< Yosiua 12 >
1 Isala: ili dunu da soge amo Yodane Hano eso mabadi la: idi amo lai dagoi. Amo da Anone Fago asili Yodane Fago asili Hemone Goumia doaga: i. Ilia da hina bagade aduna fane legei.
Aisraeli anagonjetsa dziko lonse la kummawa kwa Yorodani, kuyambira ku chigwa cha Arinoni mpaka ku phiri la Herimoni pamodzi ndi dera lonse la kummawa kwa Araba. Iwo anatenga dzikoli kukhala lawo, ndipo mafumu a dzikoli anali awa:
2 Afadafa da Saihone. E da A: moulaide hina bagade Hesiabone moilai bai bagadega esalu. Ea soge da Gilia: de la: idi amola Aloue (Anone Fago bega: dialu) asili Ya: boge Hano (amo hano da A: mone soge bega: alalo hamosu).
Sihoni mfumu ya Aamori, amene ankakhala mu Hesiboni. Iye analamulira kuyambira ku Aroeri mzinda umene uli mʼmphepete mwa mtsinje wa Arinoni, mpaka ku mtsinje wa Yaboki, umene uli mʼmalire mwa Aamori, kuphatikizanso theka la dziko la Giliyadi.
3 Amo soge ganodini, Yodane Fago (Ga: lili Hano Wayabo amoga ga asili Bedeyesimode [Bogoi Hano Wayabo amoga eso mabadi la: idi dialu] asili Bisiga Goumia doaga: i.)
Iye ankalamuliranso dera la chigwa cha Yorodani kuyambira ku Nyanja ya Kinereti, kummawa ndi kumatsika mpaka ku Beti-Yesimoti, mzinda umene unali kummawa kwa Nyanja ya Mchere ndi kutsikabe kummwera mpaka pa tsinde pa phiri la Pisiga.
4 Isala: ili dunu da Ba: isa: ne hina bagade amo Oge fane legei. Oge da fi Lefa: ime (gadenene ebelei fi) dunu. E da A: siadalode amola Edeliai ouligi.
Ogi mfumu ya mzinda wa Basani, amene anali mmodzi mwa otsala mwa Arefaimu. Iye ankakhala ku Asiteroti ndi Ederi.
5 Ea ouligisu soge ganodini da Hemone Goumi, Sa: lega amola Ba: isa: ne soge (amo da asili Gise amola Ma: iaga alaloga doaga: i) amola Gilia: de la: idi (eno la: idi Hesiabone hina bagade Saihone da gagui), amo soge ba: i dagoi.
Dera la ufumu wake linafika ku phiri la Herimoni, ku Saleka ndi dziko lonse la Basani mpaka ku malire ndi anthu a ku Gesuri Makati. Ufumu wake unaphatikizanso theka la Giliyadi mpaka ku malire a mfumu Sihoni ya ku Hesiboni.
6 Mousese amola Isala: ili dunu da amo hina bagade aduna fane legei dagoi. Hina Gode Ea hawa: hamosu dunu Mousese da ela soge amo Liubene fi, Ga: de fi amola eso mabadi la: idi Ma: na: se fi ilima i dagoi.
Mose mtumiki wa Yehova ndi Aisraeli anawagonjetsa ndipo anapereka dziko lawo kwa anthu a fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi theka la fuko la Manase kuti chikhale cholowa chawo.
7 Yosiua amola Isala: ili dunu da hina bagade huluane soge amo Yodane Hano ea eso dabe la: ididili esalebe, amo fane legei dagoi. Amo soge da Ba: ia: la Ga: de (Lebanone Fagoga galu) amoga ga asili Ha: ila: ge Goumi alaloga doaga: i. Yosiua da amo soge fifili, Isala: ili dunu eso huluane gaguma: ne, ilima i.
Yoswa ndi Aisraeli onse anagonjetsa mafumu onse okhala kumadzulo kwa mtsinje wa Yorodani kuyambira ku Baala-Gadi, ku chigwa cha Lebanoni mpaka ku phiri la Halaki, kumapita cha ku Seiri. Yoswa anagawira dzikolo mafuko a Israeli kuti likhale cholowa chawo.
8 Amo soge ganodini, agolo soge, eso dabe agolo fonobahadi soge, Yodane Fago, ea agolo, eso mabadi goumi soge amola ga (south) dialebe hafoga: i soge ba: i. Amo soge ganodini, musa: da Hidaide, A:moulaide, Ga: ina: naide, Belesaide, Haifaide amola Yebiusaide dunu esalebe ba: i.
Dziko limeneli linali dera la ku mapiri, chigwa cha kumadzulo, chigwa cha Yorodani, ku matsitso a kummawa, ndi dziko la chipululu la kummwera. Amene ankakhala mʼdzikoli anali Ahiti, Aamori, Akanaani, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi. Mafumu ake anali awa:
9 Isala: ili dunu da moilai bai bagade hagudu dedei ilia hina bagade hasali, amo,
mfumu ya Yeriko imodzi mfumu ya Ai (kufupi ndi Beteli imodzi
10 Yelusaleme amola Hibalone,
mfumu ya Yerusalemu imodzi mfumu ya Hebroni imodzi
11 Yamade amola La: igisi,
mfumu ya Yarimuti imodzi mfumu ya Lakisi imodzi
mfumu ya Egiloni imodzi mfumu ya Gezeri imodzi
mfumu ya Debri imodzi mfumu ya Gederi imodzi
14 Homa amola A: ila: de,
mfumu ya Horima imodzi mfumu ya Aradi imodzi
15 Libina amola Adala: me,
mfumu ya Libina imodzi mfumu ya Adulamu imodzi
16 Ma: gida amola Bedele,
mfumu ya Makeda imodzi mfumu ya Beteli imodzi
mfumu ya Tapuwa imodzi mfumu ya Heferi imodzi
18 A: ifege amola La: sa: ilone,
mfumu ya Afeki imodzi mfumu ya Lasaroni imodzi
19 Ma: idone amola Ha: iso,
mfumu ya Madoni imodzi mfumu ya Hazori imodzi
20 Similone Milone amola Agasa: fe,
mfumu ya Simuroni Meroni imodzi mfumu ya Akisafu imodzi
21 Da: ianage amola Megidou,
mfumu ya Taanaki imodzi mfumu ya Megido imodzi
22 Gidese amola Yogeniame (Gamele soge ganodini),
mfumu ya Kadesi imodzi mfumu ya Yokineamu ku Karimeli imodzi
23 Do (wayabo bagade bega: ) amola Gouimi,
mfumu ya Dori ku Nafoti Dori imodzi mfumu ya Goyini ku Giligala imodzi
24 amola Dusa. Huluane ilia da hina bagade31 agoane hasali.
mfumu ya Tiriza imodzi mafumu onse pamodzi analipo 31.