< Yosiua 2 >
1 Ilia da Aga: isia sogebi abula diasu gilisisu ganodini esalu. Amalalu, Yosiua da desega ahoasu dunu aduna asunasi. E da ela da wamowane Ga: ina: ne soge amola baligili Yeligou moilai bai bagade, amo hou ba: la masa: ne sia: i. Yeligou moilai bai bagadega doaga: le, ela da wadela: i hamosu uda (hina: da: i bidi lasu uda) ea dio amo La: iha: be, amo ea diasu ganodini gasi afadafa midi.
Tsono Yoswa mwana wa Nuni anatuma anthu awiri okazonda dziko mwachinsinsi kuchokera ku Sitimu. Iye anawawuza kuti, “Pitani mukaone dzikolo makamaka mzinda wa Yeriko.” Kotero iwo anapita ndipo anakafika ku nyumba ya mkazi wadama dzina lake Rahabe, ndipo anagona kumeneko.
2 Yeligou Hina bagade da amo gasia, Isala: ili dunu da ilia soge desega ba: la misi, amo sia: ne iasu nabi dagoi.
Mfumu ya Yeriko inawuzidwa kuti, “Aisraeli ena afika mu mzinda muno usiku uno kudzazonda dziko.”
3 Amaiba: le, e da La: iha: bema amane sia: si, “Dunu dia diasuga esala da ninia soge desega misi. Amo dunu, gadili oule misa.”
Choncho Mfumu ya Yeriko inatumiza uthenga kwa Rahabe kuti, “Atulutse anthu amene abwera ku nyumba kwakowo chifukwa iwo abwera kuti adzazonde dzikoli.”
4 Be La: iha: be da amane sia: i, “Dafawane! Dunu da na diasuga misi dagoi. Be ilia da habidili misi na da hame dawa: i galu. Eso dabe amoga moilai bai bagade logo ga: su da hame ga: si galu, amo dunu da fisili asi. Ilia masunu soge nama hame adoi. Be dilia da ilima hedolo fa: no bobogesea, afugili lamu.” (Be La: iha: be da desega ahoasu dunu ea diasu gadodili saga: ligisisu bi amo hagudu wamoaligi.)
Koma pa nthawiyi nʼkuti mkaziyo atatenga amuna awiriwo ndi kuwabisa. Tsono anayankha kuti, “Inde, anthuwo anafikadi ku nyumba kuno. Koma sindinadziwe kumene anachokera.
Iwo achoka kuno ndi chisisira, chipata cha mzinda chili pafupi kutsekedwa. Ndiye sindidziwa kumene alowera. Koma mukawalondola msanga muwapeza.”
Koma nʼkuti atawakweza pa denga azondiwo ndi kuwabisa pansi pa mapesi a thonje amene iye anawayika pa dengapo.
7 Hina bagade ea hawa: hamosu dunu da moilai bai bagade fisili amalalu logo da ga: si dagoi ba: i. Ilia da Isala: ili desega ahoasu dunu hogomusa: , logoga ahoanoba, logo da Yodane Hano degesu amoga doaga: i dagoiba: le fawane yolesi.
Nthumwi za mfumu zija zitatuluka ndipo chipata chinatsekedwa. Nthumwizo zinapita kukawafunafuna azondi aja mpaka ku dooko la Yorodani.
8 Desega ahoasu dunu da golamusa: dawa: i be hidadea La: iha: be da diasu gado amoga heda: le,
Azondiwo asanagone, Rahabe anakwera pa denga
9 elama amane sia: i, “Hina Gode da amo soge dilima i amo na dawa: Dunu huluane na soge ganodini da diliba: le bagade beda: i.
ndipo anawawuza kuti, “Ine ndikudziwa kuti Yehova wakupatsani dziko lino ndipo tili ndi mantha. Anthu onse a mʼdziko lino ali ndi mantha chifukwa cha inu.
10 Hina Gode da dili Idibidi sogega fisili masa: ne gadili oule asili, dilia midadi Maga: me Hano Wayabo hafoga: i dagoi amo ninia nabi. Ninia nabi dilia da A: moulaide hina bagade aduna Yodane eso mabadi la: idi, amo Saihone amola Oge medole legei.
Ife tinamva mmene Yehova anawumitsira madzi a Nyanja Yofiira inu mukufika pamene munatuluka mʼdziko la Igupto. Tamvanso zimene munachita kwa Sihoni ndi Ogi, mafumu awiri a Aamori amene ali kummawa kwa Yorodani. Inu munawawononga kotheratu.
11 Dilia hou nababeba: le, ninia da bagadewane beda: i. Diliba: le, ninia gasa huluane fisi dagoi ba: i. Dilia Hina Gode da Hebene amola osobo bagade amoma Hinadafa esala.
Titamva zimenezi, ife tinataya mtima ndipo aliyense wa ife ali ndi mantha chifukwa cha inu. Tikudziwa kuti Yehova Mulungu wanu ndi Mulungu wa kumwamba ndi dziko lapansi.
12 Wali, Hina Gode Ea Dioba: le, alia da na alima asigi hou defele, alia da na sosogo fi ilima asigima: ne ilegele sia: ma. Amola na da alia sia: dafawaneyale dawa: ma: ne, dawa: digima: ne olelesu nama ima.
