< Yoube 36 >

1 Fonobahadi eno gebewane ouesaloma! Amola na sia: nabima! Bai na da Gode Ea sia: dima alofele iaha.
Ndipo Elihu anapitirira kuyankhula nati:
2
“Mundilole pangʼono pokha ndipo ndikuonetsani kuti zilipo zambiri zoti ziyankhulidwe mʼmalo mwa Mulungu.
3 Na asigi dawa: su da bagade. Na da na asigi dawa: suga, na Hahamosu Gode da moloidafa, amo dima olelemu.
Nzeru zanga ndimazitenga kutali; ndidzaonetsa kulungama kwa Mlengi wanga.
4 Na da dima ogogosu hamedafa dawa: Na da dia midadi, bagadedafa dawa: su dunu agoai lela.
Ndithudi mawu anga si abodza; wanzeru zangwiro ali ndi inu.
5 Gode da gasa bagadedafa. E da dunu afae hame higasa. E da liligi huluanedafa dawa:
“Mulungu ndi wamphamvu, koma sanyoza anthu; Iye ndi wamphamvu, ndipo ndi wokhazikika pa cholinga chake.
6 E da wadela: i hamosu dunu gebewane esaloma: ne, logo hame doasisa. E da hame gagui dunuma mololedafa hamosa.
Salola oyipa kuti akhalebe ndi moyo koma amapereka ufulu kwa anthu osautsidwa.
7 E da molole hamosu dunu gaga: sa. E da ili hina bagade dunu defele, fi ouligisu hou ilima iaha. Amola dunu eno ilima eso huluane nodoma: ne, logo doasisa.
Iye saleka kuyangʼanira anthu olungama; amawayika kuti alamulire pamodzi ndi mafumu ndipo amawalemekeza mpaka muyaya.
8 Be fedege agoane, dunu ilia da wadela: le hamoiba: le sia: inega la: gili se nabawane esalea,
Koma ngati anthu amangidwa ndi unyolo, ndipo akondwa ndi zingwe zamasautso,
9 E da ilia wadela: i hou amola hidale gasa fi hou ilima olelesa.
Iye amawafotokozera zomwe anachita, kuti iwo anachimwa modzikuza.
10 E da ilima wadela: i hou yolesima: ne sisasu, amo noga: le nabima: ne sesesa.
Mulungu amawatsekula makutu kuti amve malangizo ake ndipo amawalamula kuti alape zoyipa zawo.
11 Ilia da Gode Ea sia: nabasea, amola Ema noga: le hawa: hamosea, ilia da olofole amola bagade gaguiwane esalumu.
Ngati iwo amumvera ndi kumutumikira, adzatsiriza masiku a moyo wawo mwamtendere, adzatsiriza zaka zawo mosangalala.
12 Be amane hame hamosea, ilia da hame dawa: iwane bogomu. Fedege agoane, ilia da hano degele, bogosu sogega doaga: mu.
Koma ngati samvera, adzaphedwa ndi lupanga ndipo adzafa osadziwa kanthu.
13 Gode Ea hou hame dawa: be dunu da mae fisili, gebewane ougiwane diala. Gode da ilima se dabe iasea, amolawane, ilia da Gode Ea fidima: ne hame sia: ne gadosa.
“Anthu osapembedza amasunga mkwiyo mu mtima mwawo; akawalanga, safuwulira kwa Iye kupempha thandizo.
14 Ilia da ayeligiwane bogosa. Ilia da ogogosu ‘gode’ ilima nodone sia: ne gadosu sogebiga, sama ea sama adole lasu hou bagadewane hamonanebeba: le, ilia da gasa guminisiba: le, hedolo bogosa.
Amafa akanali achinyamata, pakati pa amuna achiwerewere a kumalo azipembedzo.
15 Be Gode da dunu ilia se nabasu hou amoga ilima olelesa. Amola ilia bidi hamosu ganodini, ilia si fadegasa.
Koma ovutika, Iye amawapulumutsa pa mavuto awo; Mulungu amawayankhula mʼmasautso awowo.
16 Di da se nabawane bidi hamosu ganodini esaloba, Gode da di gadili oule asili gaga: iwane esaloma: ne hamoi. Dia ha: i manu da bagade lelegela heda: i ba: i.
“Iye akukukopani inu kuti muchoke mʼmasautso, kuti mupite ku malo aakulu kumene kulibe chokutchingani, kumalo a mpumulo kumene kuli chakudya chabwino kwambiri.
