< Yoube 26 >

1 Yoube da amane sia: i,
Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2 “Dilia da na fidiba: ! Na da hahani amola gasa hame galebe.
“Wamuthandizadi munthu wopanda mphamvu! Walimbitsadi dzanja la munthu wofowoka!
3 Di da nama fada: i sia: noga: idafa olelesase! Na da gagaoui dunu, be dilia da dilia bagade dawa: su nama olelesase!
Wapereka malangizo kwa munthu amene alibe nzeru! Ndipotu waonetsadi nzeru zochuluka!
4 Dilia sia: huluane, nowa da nabima: bela: ? Nowa da olelebeba: le, dilia amane sia: sala: ?” Bilida: de da amane sia: i,
Kodi wakuthandiza ndani kuti uyankhule mawu awa? Ndipo ndi mzimu wa yani umene unayankhula pakamwa pako?
5 “Bogoi dunu ilia a: silibu osobo hagududi hano amo ganodini fofogosa.
“Mizimu ya anthu akufa ikunjenjemera pansi pa madzi, ndi zonse zokhala mʼmadzimo.
6 Gode da bogoi dunu ilia soge ba: lala. Ea siga mae ba: ma: ne, amo soge da hame alaloi. (Sheol h7585)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol h7585)
7 Gode da ga (north) mu amo gasi gagai. E da osobo bagade hame fufua amo ganodini gosagisi.
Mulungu anayala thambo la kumpoto pa phompho; Iye anakoloweka dziko lapansi mʼmalo mwake pamene panali popanda nʼkanthu komwe.
8 Gode Hi fawane da mu mobi amo hanoga nabalesisa. Amola ilia dioi bagadeba: le, ili mae fudagala: ma: ne hamosa.
Amasunga madzi ambiri mʼmitambo yake, koma mitamboyo siphulika chifukwa cha kulemera kwa madziwo.
9 E da oubi ufa: amo mobiga uligilisisa.
Iye amaphimba mwezi wowala, amawuphimba ndi mitambo yake.
10 E da gasi amola hadigi mogima: ne, osobo bagade dogoa sisiga: le dedenesi.
Mulungu anawalembera madzi malire wonga uta, kukhala malire pakati pa kuwunika ndi mdima.
11 Fedege agoane, E da bada amoga mu udidili gaguia gadosa, amoma badugusia, ilia da beda: ga fofogosa.
Mizati yochirikiza mitambo yakumwamba imanjenjemera, ndi kudabwa pa kudzudzula kwake.
12 E da Ea gasaga, hano wayabo bagade hasalasi. E da gasa bagadeba: le, wadela: i ohe bagade La: iha: be gugunufinisi.
Ndi mphamvu zake anatontholetsa nyanja; ndi nzeru zake anakantha chirombo cha mʼmadzi chija chotchedwa Rahabe.
13 Gode Ea lafi holo da mu haisewe hamoi. Amola ohe bagade da hobeamusa: dawa: loba, E da amo Ea loboga medole legei.
Ndi mpweya wake anayeretsa zamumlengalenga, dzanja lake linapha chinjoka chothawa chija.
14 Be Ea gasa bagade hou da amo bagadewane baligisa. Amo hou ninia nababeba: le, da sadoga sia: agoai gala. Bai nowa da Gode Ea Gasa Bagadedafa hou dawa: ma: bela: ?”
Zimenezi ndi pangʼono chabe mwa ntchito yake; tingomva pangʼono za Iye ngati kunongʼona! Kodi ndani angathe kudziwa kukula kwa mphamvu zake?”

< Yoube 26 >