa: masane da amo efe dasai gobea ha: i defele fi.
Choncho Delila anatenga zingwe zatsopano namumanga nazo. Kenaka anati “Amuna anga, Afilisti aja afikanso!” Nthawi iyi nʼkuti anthu omubisalira aja ali mʼchipinda chamʼkati. Koma iye anadulanso zingwe mʼmanja ake ngati akudula ulusi wa thonje.
13 Dilaila da Sa: masane ema amane sia: i, “Di da nama bu ogogoiba: le, na da gagaoui dunu agoane ba: sa. Dunu da habodane di lagima: bela: ?” Sa: masane da bu adole i, “Di da na dialumasa fesuale amo amunasuga amunasea amola mae fadegala masa: ne ifa amoga nodomenesisia, na da dunu eno defele gasa hame ba: mu.”
Ndipo Delila anati kwa Samsoni, “Mpaka tsopano mwakhala mukundipusitsa ndi kumandiwuza zabodza. Chonde, tandiwuzani mmene munthu angakumangireni.” Iye anayankha kuti, “Ngati njombi zisanu ndi ziwiri za kumutu kwanga utazilukira mu cholukira nsalu ndi kuchimanga molimbika ndi chikhomo, ndidzasanduka wofowoka ndi kukhala wofanana ndi munthu wina aliyense.”
14 Dilaila da Sa: masane amo ea masele da: iya, fene golama: ne susui. Amalalu, e da ea dialumasa fesuale amo amunasuga amuni. Mae fadegama: ne, e da ifaga nodomenesi. Amalalu, e da bagade wele sia: i, “Sa: masane! Filisidini dunu da manebe!” Be e da nedigili, ea dialuma hinabo amuni amo fadegai dagoi.
Choncho iye akugona, Delila analukira njombi za ku mutu kwa Samsoni mu cholukira nsalu nachimanga molimba ndi chikhomo. Pambuyo pake anati kwa Samsoni, “Amuna anga, Afilisti aja abwera!” Tsono iye anadzuka ku tulo, nazula chikhomo chija ndipo njombi zinachoka mu cholukira chija.
15 Amalalu, Dilaila da ema amane sia: i, “Di da habodane nama asigisa amo sia: sala: ? Di da udiana agoane nama ogogoiba: le, na da gagaoui agoane ba: sa. Dia gasa bagade hou amo ea wamolegei bai, da nama hame olelei.”
Tsono mkaziyo ananenanso kwa iye kuti, “Munganene bwanji kuti mumandikonda pamene mtima wanu suli pa ine? Aka ndi kachitatu mukundipusitsa ndipo simunandiwuze pamene pagona mphamvu zanu zoopsazi.”
16 Eso huluane mae fisili, e da Sa: masanema adole ba: lalu. E da eso huluane sia: ga gegenabeba: le, Sa: masane da hele bagade nabi.
Tsono popeza anamupanikiza ndi mawu ake tsiku ndi tsiku ndi kumukakamiza, mtima wa Samsoni unatopa pafupi kufa.
17 Helebeba: le, e da moloiwane ea gasa bagade hou amo ea wamolegei bai ema olelei. E amane sia: i, “Na dialuma hinabo da hamedafa damusu. Na lalelegei eso amoga na da Na: salaide hou hamoma: ne, ilia da na Godema i. Na dialuma hinabo da damui dagoi ba: sea, na da dunu eno defele, gasa hame ba: mu.”
Choncho anamuwuza mkaziyo zonse za mu mtima mwake nati “Lumo silinapitepo pa mutu wanga chifukwa ndakhala ndili Mnaziri wopatulikira Mulungu chibadwire. Ngati nditametedwa mphamvu zanga zidzandichokera, ndidzasanduka wofowoka ndipo ndidzafanana ndi munthu wina aliyense.”
18 Dilaila da Sa: masane da ema moloidafa olelei dagoi ba: i. Amaiba: le, e da Filisidini hina bagade ema sia: adole iasi, amane, “Afadafa fawane bu misa! E da nama moloiwane olelei!” Amalalu, ilia da misini, muni dabe ema ima: ne gaguli misi.