17 Be wali dia hamobe defele, E da dima se dabe iaha.
Koma tsopano inu mwapezeka wopalamula chifukwa cha kuyipa kwanu; chiweruzo ndi chilungamo chakugwerani.
18 Dawa: ma! Hano suligisu hou da dima ogogosa: besa: le, amola bagade gagui hou da di giadofale oule ahoasa: besa: le, dawa: ma.
Muchenjere kuti wina asakukopeni ndi chuma; musalole kuti chiphuphu chachikulu chikusocheretseni.
19 Di da digini fidima: ne wele sia: sea, fidisu hame ba: mu. Amola dia gasa bagade hou da wali dima fidimu hamedei.
Kodi chuma chanu kapena mphamvu zanu zonse zingakusungeni kotero kuti simungakhale pa masautso?
20 Fifi asi gala da gasia wadela: lesi dagoi ba: mu. Be amo gasi da doaga: ma: ne mae hanaiwane dawa: ma.
Musalakalake kuti usiku ubwere, pakuti ndiyo nthawi imene anthu adzawonongeka.
21 Wadela: i hou hamosa: besa: le, dawa: ma. Bai dia wadela: le hamosu hedofama: ne, Gode da dima se nabasu hou iasi dagoi.
Muchenjere kuti musatembenukire ku uchimo, chifukwa uchimowo ndiwo unabweretsa kuzunzika kwanu.
22 Gode Ea gasa da bagadedafa, amo bu dawa: ma. E da olelesu dunu huluane ilia hou baligisa.
“Taonani, Mulungu ndi wamkulu ndiponso ndi wamphamvu. Kodi ndi mphunzitsi uti amene angafanane naye?
23 Dunu afae da Godema Ea hamomu logo olelemu da hamedei. Amola E da wadela: le hamonana, amo Ema diwaneya udidimu da hamedei.
Kodi ndani amene anamuwuzapo Mulungu zoti achite, kapena kumuwuza kuti, ‘Inu mwachita chinthu cholakwa?’
24 Eso huluane, dunu da Ea hamonanu ba: beba: le, Ema nodonanu. Di amola Ema nodonanumu da defea
Kumbukirani kutamanda ntchito zake zimene anthu amaziyamika mʼnyimbo.
25 Dunu huluane da Ea hamonanu ba: i dagoi. Be ninia da sedaga lelawane, Ea hamobe ba: lala.
Anthu onse amaziona ntchitozo; anthuwo amaziona ali kutali.
26 Ninia Ea bagadedafa hou huluane, amola Ea esalebe ode amo dawa: mu da hamedei.
Ndithudi, Mulungu ndi wamkulu, sitimudziwa nʼpangʼono pomwe! Chiwerengero cha zaka zake nʼchosadziwika.
27 Gode Hi da osobo bagadega hano lale, amola amo afadenene, gibu dadadi hamosa.
“Mulungu ndiye amakweza timadontho tamadzi kuthambo, timene timasungunuka nʼkukhala mvula;
28 Ea hamobeba: le, gibu da mumobi amo gadodili dadafusa. Gibu da osobo bagade dunu huluane fidisa.
mitambo imagwetsa mvulayo ndipo mvulayo imavumbwa pa anthu mokwanira.
29 Gode da mu ganodini esala. Be dunu afae da mu mobi ea ahoabe hou hamedafa dawa: Amola gugelebe ea geloloda: iya ahoabe hame dawa:
Kodi ndani amene angadziwe momwe mitambo imayendera, momwe Iye amabangulira kuchokera kumalo ake?
30 Gode da ha: ha: na diga: be muagadodili iasisa. Be hano wayabo bagade ea lugudu da gasiwane dialebe ba: sa.
Taonani momwe amawalitsira zingʼaningʼani pa malo ake onse, zimafika ngakhale pansi pa nyanja.
31 Gode da amanewane osobo bagadema ha: i manu bagadewane iaha.
Umu ndi mmene Iye amalamulira mitundu ya anthu ndi kuwapatsa chakudya chochuluka.
32 E da Ea loboga ha: ha: na gagulaligisa. E da ha: ha: na amoma Ea ilegei amogai disili gala: ma: ne olelesa.
Amadzaza manja ake ndi zingʼaningʼani, ndipo amazilamulira kuti zigwe pamalo pamene Iye akufuna.
33 Gugelebe da mulu ea manebe olelesa. Amola bulamagau ili da gugelebe nabasea, isu gibula bobodobe da manebe dawa: sa.
Mabingu ake amalengeza za kubwera kwa mvula yamkuntho; ngʼombe nazo zimalengeza za kubwera kwake.

< Yoube 36 >