< Yosiua 16 >

1 Soge amo da Yousefe egaga fi ilima ilegei da agoane. Ga (south) alalo da Yodane Hano amo Yeligou moilai bai bagade gadenene ba: i. Alalo da Yeligou Bubuga: su hano amo eso mabadi la: idi ba: i. Amoga asili alalo da wadela: i sogega asili, agolo sogega asili, Bedele moilaiga doaga: i.
Dziko limene linapatsidwa kwa fuko la Yosefe linayambira ku mtsinje wa Yorodani ku Yeriko, kummawa kwa akasupe a Yeriko, ndiponso kuyambira mtsinje wa Yorodaniwo nʼkumakwera, kudutsa mʼchipululu mpaka ku mapiri a ku Beteli.
2 Bedele moilai baligili, alalo da Lase moilaiga asili A: dalode A: da moilaiga doaga: i. (Agaide dunu da amo moilaiga esalu.)
Kuchokera ku Beteli malire ake anakafika ku Luzi, kudutsa dziko la Ataroti kumene kumakhala Aariki.
3 Amalu, alalo da eso dabe la: idi amoga asili Ya: felidaide dunu ilia soge Bede Holone soge amo ganodini doaga: i. Amalu, ilia soge alalo da Gisa soge baligili, Medidela: inia Hano Wayabo amoga doaga: i.
Malirewo anatsikira cha kumadzulo kwa dziko la Yafuleti mpaka ku chigawo cha kumunsi kwa Beti-Horoni. Kuchokera kumeneko anapitirira mpaka ku Gezeri nʼkuthera ku Nyanja.
4 Yousefe egaga fi (Ifala: me fi amola Eso Dabe Ma: na: se fi) da amo soge lai dagoi.
Choncho Manase ndi Efereimu, ana a Yosefe analandira cholowa chawo.
5 Ifala: ime fi dunu ilia soge alalo da A: dalode A: da amoga eso mabadi la: idi asili gadodili Bede Houlone baligili,
Dziko la mabanja a fuko la Efereimu ndi ili: Malire a dzikolo anachokera kummawa kwa Ataroti Adari mpaka ku mtunda kwa Beti-Horoni.
6 Medidela: inia Hano Wayabo Bagade amoga doaga: i. Migimida moilai da ilia sogega gano ba: i. Eso mabadi la: ididili, alalo da selefale asili Da: ina: de Siailou eso mabadi la: ididili baligili, Yanoua moilaiga doaga: i.
Malirewo anapitirira mpaka ku nyanja. Mikimetati anali kumpoto kwake. Kuchokera kumeneko anakhotera cha kummawa kuloza ku Taanati Silo ndi kudutsa kumeneko cha kummawa mpaka ku Yanowa.
7 Amoga asili, alalo da A: dalode amola Na: iala baligili, Yeligou moilai bai bagade amola Yodane Hano doaga: i.
Ndipo kuchokera ku Yanowa anatsikira ku Ataroti ndi Naara, nakafika ku Yeriko ndi kukathera ku mtsinje wa Yorodani.
8 Alalo da eso dabe la: idi amo Dabua fisili, Gana Hano amoga asili, Medidela: inia Hano amoga doaga: i.
Kuchokera ku Tapuwa anapita kumadzulo mpaka ku mtsinje wa Kana ndi kukathera ku nyanja. Dziko ili linali cholowa cha mabanja afuko la Efereimu,
9 Ifala: ime fi da amo soge lai. Amola ilia da moilai afae afae amo Eso Dabe Ma: na: se fi ilia soge alalo ganodini amo lai dagoi.
kuphatikizapo mizinda yonse ndi midzi yake yopatsidwa kwa Efereimu, koma yokhala mʼkati mwa dziko la Manase.
10 Be ilia da Ga: ina: ne fi dunu Gisa soge amo ganodini esalu, amo gadili hame sefasi. Amaiba: le, Ga: ina: ne fi dunu da Ifala: ime fi amo ganodini wali esala. Be ilia da udigili bidi mae lawane hawa: hamosu dunu esala.
Iwo sanapirikitse Akanaani amene amakhala ku Gezeri ndipo mpaka lero Akanaani akukhala pakati pa Aefereimu koma amagwira ntchito ngati akapolo.

< Yosiua 16 >