Choncho mulumbire pamaso pa Yehova ndi kundipatsa chizindikiro choti mudzachitadi zimene mwalonjeza, kuti monga inu ndakuchitirani chifundo, inunso mudzachitira chifundo a pa banja la abambo anga.
13 Dilia da na ada, na ame, na olalali, na dalusi huluane amola ilia sosogo fi huluane, amo dilia da gaga: ma: ne ilegele sia: ma. Nini mae medole legema.
Inu mulonjeze kuti simudzapha abambo anga ndi amayi anga, abale anga ndi alongo anga ndi mabanja awo omwe.”
14 Desega ahoasu dunu da bu adole i, “Defea! Di da hame bogomu. Di da ania esalusu anima iba: le, ania da dilia esalusu dabe agoane imunu. Di da dunu eno ania hou hamedafa adosea, Hina Gode da amo soge ninima iasea, ani da dafawane ilegele sia: sa, di da se hame nabimu.”
Anthuwo anamuyankha kuti, “Ife ndife okonzeka kufa chifukwa cha inu. Ngati iwe sudzawulula zimene tachitazi, ndiye kuti ife tidzakukomera mtima ndi kusunga pangano lathu ndi iwe, Yehova akadzatipatsa dziko lino.”
15 La: iha: be da diasu amo moilai bai bagade gagoi gadodili gagui galu. Amaiba: le, e da fo misa: ne agenesi doasili, desega ahoasu dunu aduna efega bagele, osoboga sanasi.
Popeza nyumba ya Rahabe inali pa linga la mzindawo, azondi aja anatulukira pa zenera. Rahabe anawatsitsa pansi ndi chingwe.
16 E amane sia: i, “Hina bagade ea hawa: hamosu dunu da ali ba: sa: besa: le, agolo sogega masa. Amogawi, eso udiana amoga wamoaligili, hogosu dunu da guiguda: bu misi dagoiba: le, bu masa.”
Iye anawawuza kuti, “Pitani ku mapiri kuti okuthamangiraniwo asakupezeni. Mukabisale kumeneko masiku atatu mpaka iwo atabwerera, ndipo kenaka muzikapita kwanu.”
17 Desega ahoasu dunu da ema amane sia: i, “Ania dima dafawane sia: i amo ania da hame gogolemu.
Anthuwo anati kwa iye, “Lonjezo limene watichititsa ifeli tidzalisungadi
18 Di agoane hamoma. Ninia da dia soge doagala: sea, amo fo misa: ne agenesi di da ani sanasi, amoga amo yoi efe bagesima. Dia ada, ame, yolalali amola dia sosogo fi huluane, amo dia diasu ganodini gilisima: ne sia: ma.
tikadzalowa mʼdzikoli, iwe udzamangirire kansalu kofiira pa zenera limene unatitulutsira, ndi kusonkhanitsa abambo ako, amayi ako, abale ako ndi banja lako lonse mʼnyumba muno.
19 Be nowa da diasu gadili ahoasea, ea bogosu da hi hamoiba: le bogoi ba: mu - ninia hame. Be nowa da dia diasu ganodini sali ba: sea amo bogosea, amo bogoi da ninima dabe lamu agoai galebe.
Ngati wina aliyense adzatuluka mʼnyumbamo kuti azikayendayenda mu msewu, magazi ake adzakhala pamutu pake, ife sitidzapalamula kanthu. Koma wina aliyense wokhala mʼnyumba mwakomo akadzaphedwa, mlandu udzakhala wathu.
20 Be, di da amo hou eno dunuma olelesea, defea, ninia amo ilegele sia: i fisili, di hame gaga: mu.”
Komanso iwe ukangowulula zimene ife tikuchitazi ndiye kuti ife sitidzasunga zimene talonjezazi.”
21 La: iha: be da ela sia: i hahawane naba ba: lalu, ela asunasi. Ela da asi dagoloba, e da yoi efe, amo ea fo misa: ne agenesi amoga bagesi dagoi.
Rahabe anayankha kuti, “Zikhale monga mwaneneramo.” Kenaka iye anawatulutsa ndipo iwowo anapita. Pambuyo pake Rahabe anamangirira kansalu kofiira pa zenera paja.
22 Desega ahoasu dunu da agolo sogega asili, wamoaligi.
Azondi aja anachoka napita ku mapiri ndipo anakhalako masiku atatu. Apa nʼkuti otumidwa ndi mfumu aja atawafunafuna ponseponse nʼkubwerera osawapeza.
23 Yeligou hina bagade ea hawa: hamosu dunu da eso udianaga ela hogolalu be hame ba: beba: le, Yeligou diasuga buhagi. Amalalu, desega ahoasu dunu aduna da agolo soge fisili, hano degele, Yosiua ema buhagi. Ela da elama doaga: i hou huluane amo Yosiuama olelei.
Pambuyo pake azondi awiri aja anayamba ulendo wobwerera kwawo. Anatsika ku mapiri kuja, nawoloka mtsinje mpaka anakafika kwa Yoswa mwana wa Nuni. Ndipo anamuwuza zonse zimene zinawachitikira.
24 Amalalu ela amane sia: i, “Hina Gode da amo soge huluane ninima i dagoi, amo ania da dafawaneyale dawa: be. Dunu huluane amo ganodini esala da niniba: le bagadewane beda: i.”
Iwo anati kwa Yoswa, “Ndithu, Yehova wapereka dziko lonse mʼmanja mwathu. Anthu onse kumeneko akuchita nafe mantha.”