Delila ataona kuti wamuwuza zonse za mu mtima mwake anatumiza uthenga kukayitana akuluakulu a Afilisti nati, “Bweraninso kamodzi kano kokha popeza wandiwululira zonse za mu mtima mwake.” Choncho akuluakulu a Afilisti aja anabwera ndi ndalama za siliva mʼmanja mwawo.
19 Dilaila da Sa: masane ea masele da: iya fene golama: ne sususu. Amalalu, e da dunu eno misa: ne wele sia: i. Amo dunu da Sa: masane ea dialuma sa fesuale gala damuni fasi. Amalalu, Dilaila da Sa: masane ougima: ne, ema gadele sia: su. Bai Sa: masane ea gasa da fisi dagoi ba: i.
Mkazi uja anagoneka Samsoni pa miyendo yake. Kenaka anayitana munthu wina ndipo anadzameta Samsoni njombi zisanu ndi ziwiri zija kumutu kwake. Pamenepo anayamba kufowoka, ndipo mphamvu zake zinamuchokera.
20 Amalalu, Dilaila da amane wele sia: i, “Sa: masane! Filisidini dunu da manebe!” E da nedigili, amane dawa: i, “Na da musa: agoane hahawane masunu.” Be Hina Gode da e yolesi dagoi, amo e da hame dawa: iou.
Pambuyo pake mkaziyo anamuyitana kuti, “Amuna anga, Afilisti aja abwera!” Iye anadzuka kutuloko, naganiza kuti, “Ndituluka monga ndimachitira nthawi zonse ndi kudzimasula.” Koma sanadziwe kuti Yehova wamuchokera.
21 Amalalu, Filisidini dunu da Sa: masane afugili, ea si aduna duga: le fasi. Ilia da e Ga: isa moilaiga oule asili, balase sia: inega la: gili, ema se iasu diasu hawa: hamomusa: logei. E se iasu diasu ganodini gagoma amola widi goudalalu.
Afilisti anamugwira ndipo anamukolowola maso. Kenaka anapita naye ku Gaza atamumanga ndi maunyolo achitsulo. Kumeneko anakhala wa pamphero mu ndende.
22 Be ea dialuma hinabo da muni bu heda: lalebe ba: i.
Pambuyo pake tsitsi la pa mutu wake, monga linametedwa, linayambanso kumera.
23 Filisidini hina bagade huluane da hahawane lolo manusa: amola ilia ogogosu ‘gode’ amo Da: igone ema gobele salasu bagade ima: ne gilisi dagoi. Ilia da amane gesami hea: i, “Ninia ‘gode’ da fidibiba: le, ninia da ninia ha lai dunu Sa: masane hasali.”
Tsono atsogoleri a Afilisti anasonkhana kuti adzapereke nsembe yayikulu kwa Dagoni mulungu wawo ndi kukondwerera popeza ankanena kuti, “Mulungu wathu wapereka Samsoni mdani wathu mʼmanja mwathu.”
Anthuwo atamuona Samsoni, anayamba kutamanda mulungu wawo popeza ankanena kuti, “Mulungu wathu wapereka mdani wathu mʼmanja mwathu, ndiye amene anawononga dziko lathu, napha anthu athu ambirimbiri.”
25 Ilia da hahawane gilisili hedebeba: le, amane sia: i, “Sa: masane misa: ne wele sia: ma! E da nini hahawane ba: ma: ne hedemu da defea.” Ilia da Sa: masane se iasu diasuga gadili oule misini, ilia da hahawane ba: ma: ne hedema: ne sia: i. Ilia da e da igi dunibugi bagade aduna dogoa leloma: ne sia: i. Filisidini dunu da Sa: masane ba: loba, ilia da ilia ‘gode’ma bagadewane nodomusa: gesami hea: i, amane, “Amo dunu da ninia soge wadela: lesi amola ninia dunu bagohame medole legei. Be ninia ‘gode’ da hamobeba: le, ninia da e hasali dagoi.”
