< Yoube 4 >

1 Ilaifa: se da amane sia: i,
Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha kuti,
2 “Yoube! Na da dima sia: sea, di da ougima: bela: ? Na bu ouiya: mu hamedei ba: sa!
“Ngati wina atakuyankha, kodi ungakhumudwe? Koma ndani angakhale chete wosayankhula?
3 Di da dunu bagohame ilima olelesu. Di da dunu bagohame, ili gasa lama: ne fidisu.
Taganiza momwe iwe walangizira anthu ambiri, momwe walimbitsira anthu ofowoka.
4 Dunu afae da helebeba: le goaiyane didigabone dafaloba, dia sia: beba: le, e da dogo denesini, aligi.
Mawu ako analimbitsa anthu ofuna kugwa; unachirikiza anthu wotha mphamvu.
5 Be wali bidi hamosu da dima doaga: i, amola di da amoga gasa fili mae aligili sidadabonei agoai ba: sa.
Koma tsopano mavuto akufikira ndipo wataya mtima, zakukhudza ndipo uli ndi mantha.
6 Di da Godema nodone sia: sa hawa: hamosu, amola dia esalusu amo ganodini dima sia: i afae hame fada: su, amaiba: le di da dia dafawane hamoma: beyale dawa: su amoga ga: nasili aligimu da defea.
Kodi kuopa Mulungu kwako sindiko kulimbika mtima kwako? Ndipo moyo wako wosalakwa ndiye chiyembekezo chako?
7 Waha bu sinidigili, musa: hamosu dawa: ma! Nowa da moloidafa hou hamoi, be e da baligiliwane se nabasu ba: bela: ? Agoaiwane hame ba: su.
“Ganiza bwino tsopano: Kodi munthu wosalakwa anawonongekapo nʼkale lonse? Nʼkuti kumene munthu wolungama mtima anaphedwa?
8 Na da ba: loba, dunu ilia wadela: i hou fawane hawa: agoane bugimusa: dawa: lala. Be waha ilia da wadela: i hou bugi gamisu agoane gugunufinisisu hou ba: sa.
Monga ndaonera ine, anthu amene amatipula zoyipa, ndi iwo amene amadzala mavuto, amakolola zomwezo.
9 Gode da amo wadela: i hamosu dunuma ougi bagadeba: le, E da mulu bagade defele ili wadela: lesisa.
Iwo amaphedwa ndi mpweya wa Mulungu; amawonongeka ndi mpweya waukali wa mkwiyo wake.
10 Wadela: i hou hamosu dunu ilia da laione wa: me agoane husa amola hagega: sa. Be Gode da ili ouiya: lesisa amola ilia bese gugulisisa.
Mikango imabangula ndi kulira, komabe mano a mikango yamphamvu amathyoledwa.
11 Ilia da laione wa: me amo da ohe fane manu hamedei ba: sa, amola ha: i manu hame galea, bogobe, amo defele bogogia: sa. Ilia da bogosea, ilia mano huluane da afagogosa.
Mkango umafa chifukwa chosowa nyama, ndipo ana amkango amamwazikana.
12 Eso afaega, sia: nama misi da ouiya: lewane nama mabeba: le, na da fada: ne hame nabi.
“Mawu anabwera kwa ine mwamseri, makutu anga anamva kunongʼona kwake.
13 Amo sia: da golaiya wadela: i liligi agoai ba: beba: le amoga na da fofogadigili nedigi.
Mʼkati mwa maloto ochititsa mantha usiku, nthawi imene anthu amagona tulo tofa nato,
14 Na da fofogadigili, beda: ga, na da: i huluane yagugui.
ndinagwidwa ndi mantha, ndi kuyamba kunjenjemera ndipo mafupa anga onse anaweyeseka.
15 Fo hisi da na odagia fogala: le, na da beda: ga, na dialuma hinabo afafai.
Pamenepo mzimu unadutsa pamaso panga, ndipo ubweya wa pa thupi langa unayima kuti njoo.
16 Na da liligi afae lelebe ba: i, be na da sosodolaligi, be amo liligi na fada: ne hame dawa: i galu. Eno liligi da ouiya: le dialebe ba: i. Amalalu, na da amane sia: be nabi,
Chinthucho chinayimirira koma sindinathe kuzindikira kuti chinali chiyani. Chinthu chinayima patsogolo panga, kunali zii ndipo ndinamva mawu akuti,
17 “Dunu afae da Gode Ea ba: ma: ne moloidafa esalabala? Dunu afae da Osobo Bagade Hahamosu Ea ba: ma: ne ledo hamedei esalabala?
‘Kodi munthu angathe kukhala wolungama kupambana Mulungu? Kodi munthu angathe kukhala wangwiro kupambana Mlengi wake?
18 Gode da Hebene ganodini hawa: hamosu dunu, ilia da Ea liligi noga: le ouligima: ne hame ilegesa. E da Ea a: igele dunu amolawane ilima giadofasu hou ba: sa.
Ngati Mulungu sakhulupirira atumiki ake omwe, ngati Iye amawapeza angelo ake ndi cholakwa,
19 Amaiba: le, dia dawa: loba Gode da osoboga hamoi dunu amo Ea liligi noga: le ouligima: ne ilegema: bela: ? Hame mabu! Bai osobo bagade dunu da guluga hamoiba: le, aowaba defele hedolo gagoudai dagoi ba: sa.
nanga kuli bwanji ndi iwo amene amakhala mʼnyumba zadothi, amene maziko awo ndi fumbi, amene amathudzuka mosavuta ngati kadziwotche!
20 Amabela: ? Ninia da hahabe esalebe ba: sa, be mae daeyagili, bogoi dagoi ba: mu.
Mmawa ali moyo, pofika madzulo afa; mwakachetechete, amawonongeka kwamuyaya.
21 Ninia gagui huluane da bu sasamogene dagoi ba: mu. Ninia asigi dawa: su hame fada: iyawane bogosa.”
Kodi zonse zimene ali nazo sizimatheratu, kotero kuti amafa osadziwa nʼkanthu komwe?’

< Yoube 4 >