< Yoube 37 >

1 Na da isu gibula bobodobe ba: sea, na dogo da gilugilusa.
“Mtima wanga ukulumphalumpha pa chimenechinso ndipo ukuchoka mʼmalo mwake.
2 Dilia huluane! Gode Ea sia: nabima! Gugelebe amo da Ea lafidili mabe, nabima!
Tamverani! Tamverani kubangula kwa liwu lake, kugunda kumene kukuchokera mʼkamwa mwake.
3 Gode da ha: ha: na diga: be muagadodili iasisa. Ha: ha: na da osobo bagade na: iyado bega: bega: ahoa.
Iye amaponya chingʼaningʼani chake pansi pa thambo lonse ndipo amachitumiza ku dziko lapansi.
4 Amasea, Gode Ea gogonomosu naba. Amo da gugelebe ea gogonomobe bagade. Amola ha: ha: na da mae fisili nene gala: lala.
Pambuyo pake kubangula kwake kumamveka. Iye amabangula ndi liwu lake laulemerero. Pamene wabangula, palibe chimene amalephera kuchita.
5 Gode da sia: sea, fofogadigisu liligi da doaga: sa. Ninia da agoai liligi hame dawa: digisa.
Liwu la Mulungu limabangula mʼnjira zambiri zodabwitsa Iye amachita zinthu zazikulu zimene sitingathe kuzimvetsa.
6 Ea sia: beba: le, mugene da osoboga daha. Gode da gibu bagadedafa osobo bagadega iasisa.
Amalamula chisanu chowundana kuti, ‘Igwa pa dziko lapansi,’ ndipo amalamulanso mvula yamawawa kuti, ‘Khala mvula yamphamvu.’
7 E da dunu ilia hawa: hamosu dagolesisa. E da Ea gasa bagade hamobe ilima olelesa.
Kuti anthu onse amene anawalenga athe kuzindikira ntchito yake. Iye amalepheretsa anthu kugwira ntchito zawo.
8 Sigua ohe fi da ilia diasuga ahoa.
Zirombo zimakabisala ndipo zimakhala mʼmaenje mwawo.
9 Gibula bobodoi isu da ga (north) amodili maha. Anegagidafa fo da ga (south) amodili maha.
Mphepo yamkuntho imatuluka ku malo ake, kuzizira kumatuluka mʼmphepo yamkunthoyo.
10 Gode Ea mifo da hano anegagini, ga: nasi mugene hamosa.
Mpweya wa Mulungu umawunditsa madzi ndipo madzi a mʼnyanja amawuma kuti gwaa.
11 Haha: na da mu mobiga nene gala: sa.
Iye amadzaza mitambo ndi madzi a mvula, amabalalitsa zingʼaningʼani zake kuchokera mʼmitambomo.
12 Mumobi da Gode Ea hanaiga ahoa. Osobo bagade huluane ganodini, mumobi da Gode Ea hamoma: ne sia: be defele hamosa.
Mulungu amayendetsa mitamboyo mozungulirazungulira dziko lonse lapansi kuti ichite zonse zimene Iye akufuna pa dziko lapansi.
13 Gode da osobo bagadega hano soga: ma: ne gibu iaha. Eso enoga E da osobo bagade dunu ilima se dabe ima: ne gibu iaha. Amola eso enoga E da ilia hahawane ba: ma: ne, gibu iaha.
Iye amagwetsa mvula kuti alange anthu, kapena kubweretsa chinyontho pa dziko lapansi kuti aonetse chikondi chake.
14 Yoube! Di fonobahadi ouesalu, nabima! Gode Ea noga: idafa hamobe amo dadawa: ma!
“Abambo Yobu, tamvani izi; imani ndipo muganizire ntchito zodabwitsa za Mulungu.
15 Gode da ha: ha: na nene gala: ma: ne sia: sa! E da habodane agoai hamosala: ? Di amo dawa: sala: ? E da habodane ha: ha: na mumobiga nene gala: ma: ne hamosala: ?
Kodi mukudziwa momwe Mulungu amayendetsera mitambo ndi kuchititsa kuti kukhale zingʼaningʼani?
16 Gode da fofogadigiliwane hamobela: le, mumobi da muagado gila ahoa. Di da amo mumobi ilia gila ahoabe hou ea bai dawa: sala: ?
Kodi mukudziwa momwe Mulungu amayalira mitambo, ntchito zodabwitsa za Iye amene ndi wanzeru zangwiro?
17 Hame mabu! Ga (south) dogoloi fo da soge wadela: sea, di da dogolobeba: le, se naba.
Inu amene mʼzovala zanu mumatuluka thukuta pamene kunja kwatentha chifukwa cha mphepo yakummwera,
18 Gode da mu fadegale gagasea, di da E fidimu dawa: sala: ? E da mu ga: nasi gula enemei defele hamosea, di da E fidimu dawa: sala: ?
kodi mungathe kuthandizana naye kutambasula thambo limene ndi lolimba ngati chitsulo?
19 Gode! Ninia Dima sia: mu amo Dia ninima olelema! Ninia asigi dawa: su da hame gala. Ninia sia: mu gogolesa.
“Tiwuzeni ife zoti tikanene kwa Iye; sitingathe kufotokoza mlandu wathu chifukwa cha mdima umene uli mwa ife.
20 Na da Godema sia: musa: hame adole ba: mu. Bai na da abuliba: le, E na gugunufinisisima: ne logo doasima: bela: ?
Kodi nʼkofunika kumudziwitsa Mulungu kuti ndili naye mawu? Kodi kutero sikuchita ngati kupempha kuti ndiwonongeke?
21 Wali, mu da: iya hadigi da si nenemeginana. Amaiba: le, ninia ba: mu si gasenei. Mu da foga fulaboiba: le, fofoloi gala.
Tsopano munthu sangathe kuyangʼana dzuwa, ndi kunyezimira mlengalenga, kuwomba kwa mphepo kutachotsa mitambo yonse.
22 Ninia da ga (north) la: idiga gouli agoai hadigi ba: sa. Amo da Gode E hadigi, amola amoga ninia da beda: sa.
Kuwala kwake kumaonekera cha kumpoto; Mulungu amabwera ndi ulemerero woopsa.
23 Gode Ea gasa da bagadedafaba: le, ninia da E gadenena misunu da hamedei. Ea ninima hamobe liligi huluane da moloidafa amola defele hamosa.
Wamphamvuzonse sitingathe kumufikira pafupi ndi wa mphamvu zoposa; pa chiweruzo chake cholungama ndi mʼchilungamo chake chachikulu Iye sapondereza anthu ozunzika.
24 Amaiba: le, dunu huluane ilia Ema beda: su hou da fofogadigisu liligi hame. E da nowa dunu da hidale, hifae da asigi dawa: su bagade lai dagoiyale sia: sea, E da amo dunu ea sia: hame naba.
Nʼchifukwa chake anthu amamuopa kwambiri, kodi saganizira za onse amene amaganiza kuti ndi anzeru?”

< Yoube 37 >