Ali mʼkati mosangalala, anthu aja amafuwula kuti, “Mutulutseni Samsoniyo kuti adzatisangalatse.” Choncho anamutulutsadi Samsoni mʼndende, ndipo anawasangalatsadi. Ndipo anamuyimiritsa pakati pa mizati.
26 Goi afae da Sa: masane lobolele, oule ahoasu. Sa: masane da ema amane sia: i, “Na da dunibugi amoga diasu da gagui amo digili ba: mu galebe. Na da ilima baligisiagamu hanai galebe.”
Pambuyo pake Samsoni anawuza mnyamata amene anamugwira dzanja kuti, “Ndilole kuti ndikhudze mizati imene yachirikiza nyumba yonseyi kuti ndiyitsamire.”
27 Amo diasu ganodini da dunu amola uda bagohame gilisili esalebe ba: i. Filisidini hina bagade biyale gala huluane esalebe ba: i. Diasu ea figisu da: iya dunu amola uda 3,000 agoane esalebe ba: i. Ilia da Sa: masane ba: lalu amola ilia hahawane ba: ma: ne, e se nabawane hedemusa: bagadewane wele sia: su.
Nthawi imeneyi nʼkuti nyumbayo ili yodzaza ndi anthu aamuna ndi aakazi. Olamulira onse a Afilisti anali momwemo, ndipo pamwamba pa nyumbayo panali anthu 3,000 aamuna ndi aakazi amene amaonerera Samsoni akusewera.
28 Amalalu, Sa: masane da Godema sia: ne gadoi, amane, “Hina Gode Bagadedafa! Dia na bu dawa: loma! Na da ha: giwane Dima edegesa. Di nama na gasa bagade hou bu afaewane nama ima. Amasea, na da afadafa fabeba: le amo Filisidini dunu da na si duga: le fasi ilima dabemu.”
Tsono Samsoni anapemphera kwa Yehova kuti, “Inu Yehova Ambuye anga, ndikumbukireni. Chonde ndilimbitseni nthawi yokha ino, inu Yehova, kuti ndiwabwezere Afilistiwa chifukwa cha maso anga awiri.”
29 Amaiba: le, Sa: masane dadunibugibagade aduna diasu dogoa dialu amo afae da lobodafa eno lobo fofadi amoga gaguli, gasawane fusu.
Choncho Samsoni anagwira mizati iwiri yapakati imene inkachirikiza nyumbayo. Anayitsamira ndi mphamvu zake zonse, dzanja lake lamanja ku mzati wina ndi dzanja lamanzere ku mzati winanso,
30 E amane wele sia: i, “Na amola Filisidini dunu da gilisili bogomu da defea.” E da gasa bagade fubiba: le, diasu da mugululi, Filisidini hina bagade biyale gala amola dunu huluane amoga fana sa: i. Huluane da bogogia: i. Sa: masane da ea bogoi eso amoga da Filisidini dunu medole legei amo ilia idi da ea esalebe eso amoga medole legei amo ilia idi baligi dagoi.
ndipo Samsoni anati, “Ndife nawo pamodzi!” Nthawi yomweyo anakankha ndi mphamvu zake zonse ndipo mizati inagwera atsogoleri a Afilisti ndi anthu onse anali mʼmenemo. Tsono chiwerengero cha anthu amene Samsoni anapha pa nthawi ya imfa yake chinaposa cha iwo amene anawapha akanali ndi moyo.
31 Ea yolali amola ea sosogo fi dunu eno da ea da: i hodo lala misi. Amo ilia gaguli, ea eda Manoua amo ea bogoi salasu Soula amola Esedoule dogoa sogebi dialu, amoga uli dogone sali. Sa: masane da ode 20amoga Isala: ili dunu ilia ouligisu esalu.
Kenaka abale ake ndi onse a pa banja la abambo ake anapita kukamutenga. Ndipo anakamuyika pakati pa Zora ndi Esitaoli mʼmanda a abambo ake, Manowa. Iye anatsogolera Israeli kwa zaka makumi awiri.