< Youna 3 >

1 Be Hina Gode da bu Younama sia: i.
Ndipo Yehova anayankhula ndi Yona kachiwiri kuti,
2 “Di Ninefe moilai bai bagade fi, ilima asili, sia: na dima sia: ne i amo, dia ilima olelema.”
“Nyamuka, pita ku mzinda waukulu wa Ninive ndipo ukalalikire uthenga umene ndikupatsa.”
3 Amabeba: le Youna da Hina Gode ea sia: nabawane, Ninefe moilai bai bagade amoga Ea sia: olelemusa: asi. Ninefe da moilai bai bagade galu. Amodili ahoanoba, eso osodayale galagai.
Yona anamvera mawu a Yehova ndipo anapita ku Ninive. Tsono Ninive unali mzinda waukulu kwambiri; wofunika masiku atatu kuwudutsa.
4 Amola Youna da Gode Ea sia: amo moilai bai bagade ganodini olelemusa: asili, eso afaega asili, amane sisia: i, “Eso 40 agoane esalu, Gode da Ninefe fi gugunufinisimu!”
Yona analowa mu mzindawo, nayenda ulendo wa tsiku limodzi. Iye ankalalikira kuti, “Atsala masiku makumi anayi kuti Ninive awonongedwe.”
5 Ninefe dunu fi ilia Gode ea sia: amo nababeba: le, dafawane dawa: i, amola ilia da ha: i mae moma: ne, sema ligi. Dunu huluane amola ouligisu dunu huluane ilia da eboboi abula gaga: ne, Hina Godema asigi hou amola sinidigisu hou olelema: ne.
Anthu a ku Ninive anakhulupirira Mulungu. Analengeza kuti aliyense, wamkulu ndi wamngʼono yemwe asale zakudya ndipo avale chiguduli.
6 Amo sia: nababeba: le, Ninefe hina bagade dunu e fisu ganodini esalu amo wa: legadole amola ea abula noga: i amo gisa: le amola eboboi abula salawane, nasubu sogebi ganodini fi.
Mfumu ya ku Ninive itamva nkhaniyi, inatsika pa mpando wake waufumu, nivula mkanjo wake waufumu ndipo inavala chiguduli ndi kukhala pansi pa fumbi.
7 Amanoba, Ninefe hina bagade ea dunu fifi lai huluane ilima hamoma: ne sisa: lai. E amane sia: i, “Goe da na sia: amola eagene ouligisu dunu huluane amola amo ilia sia: Dilia huluane da ha: i manu mae moma. Dunu fifi lai amola ohe fi, dili huluane ha: i amola hano mae moma.
Tsono mfumuyo inalengeza mu Ninive kuti, “Mwa lamulo lochokera kwa mfumu ndi akalonga ake: “Munthu aliyense kapenanso nyama, ngʼombe kapena nkhosa, zisadye kanthu kalikonse; musazilole kuti zidye kapena kumwa.
8 Dunu fi amola ohe fi huluane da abula eboboi salima: mu. Dunu huluane afae afae da hina: wadela: i hou amo fisili, amola asigili Godema sia: ne gadoma: mu.
Koma anthu avale ziguduli, ndipo nyamanso aziveke ziguduli. Munthu aliyense azifuwula kwa Mulungu ndi mphamvu zake zonse. Anthuwo asiye makhalidwe awo oyipa ndi machitidwe achiwawa.
9 Be Gode da Ea asigi bu sinidigisia, ninima asigimu amola ninia da hame bogogia: ma: bela: ?”
Angadziwe ndani? Mwina Mulungu nʼkutikhululukira ndipo mwa chifundo chake nʼkuleka kutikwiyira, ifeyo osawonongedwa.”
10 Gode Ea ilia hou amo ba: i, amola ilia da Ema bu sinidigi amo ba: i. Amabeba: le, Gode da Ea ilima se imunu dawa: i amo hame i.
Mulungu ataona zimene anthuwo anachita, ndi mmene anasiyira makhalidwe awo oyipa, anawachitira chifundo ndipo sanabweretse chiwonongeko chimene anawaopseza nacho.

< Youna 3 >