< Yoube 32 >
1 Yoube da ea hou da moloidafa dafawaneyale dawa: beba: le, ea sama da ema bu adole ima: ne yolesi dagoi.
Tsono anthu atatuwa analeka kumuyankha Yobu, chifukwa chakuti iyeyo ankadziona kuti ndi wolungama.
2 Be dunu eno la: ididili esalu, ea dio amo Ilaihiu, da ougi ba: i amola amo bu gumimu hamedei ba: i. Bai Yoube da hina: hou gaga: le, Godema diwaneya udidilalu. (Ilaihiu da Ba: lagele ea mano amola Ba: lagele da Base egaga fi dunu. Ea sosogo fi da La: me.)
Koma Elihu, mwana wa Barakeli, wa fuko la Buzi, wa banja la Ramu, anapsera mtima kwambiri Yobu chifukwa choti Yobuyo anakana kuvomera kuti anachimwa ndi kuti Mulungu anakhoza pomulanga.
3 E da Yoube ea sama udiana ilima amolawane ougi galu. Bai ilia da Youbema bu adole imunu logo hamedei ba: i. Amaiba: le, dunu eno ba: ma: ne, Gode Hi da giadofaiyale, eno dunu ilia da agoane dawa: i galu.
Anapseranso mtima abwenzi ake atatu aja chifukwa sanapeze njira yomutsutsira Yobu, ngakhale iwo anamupeza kuti anali wolakwa.
4 Ilaihiu e fawane da goi ayeligi galu. Amaiba: le, e da ouesalu, eno dunu ilia da sia: i dagoiba: le fawane sia: i.
Tsono Elihu anadikira kuti ayankhule ndi Yobu chifukwa choti abwenziwo anali akuluakulu kupambana iyeyo.
5 E da eno dunu udiana da Yoube ea adole ba: su amoga dabe hame adole iabeba: le, e da ougi ba: i.
Koma Elihu ataona kuti anthu atatuwo analibe mawu oti ayankhulenso, iye anapsa mtima.
6 E da muni amane sia: i, “Na da ayeligi, be dilia da asigilai dunu. Amaiba: le, na da na asigiga dawa: i liligi dilima adomu beda: i galu.
Choncho Elihu mwana wa Barakeli wa fuko la Buzi anati: “Ine ndine wamngʼono, inuyo ndinu akuluakulu, nʼchifukwa chake ndimaopa, ndimachita mantha kuti ndikuwuzeni zimene ndimadziwa.
7 Na da nisu amane sia: i, asigilai dunu dilia fawane sia: mu da defea. Dilia bagade dawa: su amoga ninia huluane dawa: ma: ne adomu da defea galu.
Ndimaganiza kuti, ‘Ayambe ndi akuluakulu kuyankhula; anthu amvulazakale ndiwo amaphunzitsa nzeru.’
8 Be Gode Bagadedafa Ea A: silibu, Hi fawane da ninima misini, ninima asigi dawa: su bagade iaha.
Koma mzimu wa Mulungu mwa munthu, mpweya wa Wamphamvuzonse, ndi umene umapereka nzeru zomvetsa zinthu.
9 Ninia da: i hamosea, bagade asigi dawa: su amola moloidafa hou dawa: i hame laha.
Si okalamba amene ali ndi nzeru, si amvulazakale okha amene ali ndi nzeru zomvetsa zinthu zimene zili zoyenera.
10 Amaiba: le, na hanai da dilia na sia: nabimu! Na asigiga dawa: i amo na da dilima adomusa: , logo doasima.
“Nʼchifukwa chake ndikuti, ‘Mvereni; inenso ndikukuwuzani zimene ndikuzidziwa.’
11 Dilia sia: nanoba, na da gebewane nabalu. Dilia da asigi dawa: su bagade sia: hogolalebeba: le, na da ouesalu.
Ndadikira nthawi yonseyi, ndimamvetsera mwachidwi zimene mumayankhula, pamene mumafunafuna mawu oti muyankhule,
12 Na da ha: giwane sosodolalu, amola dilia dafabe ba: i. Dilia da Yoube ea sia: be da giadofaiyale, dilia didili hame hamoi.
ineyo ndinakumvetseranidi. Koma palibe ndi mmodzi yemwe wa inu amene anatsutsa Yobu; palibe aliyense wa inu amene anamuyankha mawu ake.
13 Dilia abuliba: le, dilia da bagade dawa: su hou ba: i dagoi, amo sia: sala: ? Dilia da dafai dagoi. Amaiba: le, Gode Hi fawane da Youbema bu adole imunu gala.
Musanene kuti, ‘Ife tapeza nzeru; Mulungu ndiye amutsutse, osati munthu.’
14 Yoube da nama hame sia: i. E da dilima sia: su. Be na da dilia adole iabe defele, ema hame adole ia: noba.
Koma Yobu sanayankhule motsutsana ndi ine, ndipo ine sindimuyankha monga mmene inu mwamuyankhira.
15 Yoube! Ilia sia: da dafai dagoi. Ilia dima bu adole imunu gogolesa.
“Iwo asokonezeka ndipo alibe choti ayankhulenso; mawu awathera.
16 Ilia da wali sia: hamedene agoane udigili lela. Amaiba: le, na da ouiya: le bu ouesaloma: bela: ?
Kodi ine ndidikire chifukwa iwo sakuyankhula tsopano, pakuti angoyima phee wopanda yankho?
17 Hame mabu! Na da dima adole imunu. Na asigi dawa: su liligi, na da dima adomu.
Inenso ndiyankhulapo tsopano; nanenso ndinena zimene ndikudziwa.
18 Na da sia: ma: ne ouesalumu hamedei. Na da na sia: negabe logo hedofamu hamedei ba: sa.
Pakuti ndili nawo mawu ambiri, ndipo mtima wanga ukundikakamiza;
19 Na da sia: mu logo hame ba: sea, na da ohe gadofo amo da gaheabolo waini hano amoga nabai gala, amo defele fudagala: mu.
mʼkati mwanga ndili ngati botolo lodzaza ndi vinyo, ngati matumba a vinyo watsopano amene ali pafupi kuphulika.
20 Hamedei! Na da bu ouiya: le esalumu da hamedeidafa.
Ndiyenera kuyankhula kuti mtima utsike; ndiyenera kutsekula pakamwa panga ndi kuyankha.
21 Na da dunu afae amomagale hame sia: mu. Na da dunu afae amoma dabua hahayafuli hame sia: mu.
Sindidzakondera munthu wina aliyense, kapena kuyankhula zoshashalika,
22 Na da osobo bagade dunuma hahayafuli sia: mu hamedei ba: sa. Amane hamoi ganiaba, Gode da hedolowane nama se dabe ia: noba.
pakuti ndikanakhala wa luso loyankhula moshashalika, Mlengi wanga akanandilanga msanga.”